< 2 Mbiri 2 >

1 Solomoni anatsimikiza zoti amange Nyumba ya Dzina la Yehova ndi nyumba yake yaufumu.
Hahoi Solomon ni BAWIPA min hanelah Bawkim buet touh hoi ama siangpahrang hanelah buet touh sak hanelah a kâcai.
2 Iye analemba ntchito anthu 70,000 onyamula katundu ndi anthu 80,000 okumba miyala ku mapiri ndiponso akapitawo 3,600 oyangʼanira anthuwo.
Solomon ni hno ka phawt hane tami 70, 000 touh, thing ka bouk hane 80, 000 touh hoi ka taroun hanelah tami 3, 600 touh a rawi.
3 Solomoni anatumiza uthenga uwu kwa Hiramu mfumu ya ku Turo: “Munditumizire mitengo ya mkungudza monga munachitira ndi abambo anga pamene munawatumizira mitengo ya mkungudza yomangira nyumba yaufumu yokhalamo.
Solomon ni Taire siangpahrang Huram koevah, apa Devit hanelah hno na sak pouh teh, ao nahane im sak pouh hanelah sidar thing na poe e patetlah na poe van haw.
4 Tsono ine ndikufuna kumanga Nyumba ya Yehova Mulungu wanga ndi kuyipereka kwa Iye kuti tiziyikamo buledi wopatulika nthawi zonse ndiponso kuperekeramo nsembe zopsereza mmawa uliwonse ndi madzulo ndi pa masabata ndi pa masiku a chikondwerero cha mwezi watsopano ndiponso pa masiku osankhika a chikondwerero cha Yehova Mulungu wathu, monga mwa malamulo a Aisraeli mpaka muyaya.
Khenhaw! BAWIPA Cathut hanelah Bawkim buet touh sak hane ka kâcai. Hmuitui sawi vaiteh BAWIPA bawk nahane hmuen, Isarelnaw ni pou sak hane kâpoelawk, vaiyei ta nahane thuengnae, sabbath hoi, thapa rei nah hnin, BAWIPA Cathut min lahoi pawi hnin amom tangmin hmaisawi thuengnae pou sak hane, naw doeh. Hathateh Isarelnaw hanelah yungyoe e phunglam doeh.
5 “Nyumba ya Mulungu imene ndidzamange idzakhala yayikulu, chifukwa Mulungu wathu ndi wamkulu kuposa milungu ina yonse.
Ka sak hane Bawkim teh kalenpounge lah ao han. Bangkongtetpawiteh, Cathut teh cathutnaw pueng hlak a lenpoung dawk.
6 Koma ndani angathe kumumangira Iye Nyumba, pakuti mlengalenga, ngakhale kumwamba kwenikweni sikungamukwane? Tsono ine ndine yani kuti ndimangire Iyeyo Nyumba, kupatula malo chabe opserezerapo nsembe pamaso pake?
Kakaw pounge kalvan patenghai khout hoeh e Cathut teh apinimaw Bawkim a sak pouh thai han. Kai patetnaw ni hmuitui sawi nahane im hoeh laipateh, bangtelamaw im ka sak pouh thai han vaw.
7 “Tsono tumizireni munthu waluso pa ntchito zagolide ndi siliva, mkuwa ndi chitsulo, nsalu yapepo ndi yofiira ndi yobiriwira ndiponso waluso losema, kuti adzagwire ntchito mu Yuda ndi Yerusalemu pamodzi ndi anthu aluso amene abambo anga Davide anandipatsa.
Hatdawkvah, apa Devit ni a hmoun tangcoung e, Judah ram thung e hoi Jerusalem kho dawk e sui, ngun, rahum, sum, hahoi opaou, âthi, kamthim hni, hete hnonaw dawk thoumthainae hoi, kakuep e tami buet touh kai koe kaawm e hoi kâ kabawm hanelah patoun haw loe.
8 “Munditumizirenso mitengo ya mkungudza, payini ndiponso matabwa a mʼbawa wa ku Lebanoni, pakuti ndikudziwa kuti anthu anu ali ndi luso locheka matabwa kumeneko. Antchito anga adzagwira ntchito pamodzi ndi antchito anu
Lebanon e sidar thing hmaica thing hoi Algum thingnaw na patawn haw. Bangkongtetpawiteh, na taminaw teh lebanon thing tâtueng a thoum poung tie ka panue.
9 kuti andipatse matabwa ambiri, chifukwa Nyumba imene ndikumanga iyenera kukhala yayikulu ndi yokongola.
