< 2 Akorinto 1 >

1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu, pamodzi ndi mʼbale wathu Timoteyo, Kulembera mpingo wa Mulungu mu Korinto, pamodzi ndi oyera mtima onse mu Akaya monse.
U Paulo, utumwe wa Yesu hlugano lwa Ngulubhi, nu Timotheo uholo witu, hwubhibhanza isha hu Korintho, na hwa Kristu bhonti bhabhali humukoa gwanti gwa hu Akaya.
2 Mukhale ndi chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
Ulusajilo no lusehelo lwalufuma hwa Ngulubhi Yesu Kristu lubhe namwe.
3 Alemekezeke Mulungu, Atate a Ambuye athu Yesu Khristu, Atate achifundo chonse, Mulungu wachitonthozo chonse.
Alumbwe Ungulubhe wa Gosi witu uYesu Kristu, umwene Ngulubhi welusajilo nantele Ngulubhi we luzinzyo lwoti.
4 Iye amatitonthoza ife mʼmavuto athu onse, kuti ifenso tithe kutonthoza amene ali pavuto lililonse ndi chitonthozo chimene ife tilandira kwa Mulungu.
Ungulubhi atizinzya ate humalabha getu, aje nate tibhazinyaje bhabhali mumalabhatibhazinzyaje nabhanja huluzinzyo lwatizinzizye ate Ungulubhi.
5 Pakuti monga momwe tili mʼmasautso pamodzi ndi Khristu, momwemonso Khristu amatitonthoza kwambiri.
Neshi amalabhi ga Kristu shagahwonjelela husababu yetu nu luzinzyo luhwonjelela hulite ashilile hwa Yesu Kristu.
6 Ngati ife tikusautsidwa, nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe ndi kupulumutsidwa. Ngati ife tikutonthozedwa nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe, ndi chitonthozo chimene chimabweretsa mwa inu kupirira kosawiringula pa zosautsa zomwe timasauka nazo ife.
Lelo nkatitamansiwa, titamansiwa hunongwa ye luzinzyo lwenyu nu wokovu wenyu, nkashele tuzinziwa, tizinziwa, tizinziwa hunongwa yeluzinzyo lwenyu uluzinzyo lwenyu lubhomba embombo pamuhweteshela amalabha galabaga uYesu namuvulila neshi patuvumilila ate.
7 Ndipo chiyembekezo chathu pa inu nʼcholimba chifukwa tikudziwa kuti monga momwe mumamva zowawa pamodzi nafe, momwemonso mumatonthozedwa nafe pamodzi.
Nu ujasili wetu hulimwe ulishinza, tumenye aje namwahitishie amalabhi, muhweteshela nuluzinzyo.
8 Abale, sitikufuna kuti mukhale osadziwa za masautso amene tinakumana nawo mʼchigawo cha Asiya. Tinapanikizidwa koopsa kuposa muyeso woti nʼkutha kupirira, mwakuti sitinkadziwa kuti nʼkukhalabe ndi moyo.
Sagatuhwanza aje mubhe bhalema, bhaholo, gatalinago hu Asia. Tabhonelwe pakasetamenye huje taibhabhomi nantele.
9 Zoonadi, tinamva mʼmitima mwathu chilango cha imfa. Koma izi zimachitika kuti tisangodzidalira mwa ife tokha koma Mulungu yemwe amaukitsa akufa.
Twali nulongwe ulwafwe eli lyatibheshele huje tusahwisubhile tetee, aje tisubhilaje Ungulubhi yazyusya nabhafwe.
10 Mulungu watilanditsa ku zoopsa zotere za imfa, ndipo adzatilanditsanso. Ife tayika chiyembekezo chathu pa Iyeyo kuti adzapitiriza kutilanditsabe.
Atokoye nenfwa, abhatokole nantele, tibheshele uujasiri wetu aje abhatokole nantele.
11 Mutithandize potipempherera. Pamenepo ambiri adzathokoza mʼmalo mwathu, chifukwa cha chisomo chake poyankha mapemphero a anthu ambiri.
Abhabhombe eshi neshi amwe namutaavwa humputo zyenyu abhinji bhaayenza asalifye huniaba yetu hunongwa ye upendelelo lwe lusajilo humputo zyenyu.
12 Tsono chonyadira chathu nʼchakuti, chikumbumtima chathu chimatitsimikizira kuti timakhala bwino mʼdziko lapansi, makamaka pa ubale wathu ndi inu. Takhala moona mtima ndi oyera mtima. Sitinachite chomwechi mwa nzeru ya dziko lapansi koma monga mwa chisomo cha Mulungu.
