< 2 Mbiri 32 >

1 Zitatha zonse zimene Hezekiya anachita mokhulupirika, Senakeribu mfumu ya ku Asiriya anabwera ndi kuthira nkhondo dziko la Yuda. Iye anazinga mizinda yotetezedwa ya Yuda, kuganiza kuti ayigonjetsa.
Hina bagade Hesigaia da Hina Godema molole fa: no bobogei. Be amogalu, Asilia hina bagade Sena: galibi da Yuda fi doagala: i. E da gagili sali moilai bai bagade huluane eale disili, ea dadi gagui dunu ilia gagili sali dobea muguluma: ne sia: i.
2 Pamene Hezekiya anaona kuti Senakeribu wabwera ndipo wakonzeka kuchita nkhondo ndi Yerusalemu,
Amola Sena: gelibi da Yelusaleme doagala: ma: ne ilegei. Hina bagade Hesigaia da amo hou dawa: loba,
3 iye anakambirana ndi akuluakulu ake pamodzi ndi atsogoleri a gulu lankhondo za kutseka akasupe ochoka ku kasupe amene anali kunja kwa mzinda, ndipo iwo anamuthandiza.
4 Gulu lalikulu la anthu linasonkhana, ndipo anatseka akasupe onse pamodzi ndi mtsinje umene umayenda mʼkati mwa nthakamo. Iwo ankanena kuti, “Nʼchifukwa chiyani mafumu a Asiriya akabwera kuno adzapeze madzi ambiri?”
e amola eagene ouligisu dunu da Asilia dunu ilia da Yelusaleme gadenene doaga: lalu, hano mae moma: ne logo hedofama: ne, hano logo Yelusaleme gadili galu, amo hedofamusa: dawa: i. Eagene ouligisu dunu da Yelusaleme fi dunu bagohame gadili oule asili, gu hano logo huluane hedofai.
5 Kenaka iye anagwira ntchito molimbika kukonza madera ogumuka a khoma ndi kumangapo msanja. Anamanganso mpanda wina kunja kwa mpanda winawo ndipo anamanga zolimbitsa Milo ku mzinda wa Davide.
Hina bagade da Yelusaleme bu gasawane gagili salima: ne, gagili sali dobea dodoa: i, amola amo da: iya diasu gado gagagula heda: su gaguli gagai. Amola e da gagoi gadili, eno dobea gagui. Amola e da gagili sali liligi amo da Yelusaleme musa: gagui gusudili dialu, be wali osobo gasa: le da: iya ligisi, amo dodoa: i. Amola e sia: beba: le, ilia da goge agei amola da: igene ga: su bagohame hamoi.
6 Iye anasankha atsogoleri a ankhondo olamulira anthu ndipo anawasonkhanitsa pamaso pake pa bwalo la chipata cha mzinda ndi kuwalimbikitsa ndi mawu awa:
E da dadi gagui ouligisu dunu, ilia Yelusaleme fi dunu huluane ouligima: ne ilegei, amola ilia huluane sogebi amo da Yelusaleme logo ga: su gadenene dialu, amogawi gilisima: ne sia: i.
7 “Khalani amphamvu ndi olimba mtima. Musachite mantha kapena kutaya mtima chifukwa cha mfumu ya ku Asiriya ndi gulu lalikulu lankhondo limene ali nalo, pakuti ife tili ndi mphamvu yayikulu kuposa imene ili ndi iye.
E da ilima amane sia: i, “Dilia gasa fili, amola Asilia hina bagade amola ea dadi gagui wa: i ilima mae beda: ma! Ninima gai gasa bagade hou da ema gai gasa hou, bagadewane baligisa.
8 Iye ali ndi mphamvu ya anthu basi, koma ife tili ndi Yehova Mulungu wathu kutithandiza ndi kuchita nkhondo zathu.” Ndipo anthu anapeza chilimbikitso kuchokera pa zimene Hezekiya mfumu ya Yuda ananena.
Ea gasa da osobo bagade dunu ea gasa fawane. Be ninia Hina Gode da ninima gai esala. Amola E da nini fidimu amola ninima gale gegemu.” Dunu huluane da ilia hina bagade ea sia: nababeba: le, dogo denesi.
