< 1 Atesalonika 4 >
1 Potsiriza, abale, tinakulangizani kale momwe mukuyenera kukhalira kuti mukondweretse Mulungu, monga momwe mukukhaliramo. Tsopano tikukupemphani ndi kukulimbikitsani mwa Ambuye Yesu kuti muchite zimenezi koposa kale.
Now, my fellow believers, [I want to write] about some other matters. Because we all have a close relationship with the Lord Jesus, we(exc) strongly urge you [DOU] to live in a way that pleases God. We taught you to do that, and you know that we lived that way as a result of what the Lord Jesus [told us]. We know that you are conducting your lives that way, but [we strongly urge] that you do that even more.
2 Inu mukudziwa malangizo amene tinakupatsani mwa ulamuliro wa Ambuye Yesu.
3 Ndi chifuniro cha Mulungu kuti muyeretsedwe: kuti mupewe dama;
God wants you to live pure lives that will show that you completely belong to him. He wants you to avoid doing any sexually immoral acts (OR, avoid being sexually immoral in any way).
4 aliyense wa inu aphunzire kulamulira thupi lake mʼnjira yoyera ndi yaulemu,
[That is, he wants] each one of you to know how to control your own sexual desires [EUP]. He wants you to live pure lives that all people will see as good.
5 osati yotsata chilakolako chonyansa monga amachitira akunja, amene sadziwa Mulungu.
You must not lustfully desire [to do] immoral acts as unbelievers [MTY] [do] who do not obey God.
6 Pa zimenezi munthu asachimwire mʼbale wake kapena kumuonerera. Ambuye adzalanga anthu onse amene amachita machimo amenewa, monga tinakuwuzani kale ndi kukuchenjezani.
[God wants each one of you to control your sexual desires, in order that] no one of you sin against your fellow believer and take advantage of him or her by doing things like that. Remember that we strongly warned you previously [DOU] that the Lord [Jesus] will punish all [people who do] sexually immoral acts.
7 Pakuti Mulungu sanatiyitane kuti tizichita zonyansa, koma kuti tikhale oyera mtima.
When God chose us [believers], he did not want us to [be people who] behave in a sexually immoral way. On the contrary, [he wants us] to be [people who] behave in a morally pure way.
8 Choncho, aliyense amene akukana malangizo awa sakukana munthu koma Mulungu, Mulungu weniweniyo amene amakupatsani Mzimu Woyera.
So I warn you that those who disregard [this teaching] of mine [are] not just disregarding me. On the contrary, [they are disregarding] God, [because God commanded it. Remember that] God sent his Spirit, who is holy, [to live] in you!
9 Tsono kunena za kukondana wina ndi mnzake, nʼkosafunikira kuti tikulembereni, popeza ndi Mulungu amene anakuphunzitsani za kukondana wina ndi mnzake.
[I want to urge you] again [that you should] love [your] fellow believers [MET]. You do not really need that [anyone] write to you about that, because God has already taught you [how] to love each other,
10 Ndipo kunena zoona, mumakonda abale onse a mʼbanja la Mulungu a ku Makedoniya. Komabe, abale tikukulimbikitsani kuti muzichita zimenezi koposa kale.
and because you already are [showing that you love] your fellow believers [HYP] [who live] in other places [in your province] of Macedonia. Nevertheless, my fellow believers, we urge you to [love each other] even more.
11 Yesetsani kuti mukhale moyo wofatsa. Aliyense asamale ntchito yakeyake ndi kugwira ntchito ndi manja ake.
[We urge you] also to eagerly strive/try to mind your own affairs and to not meddle/interfere with the affairs of others. We urge you also to work at your own occupations/jobs [to earn what you need to live]. Remember that we taught you previously to live like that.
12 Mukatero akunja adzalemekeza makhalidwe anu a tsiku ndi tsiku, ndi kuti inuyo mukhale osadalira wina aliyense.
If you do these things, unbelievers will acknowledge/see that you behave decently/properly, and you will not have to depend on others [to] ([supply/give to you]) [what you need].
13 Abale, ife sitikufuna mukhale osadziwa za amene akugona, kapena kumva chisoni ngati anthu ena opanda chiyembekezo.
My fellow believers, we also want you to understand well [LIT] [what will happen] to our fellow believers [who now] are dead [EUP]. [You must not be/do like] the unbelievers. They [grieve deeply for people who die because] they do not confidently expect [people to live again after they die].
14 Ife timakhulupirira kuti Yesu anamwalira naukanso. Moteronso timakhulupirira kuti amene anamwalira ali mwa Yesu, Mulungu adzawaukitsa nʼkubwera nawo pamodzi ndi Yesuyo.
We [believers] know that it is true that Jesus died and that he came back [to life] again. So [we also know well that] when Jesus returns, God [will cause] those [believers] who died [EUP] [to live again] and to come with [Jesus].
15 Molingana ndi mawu a Ambuye mwini, tikukuwuzani kuti, ife amene tikanali ndi moyo, otsala mpaka kubwera kwa Ambuye, sitidzawasiya kumbuyo amene anagona kale.
[I write this] because the Lord [Jesus] revealed [to me] what I am now telling you. [Some of you may think that] when the Lord [Jesus] comes back, he will consider that we [believers] who are still living will be superior to those [believers] who have died [EUP], because [we will meet Jesus first. That is certainly not true]!
16 Pakuti Ambuye mwini adzatsika kuchokera kumwamba, ndi mfuwu waulamuliro, ndi liwu la mngelo wamkulu, ndi kulira kwa lipenga la Mulungu, ndipo akufa amene ali mwa Yesu adzauka poyamba.
It is the Lord [Jesus] himself who will descend from heaven. [When he comes down, he] will command all of [us believers to rise from their graves]. The chief angel will shout [loudly], and [another angel] will blow a trumpet for God. Then (OR, As a result), the first thing that will happen is that the people who [trusted] in Christ before they died will live again.
17 Kenaka, ife amene tili ndi moyo, otsalafe, tidzakwatulidwa pamodzi ndi iwo mʼmitambo kukakumana ndi Ambuye mlengalenga. Tsono ife tidzakhala ndi Ambuye mpaka muyaya.
After that, [God] will powerfully take up into the clouds all of us [believers] who are still living [on this earth]. [He will take us] and those [other believers who have died], in order that [we all] might together meet/welcome the Lord [Jesus] in the sky. As a result of that, we [all] will be with him forever.
18 Nʼchifukwa chake tsono muzilimbikitsana ndi mawu amenewa.
Because [all this is true], encourage/comfort each other by reminding each other of this teaching.