< 2 Mbiri 14 >
1 Tsono Abiya anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda mu mzinda wa Davide. Asa mwana wake anakhala mfumu mʼmalo mwake ndipo pa masiku ake, dziko linakhala pa mtendere kwa zaka khumi.
Abijah teh mintoenaw koe a i teh Devit khopui dawk a pakawp awh. Hahoi a yueng lah a capa Asa ni a uk. Ahnie tueng navah kum 10 touh roumnae ao.
2 Asa anachita zabwino ndi zolungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.
Asa ni BAWIPA Cathut hmalah hawinae hoi lannae hno a sak.
3 Iye anachotsa maguwa achilendo ndi malo opembedzerapo mafano, anaphwanya zipilala za miyala yachipembedzo ndi kugwetsa mafano a Asera.
Jentelnaw e thuengnae khoungroenaw hoi hmuenrasangnaw koung a takhoe. Talung ungenaw hai koung a raphei teh meikaphawk thingnaw hai koung a tâtueng.
4 Asa analamula Yuda kuti afunefune Yehova Mulungu wa makolo awo ndi kumvera malamulo ndi zolamulira zake.
Judahnaw ni mintoenaw e BAWIPA Cathut tawng vaiteh, kâlawknaw tarawi hanelah kâ a poe.
5 Iye anachotsa malo opembedzera mafano ndi maguwa ofukizira lubani mu mzinda uliwonse wa mu Yuda, ndipo mu ufumu wake munali mtendere pa nthawi ya ulamuliro wake.
Judah kho tangkuem dawk e hmuenrasangnaw hoi meikaphawk a takhoe awh teh, a uknaeram teh karoumcalah ao.
6 Asa anamanga mizinda yonse yotetezedwa ya Yuda pakuti dziko linali pa mtendere. Panalibe amene anachita naye nkhondo mʼzaka zimenezo, pakuti Yehova anamupatsa mpumulo.
Judah ram dawk e khopuinaw rapan hoi koung a kalup teh BAWIPA ni roumnae a poe dawkvah, kum moikasawlah kâtuknae awm hoeh.
7 Iye anati kwa Yuda “Tiyeni timange mizinda iyi ndipo timange makoma ndi nsanja, zitseko ndi zotchinga. Dzikoli likanali lathu chifukwa tafuna Yehova Mulungu wathu; tinamufuna Iye ndipo watipatsa mpumulo mbali zonse.” Kotero iwo anamanga ndi kukhala pa ulemerero.
Hahoi Judahnaw koevah, hete khopuinaw sak awh vaiteh, rapan hoi koung kalup awh sei. Radoung nahane imrasang hoi longkha taren nahane hai sak awh seh. BAWIPA Cathut e a ngainae tawng dawkvah, maimae ram teh kahawicalah uk thai awh. Hatdawkvah ahni ni kho tangkuem roumnae na poe awh telah atipouh. Hahoi a dei e patetlah a sak teh hoehoe a roung awh.
8 Asa anali ndi ankhondo 300,000 ochokera ku Yuda, okhala ndi zishango zikuluzikulu ndi mikondo, ndiponso ankhondo 280,000 ochokera ku Benjamini, okhala ndi zishango ndi mauta. Onsewa anali ankhondo amphamvu ndi olimba mtima.
Asa ni Judahnaw bahlingnaw hoi tahroenaw ka patuem e tami 300,000 touh a tawn. Benjamin miphun dawk bahlingnaw hoi lilava ka patuem e tami 280,000 touh a tawn teh, hete taminaw pueng teh thakasaipounge naw hoi tarankahawi poung e naw doeh.
9 Zera wa ku Kusi anapita kukamenyana nawo ali ndi gulu lalikulu kwambiri la asilikali ndi magaleta 300 ndipo anafika mpaka ku Maresa.
Ethiopia tami Zerah teh ransa 1,000,000, rangleng 300 touh hoi ahnimanaw tuk hanelah Mareshah kho dawk a pha.
10 Asa anapita kukakumana naye ndipo anakhala pa mizere yawo ya nkhondo mʼchigwa cha Zefata pafupi ndi Maresa.
Asa ni ahnimanaw tuk hanelah a tâco teh, Mareshah kho teng e Zephathah yawn dawk taran a kâtuk awh.
11 Kenaka Asa anafuwulira Yehova Mulungu wake ndipo anati “Yehova palibe wina wofanana nanu kuti angathandize anthu opanda mphamvu pakati pa amphamvu. Tithandizeni Inu Yehova Mulungu wathu pakuti ife timadalira Inu ndipo mʼdzina lanu ife tabwera kudzalimbana ndi gulu la ankhondo lalikulu kwambiri ngati ili. Inu Yehova ndinu Mulungu wathu, musalole kuti munthu akupambaneni.”
Asa ni BAWIPA Cathut a kaw teh Oe BAWIPA nang teh athakaawme hoi athakayounnaw rungngang hanelah na coung thai dawkvah, Oe BAWIPA Cathut na rungngang awh haw. Kaimanaw ni nang na kâuep awh teh, na min lahoi hete tamihupui tuk hanelah ka cei awh. Oe BAWIPA nang teh kaimae Cathut lah na o teh taminaw ni na ta hanh seh telah a ratoum.
12 Yehova anakantha Akusi pamaso pa Asa ndi Ayuda. Akusi anathawa,
Hottelah BAWIPA ni Asa hoi Judahnaw hmalah, Ethiopia taminaw a tuk teh koung a yawng awh.
13 ndipo Asa ndi ankhondo ake anawathamangitsa mpaka ku Gerari. Gulu lonse lalikulu lija la Akusi linaphedwa. Sanapezeke mmodzi wamoyo pakati pawo. Iwo anakanthidwa pamaso pa Yehova ndi asilikali ake. Anthu a ku Yuda anatenga katundu wambiri olanda ku nkhondo.
Asa hoi a taminaw ni Gerar kho totouh a pâlei awh. Ethiopianaw ni bout a tuk thai hoeh dawkvah, a kâhno awh toe. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA hoi a ransanaw hmalah sung sak lah ao teh, hnopai moikapap a la pouh awh.
14 Iwo anawononga midzi yonse yozungulira Gerari pakuti mantha aakulu wochokera kwa Yehova anagwera anthuwo. Analanda katundu wa midzi yonse, popeza kunali katundu wambiri kumeneko.
Gera kho teng e naw pueng koung a tâ awh. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA takinae ahnimae thung a pha teh, khopuinaw hai koung a raphoe awh. Hnopai moikapap a la awh.
15 Anakathiranso nkhondo misasa ya anthu oweta ziweto ndipo anatenga nkhosa zambiri, mbuzi ndi ngamira. Atatero anabwerera ku Yerusalemu.
Saring hrueknae imnaw hai koung a raphoe awh teh, tu hoi kalauknaw moikapap a lawp awh teh Jerusalem lah a ban awh.