< 2 Mbiri 27 >

1 Yotamu anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16. Dzina la amayi ake linali Yerusa mwana wa Zadoki.
Jotham te kum kul kum nga a lo ca vaengah manghai tih Jerusalem ah kum hlai rhuk manghai. A manu ming tah Zadok canu Jerusha ni.
2 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga anachitira Uziya abambo ake, kupatula kuti iyeyo sanalowe mʼNyumba ya Yehova. Komabe anthu anapitirira kuchita zoyipa.
A napa Uzziah kah a saii bang boeih la BOEIPA mikhmuh ah a thuem saii cakhaw BOEIPA bawkim la a kun pawt dongah pilnam koep poci.
3 Yotamu anamanganso chipata chakumtunda cha Nyumba ya Yehova ndipo anagwira ntchito yayikulu yomanga khoma la ku phiri la Ofeli.
Anih loh a so BOEIPA im kah vongka te a thoh tih Ophel vongtung dongah a cungkuem la a sak.
4 Iye anamanga mizinda mʼmapiri a ku Yuda ndipo anamanganso malinga ndi nsanja mʼmadera a ku nkhalango.
Judah tlang ah khopuei a suen tih thingkho ah rhalmah im neh rhaltoengim a sak.
5 Yotamu anachita nkhondo ndi mfumu ya Aamoni ndipo anawagonjetsa. Chaka chimenecho Aamoni anapereka makilogalamu 3,400, matani 1,000 a tirigu ndiponso matani 1,000 a barele. Aamoni anabweretsa zinthu zomwezi chaka chachiwiri ndi chachitatu.
Anih loh Ammon koca kah manghai te a vathoh thil tih amih te a buem. Te dongah anih te Ammon koca loh kum khat ah cak talent yakhat, cang kore thawng rha, cangtun thawng rha a paek. Te tlam te Ammon ca rhoek loh anih te kum bae ah khaw, a kum thum dongah khaw a sah uh.
6 Yotamu anakula mphamvu chifukwa anayenda molungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.
A Pathen BOEIPA mikhmuh ah a longpuei a cikngae sak dongah Jotham khaw a thaa caang.
7 Zina ndi zina zokhudza ulamuliro wa Yotamu, kuphatikizapo nkhondo zake zonse ndi zinthu zina zimene anachita, zinalembedwa mʼbuku la mafumu a Israeli ndi Yuda.
Te dongah kah ol noi khaw, a caemtloek boeih neh a longpuei khaw, Israel neh Judah manghai rhoek kah cabu dongah a daek uh coeng ke.
8 Iye anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16.
A manghai vaengah kum kul neh kum nga lo ca tih Jerusalem ah kum hlai rhuk manghai.
9 Yotamu anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda mu Mzinda wa Davide. Ndipo Ahazi mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
Te dongah te a napa rhoek taengla a khoem uh vaengah anih te David khopuei ah a up uh. Te phoeiah a capa Ahaz te anih yueng la manghai.

< 2 Mbiri 27 >