9 Nthawi ina, pamene Senakeribu mfumu ya ku Asiriya ndi gulu lake lonse lankhondo anali atazinga Lakisi, iye anatumiza atsogoleri ake ankhondo ku Yerusalemu ndi uthenga uwu kwa Hezekiya mfumu ya Yuda ndi anthu onse a ku Yuda amene anali kumeneko:
Amalu, fa: no, Sena: gelibi amola ea dadi gagui wa: i da La: igisi moilai bai bagadega esaloba, e da Hesigaia amola Yuda fi dunu ili gilisili Yelusalemega esalu, ilima amane sia: si,
10 “Senakeribu mfumu ya ku Asiriya akuti: Kodi inu mukukhulupirira chiyani, kuti mukukhalabe mu Yerusalemu mutazingidwa?
“Na da Asilia hina bagade Sena: gelibi! Na da dilima adole ba: sa. Na da Yelusaleme eale disi dagoi. Dilia abuliba: le hame beda: sala: ?
11 Pamene Hezekiya akunena kuti ‘Yehova Mulungu wathu adzatipulumutsa kuchoka mʼdzanja la mfumu ya ku Asiriya,’ iye akukusocheretsani, kuti mufe ndi njala ndi ludzu.
Hesigaia da dilima, dilia Hina Gode da nini dilima mae hasalasima: ne, dili gaga: mu sia: sa. Be Hesigaia da dilima ogogosa. E da dili ha: ga amola hano hanaga bogoma: ne, logo doasisa.
12 Kodi si Hezekiya amene anachotsa malo opembedzerapo Mulungu ameneyu ndi maguwa ansembe ndi kunena kwa anthu a ku Yuda ndi Yerusalemu kuti, ‘Muzipembedza pa guwa lansembe limodzi ndi kupserezapo nsembe?’
Hesigaia hisu da Hina Godema nodone sia: ne gadosu sogebi amola oloda huluane gugunufinisili, Yuda fi dunu amola Yelusaleme fi dunu ilima oloda afae fawane amoga nodone sia: ne gadoma: ne amola gabusiga: manoma gobele salima: ne sia: i.
13 “Kodi inu simukudziwa zimene ine ndi makolo anga tachita kwa anthu a mitundu ina? Kodi milungu ya mitundu imeneyi inatha kupulumutsa dziko lawo kuchoka mʼdzanja langa?
Dilia na aowalali, ilia eno fifi asi ilima hamosu amo dawa: sala: ? Eno fifi asi gala dunu ilia ‘gode’ da Asilia hina bagade ili mae hasalima: ne, gaga: bela: ? Hame mabu!
14 Kodi ndi milungu iti mwa milungu ya mitundu ina ya anthuwo, imene makolo anga anayiwononga kotheratu, inatha kupulumutsa anthu ake mʼdzanja langa? Nanga tsono Mulungu wanuyo adzakupulumutsani mʼdzanja langa motani?
Amo fifi asi gala huluane ilia ‘gode’ da ninia ili mae hasalima: ne, hamedafa gaga: i. Amaiba: le, dilia abuliba: le dilia Gode da dili gaga: ma: ne dawa: sala: ?
15 Choncho inu musalole kuti Hezekiya akunamizeni ndi kukusocheretsani motere. Musamukhulupirire, pakuti palibe mulungu wa mtundu wina uliwonse kapena ufumu wina uliwonse umene unatha kupulumutsa anthu ake kuchoka mʼdzanja langa kapena mʼdzanja la makolo anga. Nanga bwanji Mulungu wanuyo, sadzatha kukupulumutsani kuchoka mʼdzanja langa!”
Hesigaia da dilima ogogosa. Ea sia: dafawaneyale mae dawa: ma. Fifi asi gala huluane ilia ‘gode’ da Asilia hina bagade ili mae hasalima: ne gaga: mu da hamedei ba: i. Amaiba: le, dilia Gode da dili gaga: mu hamedeidafa ba: mu.”
16 Atsogoleri a ankhondo a Senakeribu anapitiriza kuyankhula zotsutsana ndi Yehova Mulungu ndi mtumiki wake Hezekiya.
Asilia eagene ouligisu dunu ilia da baligili Hina Gode amola Hina Gode ea hawa: hamosu dunu Hesigaia elea hou lasogole sia: i.
17 Mfumunso inalemba makalata onyoza Yehova, Mulungu wa Israeli, ndipo inanena zotsutsana naye izi: “Monga momwe milungu ya anthu a mayiko ena sinathe kuwapulumutsa kuchoka mʼdzanja langa, chonchonso Mulungu wa Hezekiya sadzapulumutsa anthu ake kuchoka mʼdzanja langa.”
