< 2 Mbiri 1 >

1 Solomoni mwana wa Davide anakhazikika molimbika mu ufumu wake, pakuti Yehova Mulungu wake anali naye ndipo anamukweza kwambiri.
USolomoni indodana kaDavida waqina embusweni wakhe, ngoba uThixo uNkulunkulu wakhe wayelaye njalo wamenza waba mkhulu kakhulu.
2 Tsono Solomoni anayankhula kwa Aisraeli onse, olamulira a anthu 1,000, olamulira a anthu 100, oweruza ndiponso kwa atsogoleri onse a Israeli ndi atsogoleri amabanja.
Kwathi uSolomoni wakhuluma kubo bonke abako-Israyeli kusukela kubalawuli bezinkulungwane labalawuli bamakhulu, kusiya kubahluleli lakubo bonke abakhokheli bako-Israyeli, abazinhloko zezimuli
3 Solomoni pamodzi ndi gulu lonse la anthu anapita ku malo ofunika kwambiri pachipembedzo ku Gibiyoni. Tenti ya msonkhano ya Mulungu inali kumeneko, imene Mose mtumiki wa Yehova anayipanga mʼchipululu muja.
kwaze kwathi yena uSolomoni lebandla lonke baya endaweni ephakemeyo yokukhonzela eGibhiyoni, njengoba ithente lokuhlanganela likaNkulunkulu, elalenziwe nguMosi inceku kaThixo enkangala lalikuleyondawo.
4 Davide anabweretsa Bokosi la Mulungu kuchokera ku Kiriyati Yearimu, ndi kulikhazika kumalo kumene analikonzera popeza analimangira tenti mu Yerusalemu.
UDavida wayeselethe ibhokisi lesivumelwano sikaNkulunkulu lisuka eKhiriyathi-Jeyarimi elisa endaweni ayelilungisele yona, ngoba wayeselimisele ithente eJerusalema.
5 Koma guwa lansembe lamkuwa limene Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huri analipanga linali ku Gibiyoni kutsogolo kwa tenti ya Yehova. Kotero kuti Solomoni ndi gulu lonse anakapembedza kumeneko.
Kodwa i-alithari lethusi elalakhiwe nguBhezaleli indodana ka-Uri, indodana kaHuri, laliseGibhiyoni phambi kwethabanikeli likaThixo; ngakho uSolomoni lebandla lonke bahamba ukuyafuna intando yakhe khona.
6 Solomoni anapita pamene panali guwa lansembe lamkuwa pamaso pa Yehova mu tenti ya msonkhano ndipo anapereka nsembe zopsereza 1,000.
USolomoni wasesiya e-Alithareni lethusi phambi kukaThixo ethenteni lokuhlanganela wafika wanikela iminikelo yokutshiswa eyinkulungwane phezu kwalo.
7 Usiku umenewo Mulungu anaonekera kwa Solomoni ndipo anati kwa iye, “Pempha chilichonse chimene ukufuna ndipo ndidzakupatsa.”
Ngalobobusuku uNkulunkulu wabonakala kuSolomoni wathi kuye: “Cela loba kuyini okufunayo ukuze ngikunike khona.”
8 Solomoni anayankha Mulungu kuti, “Inu munaonetsa kukoma mtima kwakukulu kwa Davide abambo anga ndipo mwayika ine kukhala mfumu mʼmalo mwake.
USolomoni ephendula uNkulunkulu wathi: “Utshengisile umusa omkhulu kakhulu kubaba uDavida njalo mina usungibeke ngaba yinkosi esikhundleni sakhe.
9 Tsopano Inu Yehova Mulungu, lolani kuti lonjezo lanu kwa abambo anga Davide likwaniritsidwe, pakuti mwandiyika kukhala mfumu ya anthu anu amene ndi ochuluka ngati fumbi la pa dziko lapansi.
Khathesi, Thixo Nkulunkulu, gcwalisa isithembiso owasenza kubaba uDavida, ngoba ungenze inkosi phezu kwabantu abanengi okothuli lomhlabathi.
