< 1 Timoteyo 6 >

1 Onse amene ali mu ukapolo ayenera kuona ambuye awo ngati oyenera kuwachitira ulemu, kuti anthu anganyoze dzina la Mulungu ndi chiphunzitso chathu.
Bhala bhoha bhabhajhele pasi pa nira kama bhatumwa bhabhatolelayi mabwana bhabhi kama bhajhe ni litengo lyoha bhilondeka kubhomba naha ili lihina lya K'yara ni mafundisu ghasilighibhu.
2 Amene ambuye awo ndi okhulupirira, asawapeputse chifukwa ambuye ndi abale mʼchikhulupiriro. Mʼmalo mwake akuyenera kuwatumikira bwino chifukwa ambuye wawo ndi okondedwa monga okhulupirira ndiponso ndi odzipereka kusamalira akapolo awo. Zinthu izi ukuyenera kuziphunzitsa ndi kuwalamula anthu.
Bhatumwa bhabhajhele ni mabwana bhabhikiera bhasibhajimuli kwandabha bhene ndo bhalongobhe. Badala jhhiake bhabhatumiklayi nesu. Kwandabha mabwana bhabhitangatibhwa mahengu gha bhene ndo bhaamini na bhiganikibhwa. Manyisiajhi ni kughatangasya mambo agha.
3 Ngati wina aphunzitsa zosiyana ndi zimenezi, wosagwirizana ndi malangizo woona a Ambuye athu Yesu Khristu ndi chiphunzitso cholemekeza Mulungu,
Ikajhelayi munu fulani imanyisya kwa upotovu na ikaghapokelalepi majhelekesu ghitu gha ghiaminika, ambagho ndo malobhi gha Bwana bhitu Yesu Kristu, japo bhakalijhedekela lepi lifundisu lyalilongosibhwa mu utauwa.
4 ameneyo ndi wodzitukumula ndipo sakudziwa chilichonse. Iyeyo ali ndi maganizo oyipa, wokonda kusemphana mawu ndi kutsutsana. Zimenezi zimabweretsa nsanje, mikangano, mʼnyozo, kuganizirana zoyipa,
Munu ojhu ikwifuna na amanyili lepi kyokyoha. Badala jhiake, ajhe ni fuju ni mabishanu panani pa malobhi. Malobhi agha ghihogola bhuifu, ngondo, malighu, shuku jhibhibhi,
5 ndi kulimbana kosatha pakati pa anthu amitima yopotoka amene alandidwa choonadi ndipo amaganiza kuti kulemekeza Mulungu ndi njira yopezera chuma.
ni fuju sya mara kwa mara kati jha bhanu bhabhajhele ni luhala kwa liharibiki. Bhakajhileka bhukweli. Bhifikiri kujha utauwa ndo njela jha kujha matajiri”
6 Koma kulemekeza Mulungu kuli ndi phindu lalikulu.
Henu utauwa ni kuridhika ni faida mbaha.
7 Pakuti sitinabweretse kanthu mʼdziko lapansi, ndipo sitingatengenso kanthu pochoka mʼdziko lapansi.
Kwa ndabha twahidili lepi ni kyokyoha pa duniani. Wala twibhwesyalepi kutola kyokyoha kuhoma paduniani.
8 Koma ngati tili ndi chakudya ndi zovala, zimenezi zitikwanire.
Badala jhiake, tufukuajhi ni kyakulya ni maguanda.
9 Anthu amene amafuna kulemera amagwa mʼmayesero ndi mu msampha ndi mʼzilakolako zambiri zopusa ndi zoopsa zimene zimagwetsera anthu mʼchitayiko ndi mʼchiwonongeko.
Henu abhu bhabhibeta kujha ni mali bhibina mu majaribu, mu n'teghu ni tamaa sibhibhi, ni mu khenu kyokyoha kyakikabhabhomba bhanu bhajhibhilayi mu majhangamisi ni bhuharibifu.
10 Pakuti kukonda ndalama ndiye muzu wa zoyipa za mitundu yonse. Anthu ena ofunitsitsa ndalama, asochera ndipo asiya njira yachikhulupiriro ndipo adzitengera zowawitsa zambiri.