Thing moikapap rakueng hanelah ka sannaw teh nange na sannaw koe kambawk van naseh. Bangkongtetpawiteh, sak han ka noe e Bawkim teh kalen pounge hoi kângairu hane kawilah ao.
10 Ine ndidzalipira antchito anu amene adzacheke matabwa matani 1,000 a tirigu wopunthapuntha, matani 2,000 a barele, malita 440,000 a vinyo, ndiponso malita 440,000 a mafuta a olivi.”
Thing ka bouk e na sannaw hanelah, satun kor 20, 000, misur bath 20, 000 hoi satui bath 20, 00 ka poe a han telah lawk na thui.
11 Hiramu, mfumu ya ku Turo, anamuyankha Solomoni pomulembera kalata kuti, “Chifukwa Yehova amakonda anthu ake, wayika iwe kukhala mfumu yawo.”
Taire siangpahrang Huram ni, BAWIPA ni a taminaw lungpataw dawkvah ahnimae siangpahrang lah na coung sak e doeh telah Solomon koe ca lahoi bout a patawn.
12 Ndipo Hiramu anawonjezera kunena kuti, “Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli, amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi! Iye wamupatsa Davide mwana wanzeru, wodzaza ndi luntha ndi wozindikira, amene adzamanga Nyumba ya Mulungu ndi kudzimangira yekha nyumba yaufumu.
Huram ni, Isarelnaw e BAWIPA Cathut, talai hoi kalvan kasakkung BAWIPA hanelah Bawkim hoi siangpahrang im sak hanelah lungangnae hoi panuethainae a capa siangpahrang Devit koe kapoekung teh yawhawinae awmseh.
13 “Ine ndikukutumizira Hiramu Abi, munthu wa luso lalikulu,
Hatdawkvah thoumthainae hoi ka kuep e Huram heh ka patoun.
14 amene amayi ake anali wochokera ku Dani ndipo abambo ake anali a ku Turo. Iye anaphunzitsidwa kugwira ntchito zagolide ndi siliva, mkuwa ndi chitsulo, miyala yokongola ndi matabwa, ndiponso nsalu zofewa zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Alinso ndi luso la zosemasema ndipo atha kupanga chilichonse chimene wapatsidwa. Iye adzagwira ntchito ndi amisiri anu ndi a mbuye wanga, Davide abambo anu.
A manu teh dan miphun, A na pa teh Taire miphun lah ao. Huram teh sui, ngun, rahum, sum, talung hoi thing hetnaw hoi aphunphun ka sak thai e tami lah ao. Âthi hni, opaou hni kamthim hni hoi lukkarei naw hai koung a kawng thai, Hatdawkvah BAWIPA na pa Devit e thaw katawknaw hoi cungtalah rei tawk naseh.
15 “Tsono mbuye wanga tumizirani antchito anu tirigu ndi barele, mafuta a olivi ndi vinyo zimene mwalonjeza,
Ka BAWIPA ni a dei tangcoung e patetlah satun, barli, satui hoi misur naw hah ka sannaw koe patawn awh lawih.
16 ndipo ife tidzadula mitengo yonse imene mukuyifuna kuchokera ku Lebanoni ndipo tidzayimanga pamodzi ndi kuyiyadamitsa pa madzi mpaka ku Yopa. Ndipo inu mudzatha kuyitenga mpaka ku Yerusalemu.”
Hottelah, kaimouh ni Lebanon mon dawk e thingnaw, na ngai yit touh ka tâtueng vaiteh tui dawk hoi Joppa totouh na phu han telah atipouh.
17 Solomoni anawerenga alendo onse amene anali mu Israeli, potsatira chiwerengero chimene abambo ake Davide anachita ndipo panapezeka kuti analipo anthu 153,600.
Solomon ni Isarel ram dawk e a na pa Devit ni a touk tangcoung e miphun alouke tami bout a touk navah 153, 600 touh a pha.
18 Iye anayika anthu 70,000 kuti akhale onyamula katundu ndi anthu 80,000 kuti akhale ophwanya miyala mʼmapiri, anthu 3,600 anawayika kukhala akapitawo oyangʼanira anthu pa ntchitoyo.
Hahoi hno ka phawt hanelah tami 70, 000 hoi, mon dawk e thing ka tâtueng hane 80, 000, hoi thaw katawknaw khenyawnkung lah, 3,600 touh, touh lah a hmoun.

< 2 Mbiri 2 >