Amola meloa amo Asilia hina bagade ea dedei, amo ganodini Isala: ili Hina Godema odoga: su sia: bagade ba: i, “Fifi asi gala huluane ilia ‘gode’ da na gasaga ili hasalima: ne hame gaga: i. Amola Hesigaia ea Gode da dili na mae hasalima: ne, hamedafa gaga: mu.”
18 Kenaka iwo anafuwula mu Chihebri kwa anthu a mu Yerusalemu amene anali pa khoma, kuwaopseza ndi kuwachititsa mantha ndi cholinga choti alande mzindawo.
Sena: gelibi eagene ouligisu dunu da amo sia: Hibulu sia: ga wele sia: i. Bai ilia da Yelusaleme fi dunu dobea da: iya esalu, amo ili beda: ma: ne amola da: i dioma: ne hamomusa: dawa: i galu. Amalalu, ilia da hedolowane moilai sugumusa: dawa: i.
19 Iwo anayankhula za Mulungu wa Yerusalemu monga anayankhulira za milungu ya anthu ena a pa dziko lapansi, ntchito ya manja a anthu.
Ilia da Yelusaleme hadigi Godedafa, amo da fifi asi gala eno ilia udigili ogogosu ‘gode’, amo ili defele dawa: iwane sia: dasu.
20 Mfumu Hezekiya ndi mneneri Yesaya mwana wa Amozi anafuwulira kumwamba mʼpemphero chifukwa cha zimenezi.
Amalalu, hina bagade Hesigaia amola balofede dunu Aisaia (A: imose egefe), ela da Godema sia: ne gadoi amola Godea ili fidima: ne Ema digini wele sia: i.
21 Ndipo Yehova anatumiza mngelo amene anadzapha anthu onse odziwa nkhondo ndi atsogoleri ndiponso oyangʼanira misasa ya mfumu ya ku Asiriya. Choncho Senakeribu anabwerera kwawo wamanyazi. Ndipo atalowa mʼnyumba ya mulungu wake, ena mwa ana ake anamupha ndi lupanga.
Hina Gode da a: igele dunu asunasili, e da Asilia dadi gagui dunu amola ilia ouligisu dunu medole legei. Amaiba: le, Asilia hina bagade da gogosiane, Asilia sogega buhagi. Eso afaega, e da ea ogogosu ‘gode’ ea debolo diasua esaloba, egefelali mogili da gegesu gobiheiga, e medole legei.
22 Kotero Yehova anapulumutsa Hezekiya ndi anthu a ku Yerusalemu kuchoka mʼdzanja la Senakeribu mfumu ya ku Asiriya ndi mʼdzanja la anthu ena. Yehova anawateteza ku mbali zonse.
Hina Gode da agoane hina bagade Hesigaia amola Yelusaleme fi dunu huluane amo Asilia hina bagade Sena: gelibi amola Yuda fi ha lai dunu eno, ili mae hasalima: ne gaga: i dagoi.
23 Anthu ambiri anabweretsa zopereka kwa Yehova ku Yerusalemu ndi mphatso zamtengowapatali kwa Hezekiya mfumu ya Yuda. Kuyambira nthawi imeneyo Hezekiya ankalemekezedwa kwambiri ndi mitundu ina yonse.
Dunu bagohame da Yelusalemega, Hina Godema gobele salimusa: amola Hesigaiama hahawane dogolegele iasu liligi imunusa: misi. Ha amogainini, fifi asi gala dunu huluane da Hesigaiama nodone dawa: i.
24 Pa nthawi imeneyo Hezekiya anadwala ndipo anali pafupi kufa. Iye anapemphera kwa Yehova, amene anamuyankha ndi kumupatsa chizindikiro chodabwitsa.
Amo galu, hina bagade Hesigaia da olole, bogomuwane galu. E Godema sia: ne gadoiba: le, Hina Gode da e uhinisima: ne, ema dawa: digima: ne olelesu i.
25 Koma Hezekiya anali ndi mtima wonyada ndipo sanachite molingana ndi kukoma mtima kumene Mulungu anamuonetsera. Choncho mkwiyo wa Yehova unali pa iye ndi pa Yuda ndi Yerusalemu.
