< 2 Mbiri 27 >

1 Yotamu anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16. Dzina la amayi ake linali Yerusa mwana wa Zadoki.
Yotam yirmi beş yaşında kral oldu ve Yeruşalim'de on altı yıl krallık yaptı. Annesi Sadok'un kızı Yeruşa'ydı.
2 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga anachitira Uziya abambo ake, kupatula kuti iyeyo sanalowe mʼNyumba ya Yehova. Komabe anthu anapitirira kuchita zoyipa.
Babası Uzziya gibi, Yotam da RAB'bin gözünde doğru olanı yaptı. Ancak RAB'bin Tapınağı'na girmedi. Ne var ki, halk kötülük yapmayı sürdürmekteydi.
3 Yotamu anamanganso chipata chakumtunda cha Nyumba ya Yehova ndipo anagwira ntchito yayikulu yomanga khoma la ku phiri la Ofeli.
Yotam RAB'bin Tapınağı'nın Yukarı Kapısı'nı onardı. Ofel Tepesi'ndeki surun üzerinde de birçok iş yaptı.
4 Iye anamanga mizinda mʼmapiri a ku Yuda ndipo anamanganso malinga ndi nsanja mʼmadera a ku nkhalango.
Yahuda'nın dağlık bölgesinde kentler, ormanlık tepelerinde kaleler ve kuleler kurdu.
5 Yotamu anachita nkhondo ndi mfumu ya Aamoni ndipo anawagonjetsa. Chaka chimenecho Aamoni anapereka makilogalamu 3,400, matani 1,000 a tirigu ndiponso matani 1,000 a barele. Aamoni anabweretsa zinthu zomwezi chaka chachiwiri ndi chachitatu.
Ammon Kralı'yla savaşarak Ammonlular'ı yendi. Ammonlular o yıl için kendisine yüz talant gümüş, on bin kor buğday, on bin kor arpa verdiler. İkinci ve üçüncü yıllar için de aynı miktarı ödediler.
6 Yotamu anakula mphamvu chifukwa anayenda molungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.
Tanrısı RAB'bin önünde kararlı bir şekilde yürüyen Yotam giderek güçlendi.
7 Zina ndi zina zokhudza ulamuliro wa Yotamu, kuphatikizapo nkhondo zake zonse ndi zinthu zina zimene anachita, zinalembedwa mʼbuku la mafumu a Israeli ndi Yuda.
Yotam'ın yaptığı öbür işler, bütün savaşları ve uygulamaları, İsrail ve Yahuda krallarının tarihinde yazılıdır.
8 Iye anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16.
Yotam yirmi beş yaşında kral oldu ve Yeruşalim'de on altı yıl krallık yaptı.
9 Yotamu anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda mu Mzinda wa Davide. Ndipo Ahazi mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
Yotam ölüp atalarına kavuşunca, onu Davut Kenti'nde gömdüler. Yerine oğlu Ahaz kral oldu.

< 2 Mbiri 27 >