Tihwisunvya eli, oushuha wiza amili yetu uwinza we mwoyo hwa Ngulubhi aje tajendeleye pansi, namwe siyo ne hekima ya munsi. Tumefanya hivi hasa na ninyi, na sio katika hekima ya ulimwengu, lelo hu neema ya Ngulubhi.
13 Pakuti sitikukulemberani zoti simungawerenge kapena kumvetsetsa.
Setibhasimbila zyasigamuzibajiye abhazye awe ahwelewe. Endinoujasiri
14 Monga mwamva pangʼono chabe, ndikuyembekeza kuti mudzamvetsa kwenikweni, kuti mutha kutinyadira monga ife tidzakunyadirani, pa tsiku la Ambuye Yesu.
kwamba kwa sehemu mutelewe nantele endinuujasiri aji isiku elya Yesu Ugosi wetu, taibha sababu yenyu hunongwa ye mabado genyu, neshi shamwaibha hulite.
15 Popeza ndinatsimikiza mtima za ichi, nʼchifukwa chake ndinafuna kuti poyamba, ndidzakuchezereni kuti mupindule pawiri.
Nali noujasiri aje nahanzaga ahwenze hulimwe nasoti aje nkamwejelele efaida eyahwenze awe hulimwe ulwabhili.
16 Ndinafuna kuti ndidzakuchezereni pa ulendo wanga wopita ku Makedoniya ndi kudzakuonaninso pochokera ku Makedoniyako kuti inu mudzandithandize pa ulendo wanga wopita ku Yudeya.
Napanjile ahwenze nanabhalaga hu Makedonia, ata nanawelaga napanjile ahwinze, nante amwe antume ane nabhalaga hu Uyahudi.
17 Kodi pamene ndinkakonzekera zimenezi, mukuganiza kuti ndinkachita mwachibwana? Kapena kuti ndinkaganiza ngati mwa dziko lapansi; kuti ndikhoza kumanena kuti, “Inde, Inde,” nthawi yomweyo nʼkumatinso “Ayi, Ayi?”
Nanasibhaga eshi, je, nalunzanyaga humwoyo? Je napangashibi nadamu huje eje “Ena, ena” ndadi, ndadi huwakati umo?
18 Koma zoona monga Mulungu ali wokhulupirika, uthenga wathu kwa inu siwakuti, “Inde” nʼkutinso “Ayi.”
Lelo Ungulubhi shamwinza, setiyanga aja, “Ndadi” Awe “Ewa.”
19 Pakuti Yesu Khristu mwana wa Mulungu amene ine, Silivano ndi Timoteyo tinamulalikira pakati panu sali “Inde” yemweyonso “Ayi.” Koma nthawi zonse mwa Iye muli “Inde.”
Abhe umwana wa Ngulubhi uYesu Kristu, u Silwano, nu Timotheo nanee tabhatangazizizye huje hwamwene tiyiga “Ena” au “Ndadi” hwa mwene tiyiga “Ena.”
20 Pakuti ngakhale malonjezo a Mulungu atachuluka chotani, onsewo ndi “Inde” mwa Khristu. Kotero kuti mwa Iye, ife timati “Ameni” kuchitira Mulungu ulemu.
Maana ululagano lwa Ngulubhi huje “Ena” humambo gonti, hwa mwene zyonti huje “Ena” mwamwenye esho ashilile hwa mwene tiiga “Amina” hutuntumu wa Ngulubhi.
21 Tsono ndi Mulungu amene anachititsa kuti inu ndi ife tiyime molimba mwa Khristu. Anatidzoza ife,
Yu Ngulubhi yatihakikisyi ati namwe mwa Yesu aje atitumile.
22 nayikanso Mzimu wake mʼmitima mwathu kutitsimikizira za mʼtsogolo.
Abeshele eshimanyilo (omuhuru) hulite nantele atipiye no Mpepo wakwe mumoyo getu aje shibhe shilongolo shaitipela pamande.
23 Mulungu ndi mboni yanga kuti sindinabwererenso ku Korinto kuno kuti ndisakumvetseni chisoni.
Ehubhuzya Ungulubhi ambule zyasigana henzeye hu Koritho, aje ensabhabidushile amwe.
24 Sikuti ife tikufuna kukhala olamulira chikhulupiriro chanu, koma timagwira nanu ntchito pamodzi kuti mukhale achimwemwe, chifukwa ndinu okhazikika kwambiri mʼchikhulupiriro.
Eli siyo huje tibhonesya sa aluhwanziwa ulweteshelo lwetu aje shalubhe, tibhombha pandwemo namwe hunongwa.

< 2 Akorinto 1 >