Kwa kujha kugana hela ndo chanzo kya aina syoha sya uovu. Bhanu ambabho bhinoghela ejhu bhapotosibhu, patali ni imani na bhakinyanyili bhene kwa huzuni jhimehele.
11 Koma iwe, munthu wa Mulungu, thawa zinthu zonsezi. Tsatira chilungamo, moyo wolemekeza Mulungu, chikhulupiriro, chikondi, kupirira ndi kufatsa.
Lakini bhebhe munu ghwa K'yara, ghajumbayi mambo aghu. Khesijhi haki, utauwa, bhuaminifu, luganu, bhusindamalifu ni bhololo.
12 Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
Komanayi vita finofu fya imani. Kamulilayi bhusima bhwa milele bhwa bhusopibhu. Jhajhele kwa ndabha ejhe kujha ghwahomisi bhushuhuda palongolo pa mashahidi bhamehele kwa khela kya kijhele kinofu. (aiōnios g166)
13 Ndikukulamula pamaso pa Mulungu amene amapatsa moyo zinthu zonse, ndiponso pamaso pa Khristu Yesu amene pochitira umboni pamaso pa Pontiyo Pilato, ananena zoona zenizeni.
Nikupela amri ejhe palongolo pa K'yara, jhaisababisya fenu fyoha kuishi, ni palongolo pa Yesu Kristu, jhaajobhili jhajhijhele jha bhukweli kwa Pontio Pilato:
14 Usunge lamuloli mopanda banga ndi cholakwa kufikira Ambuye athu Yesu Khristu ataonekera.
jhitunzayi amri kwa bhukamilifu, bila bhuogha, hadi kuhida kwa Bwana bhitu Yesu Kristu.
15 Pa nthawi yake Mulungu adzamubweretsa kwa ife. Mulungu ndi wodalitsika ndipo Iye yekha ndiye Wolamulira, Mfumu ya mafumu, Mbuye wa ambuye.
K'yara ibetakudhihirisha kuhida kwa muene kwa bhwakati bhwa wilondeka- K'yara, Mbarikibhwa, nghofu jhiene, Mfalme jha itabhwala, Bwana jhailongosya.
16 Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
Muene jhaitama milele na jhaitama mu muanga bhwa bhukaribilibhu lepi. Ajhe lepi munu jhaibhwesya kumbona bhwala jhaibhwesya kundanga. Kwa muene lijhelayi litengo ni uweza bhwa milele. Amina. (aiōnios g166)
17 Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
Bhajobhelayi matajiri mu ulimwengu obho bhasikifuni, na bhasitegemeli mu utajiri, anibho bhwa bhuhakikalepi. Badala jhiake, bhilondeka kuntumaini K'yara. Ambajhe akatupela, utajiri bhuoha bhwa ukweli ili tuhobhokelayi. (aiōn g165)
18 Uwalamule kuti azichita zabwino, kuti azikhala olemera pa ntchito zabwino, owolowamanja ndi okonda kugawana zinthu zawo ndi anzawo.
Bhajobhelayi bhabhombayi manofu, bhatajirikayi mu mbombo sinofu, bhajhelayi bhakarimu, ni utayari bhwa kuhomesya.
19 Potero adzadziwunjikira chuma chokhalitsa ngati maziko okhazikika a nthawi zakutsogolo, kuti akalandire moyo, umene ndi moyo weniweni.
Mu njela ejhu bhibetakwibhekela misingi minofu kwa mambo ghaghihida, ili kwamba bhabhwesiajhi kukamula maisha halisi.
20 Timoteyo, samalitsa zimene unapatsidwa. Upewe nkhani zopanda pake zosalemekeza Mulungu ndiponso maganizo otsutsana amene amaganizidwa molakwika kuti ndi nzeru.
Timotheo, l'endayi khela kyaupelibhu. Kijhepusiajhi ni majadilianu gha kipumbafu ni mabishanu ghenye kwip'enga ambagho kwa udesi ghikutibhwa maarifa.
21 Anthu ena chifukwa chovomereza nzeru zotere, asochera nʼkutaya chikhulupiriro chawo. Chisomo chikhale nawe.
Baadhi jha bhanu bhikaghatangasya mambo agha, ni naha bhadulili imani. Neema na ijhelayi pamonga nabhi.

< 1 Timoteyo 6 >