Be Hesigaia da gasa fili, Hina Gode Ea uhinisisu hou ba: beba: le, Godema hame nodoi. Amaiba: le, Yuda fi amola Yelusaleme fi da se nabi.
26 Koma kenaka Hezekiya analapa za kunyada kwakeko, monga anachitanso anthu a mu Yerusalemu. Choncho mkwiyo wa Yehova sunafike pa iwo pa nthawi ya Hezekiya.
Be fa: nowane, Hesigaia amola Yelusaleme fi da ilia hou fofonoboi. Amaiba: le, Hesigaia esalebe galu, ilima se hame i.
27 Hezekiya anali ndi chuma ndi ulemu wambiri ndipo anamanga nyumba zosungiramo chuma cha siliva wake ndi golide ndi za miyala yokongola, zokometsera zakudya, zishango ndi mtundu uliwonse wa zinthu zamtengowapatali.
Hina bagade Hesigaia da liligi bagade gaguiwane hamoi. Dunu huluane da ema nodosu. Ea sia: beba: le, ilia da liligi ligisisu sesei gaguia gagai. Amo ganodini, ilia da ea gouli, silifa, igi noga: idafa, ha: i manu fodole nasu, da: igene ga: su amola eno noga: idafa liligi, ligisisu.
28 Iye anamanganso nyumba zosungiramo tirigu, vinyo watsopano ndi mafuta a olivi, ndiponso anamanga nyumba zodyeramo ngʼombe zosiyanasiyana, ndi makola a nkhosa.
Amola ea sia: beba: le, ilia da liligi ligisisu diasu gaguia gagai. Amo ganodini, ilia da ea gala: ine, waini hano amola olife susuligi ligisisu. Amola ilia da ea bulamagau diasu gaguia gagai, amola sibi gagole gagai.
29 Iyeyo anamanga midzi ndipo anali ndi nkhosa ndi ngʼombe zambiri, pakuti Mulungu anamupatsa chuma chambiri.
Eno amolawane, Gode da ema bulamagau amola sibi amola liligi bagohamedafa iabeba: le, e da moilai bai bagade eno bagohame gaguia gagai.
30 Ndi Hezekiya amene anatseka ku mtunda kwa kasupe wa Gihoni, ndi kumuwongolera kuti madzi ake apite mbali ya kumadzulo kwa Mzinda wa Davide. Iye ankachita bwino pa ntchito iliyonse imene ankagwira.
Hina bagade Hesigaia da Gihone Gu hano hihiga: le, ea hano logo eno hamegadili ogane, osobo hagududili, Yelusaleme gagoi ganodini doafasi. Hesigaia da ea hamosu defele huluane didili hamoi.
31 Koma pamene nthumwi zotumizidwa ndi atsogoleri a ku Babuloni zinabwera kudzamufunsa za chizindikiro chozizwitsa chimene chinachitika mʼdzikomo, Mulungu anamusiya yekha, kumuyesa kuti adziwe zonse zimene zinali mu mtima mwake.
Amola Ba: bilone alofele iasu dunu da musa: hame ba: su hou amo abedela manoba, (2 Hina 20:7-19), Gode da Hesigaia hi hanaiga hamoma: ne yolesi. Bai E da ea hou adoba: musa: dawa: i.
32 Zina ndi zina zokhudza ulamuliro wa Hezekiya ndi ntchito za kudzipereka kwake zalembedwa mʼmasomphenya a Yesaya mwana wa Amozi, mʼbuku la mafumu a Yuda ndi Israeli.
Hesigaia ea hamonanu eno, amola ea Hina Godema asigidafa hou, amo huluane da “Balofede Dunu Aisaia (A: imose egefe) ea Esala Ba: su Meloa” amola “Yuda amola Isala: ili hina bagade Ilia Hamonanu Meloa” amo ganodini dedene legei.
33 Hezekiya anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pa phiri pamene pali manda a zidzukulu za Davide. Ayuda onse ndi anthu a mu Yerusalemu anamulemekeza atamwalira. Ndipo Manase mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
Hesigaia da bogole amola ilia ea da: i hodo gadodili sogebiga, hina bagade ilia gele gelabo ganodini sali. Yuda fi amola Yelusaleme fi dunu huluane da ema asigiba: le, ema nodomusa: gegedole fi. Egefe Ma: na: se da e bagia hina bagade hamoi.

< 2 Mbiri 32 >