< 2 Mbiri 11 >

1 Rehobowamu atafika ku Yerusalemu anasonkhanitsa asilikali 180,000 a fuko la Yuda ndi Benjamini kuti akachite nkhondo ndi Israeli, kuti abwezeretse ufumu kwa Rehobowamu.
Då Rehabeam kom till Jerusalem, församlade han Juda hus och BenJamin, hundradetusend, och åttatiotusend unga män, som stridsamme voro, till att strida emot Israel, att de måtte komma åter riket under Rehabeam.
2 Koma Yehova anayankhula ndi munthu wa Mulungu Semaya kuti,
Men Herrans ord kom till Semaja, den Guds mannen, och sade:
3 “Kawuze Rehobowamu mwana wa Solomoni mfumu ya Yuda ndi Aisraeli onse ali mu Yuda ndi Benjamini kuti,
Tala till Rehabeam, Salomos son, Juda Konung, och till hela Israel, som under Juda och BenJamin är, och säg:
4 ‘Yehova akuti: Musapite kukamenyana ndi abale anu. Pitani kwanu, aliyense wa inu, pakuti izi ndikuchita ndine.’” Choncho anamvera mawu a Yehova ndi kubwerera osapita kukamenyana ndi Yeroboamu.
Detta säger Herren: I skolen icke draga upp, ej heller strida emot edra bröder; hvar och en gånge åter hem, förty det är skedt af mig. De lydde Herrans ord, och vände igen att draga emot Jerobeam.
5 Rehobowamu amakhala mu Yerusalemu ndipo anamanga mizinda ya chitetezo iyi mu Yuda:
Men Rehabeam bodde i Jerusalem, och byggde de städer fasta i Juda;
6 Betelehemu, Etamu, Tekowa,
Nämliga BethLehem, Etham, Thekoa,
7 Beti Zuri, Soko, Adulamu,
Bethzur, Socho, Adullam,
8 Gati, Maresa, Zifi,
Gath, Maresa, Siph,
9 Adoraimu, Lakisi, Azeka,
Adoraim, Lachis, Aseka,
10 Zora, Ayaloni ndi Hebroni. Iyi ndiye inali mizinda yotetezedwa ya Yuda ndi Benjamini.
Zorga, Ajalon och Hebron; hvilke voro de fastaste städer i Juda och BenJamin.
11 Iye anakhwimitsa chitetezo cha mizindayi ndipo anayikamo atsogoleri a ankhondo, pamodzi ndi chakudya, mafuta a olivi ndi vinyo.
Och han gjorde dem fasta, och satte der öfverstar in, och besörjde dem med spisning, oljo och vin.
12 Mʼmizinda yonse anayikamo zishango zikuluzikulu ndi mikondo, ndipo anachititsa kuti mizindayo ikhale yamphamvu. Choncho iye amalamulira Yuda ndi Benjamini.
Och i alla städer skaffade han sköldar och spjut, och gjorde dem ganska fasta. Och Juda och BenJamin voro under honom.
13 Ansembe ndi Alevi a mʼmadera onse a Israeli anakhala mbali ya Rehobowamu.
Och gåfvo sig till honom Presterna och Leviterna utaf hela Israel, och alla deras gränsor.
14 Alevi anasiya malo awo owetera ziweto ndi katundu wawo, ndi kubwera ku Yuda ndi ku Yerusalemu chifukwa Yeroboamu ndi ana ake anawakana kukhala ansembe a Yehova.
Och de öfvergåfvo alla deras förstäder och håfvor, och kommo till Juda i Jerusalem; förty Jerobeam och hans söner fördrefvo dem, att de icke kunde bruka Herranom Presterskapet.
15 Ndipo iye anasankha ansembe akeake a pa malo opatulika ndi a mafano a mbuzi ndi mwana wangʼombe amene anapanga.
Men han stiktade sig Prester till höjderna, och till djeflar, och kalfvar, som han göra lät.
16 Anthu ochokera fuko lililonse la Israeli amene anatsimikiza mitima yawo kufunafuna Yehova Mulungu wa Israeli, ankapitabe ku Yerusalemu kukapereka nsembe kwa Yehova, Mulungu wa makolo awo.
Och efter dem kommo, utaf all Israels slägter, de som sitt hjerta gåfvo till att fråga efter Herran Israels Gud, till Jerusalem, att de måtte offra Herranom sina fäders Gud;
17 Iwo analimbikitsa ufumu wa Yuda, ndipo anathandiza Rehobowamu mwana wa Solomoni kwa zaka zitatu. Pa nthawi imeneyi iye amatsatira zochita za Davide ndi Solomoni.
Och förstärkte alltså Juda rike, och styrkte Rehabeam, Salomos son, i tre år; ty de vandrade på Davids och Salomos väg i tre år.
18 Rehobowamu anakwatira Mahalati, amene abambo ake anali Yerimoti, mwana wa Davide, ndipo amayi ake anali Abihaili, mwana wa Eliabu, mwana wa Yese.
Och Rehabeam tog Mahalath, Jerimoths dotter, Davids sons, till hustru, och Abihail, Eliabs dotter, Isai sons.
19 Mkaziyo anamubereka ana aamuna awa: Yeusi, Semariya ndi Zahamu.
Hon födde honom dessa söner: Jehus, Semaria och Saham.
20 Kenaka anakwatira Maaka, mwana wamkazi wa Abisalomu, amene anamubereka Abiya, Atai, Ziza ndi Selomiti.
Derefter tog han Maacha, Absaloms dotter. Hon födde honom Abia, Attai, Sisa och Selomith.
21 Rehobowamu ankamukonda Maaka mwana wa Abisalomu kuposa aliyense mwa akazi ake ndi azikazi. Iye anali ndi akazi 18, azikazi 60, ana aamuna 28 ndi ana aakazi 60.
Men Rehabeam hade Maacha, Absaloms dotter, kärare, än alla sina hustrur och frillor; ty han hade aderton hustrur, och sextio frillor, och födde åtta och tjugu söner, och sextio döttrar.
22 Rehobowamu anasankha Abiya mwana wa Maaka kuti akhale mtsogoleri pa abale ake, ndi cholinga choti adzakhale mfumu.
Och Rehabeam satte Abia, Maachas son, till ett hufvud och Första öfver hans bröder; ty han hade i sinnet göra honom till Konung.
23 Iye anachita mwanzeru, pomwaza ena mwa ana ake ku madera onse a Yuda ndi Benjamini, ndi ku mizinda yonse yotetezedwa. Iye anawapatsa zinthu zambiri ndiponso anawafunira akazi ambiri.
Och han växte till, och yppade sig för alla hans söner i Juda och BenJamins land, i alla fasta städer. Och han gaf dem spisning en stor hop; och han tog många hustrur.

< 2 Mbiri 11 >