10 Mundipatse nzeru ndi luntha zolamulira anthu awa, pakuti ndani amene angathe kulamulira anthu anu ochulukawa?”
Nginika ukuhlakanipha lolwazi, ukuze ngikhokhele lababantu, ngoba ngubani ongabusa abantu bakho abanengi kangaka?”
11 Mulungu anati kwa Solomoni, “Popeza izi ndi zokhumba za mtima wako ndipo sunapemphe katundu, chuma kapena ulemu, kapena imfa ya adani ako, ndiponso poti sunapemphe moyo wautali koma nzeru ndi luntha kuti ulamulire anthu anga amene Ine ndakuyika kukhala mfumu yawo,
UNkulunkulu wathi kuSolomoni, “Njengoba lesi kuyisifiso somoya wakho njalo kawucelanga impahla lenotho lodumo, lokubhubha kwalabo abakuzondayo, lokuthi awucelanga impilo ende kodwa ucele inhlakanipho lolwazi ukuze ubuse phezu kwabantu bami engikwenze waba yinkosi yabo,
12 Ine ndidzakupatsa nzeru ndi chidziwitso. Ndipo ndidzakupatsanso katundu, chuma ndi ulemu, zinthu zoti palibe mfumu imene inali nazo iwe usanakhalepo ndipo palibe wina amene adzakhale nazo iweyo ukadzafa.”
ngenxa yalokho ngizakunika inhlakanipho lolwazi. Njalo ngizakunika impahla, lenotho lodumo, okungakaze kwenzakale emakhosini akwandulelayo njalo akuyikwenzakala lakumakhosi alandelayo.”
13 Kotero Solomoni anabwerera ku Yerusalemu kuchoka kumalo opembedzerako a ku Gibiyoni, ku tenti ya msonkhano ndipo analamulira Israeli.
Ngakho uSolomoni waya eJerusalema esuka endaweni yokukhonzela eGibhiyoni, evela phambi kwethente lokuhlanganela. Wabusa phezu kuka-Israyeli.
14 Solomoni anasonkhanitsa magaleta ndi akavalo; anali ndi magaleta 1,400 ndi akavalo 12,000, amene anawayika mʼmizinda yosungira magaleta ndipo ena anali ndi iye mu Yerusalemu.
USolomoni wabuthanisa izinqola zokulwa lamabhiza; wayelezinqola zokulwa ezingamakhulu alitshumi lane lamabhiza azinkulungwane ezilitshumi lambili, ayekugcina emizini yezinqola zezimpi okunye ekugcina yena eJerusalema.
15 Mfumu inasandutsa siliva ndi golide kukhala ngati miyala wamba mu Yerusalemu. Inasandutsanso mkungudza kukhala wochuluka ngati mitengo ya mkuyu ya ku zigwa.
Inkosi yandisa isiliva legolide eJerusalema kwangani ngamatshe, lezihlahla zomsedari zanda kwangani yizihlahla zomkhiwa wesikhamore emawatheni ezintaba.
16 Solomoni amagula akavalo ku Igupto ndi Kuwe pakuti anthu amalonda a mfumu amakawagula ku Kuwe.
Amabhiza kaSolomoni ayethengwe eGibhithe laseKhuwe, abathengi besikhosini babewathenga eKhuwe.
17 Anthu ankagula galeta ku Igupto pa mtengo wa masekeli asiliva 600 ndipo kavalo pa mtengo wa ndalama zasiliva 150. Iwo ankazigulitsanso kwa mafumu onse a Ahiti ndi a Aramu.
Bathenga inqola yempi eGibhithe ngamashekeli esiliva angamakhulu ayisithupha kanye lebhiza ngamashekeli alikhulu elilamatshumi amahlanu. Babuya bawedlulisa wonke bayawathengisela amakhosi amaHithi kanye lawama-Aramu.

< 2 Mbiri 1 >