< 1 Atesalonika 4 >
1 Potsiriza, abale, tinakulangizani kale momwe mukuyenera kukhalira kuti mukondweretse Mulungu, monga momwe mukukhaliramo. Tsopano tikukupemphani ndi kukulimbikitsani mwa Ambuye Yesu kuti muchite zimenezi koposa kale.
Ni klekle, mri vayi, kisi bre nimi Bachi mbu Yesu dun yi kri gbamgba. Na wa bi wo ki bla hla ni yiwu nitu dun yi zren bi ni nkoh Irji, u bika zren tohki ndi kpa suron Irji kasi.
2 Inu mukudziwa malangizo amene tinakupatsani mwa ulamuliro wa Ambuye Yesu.
U bi toh ndi ikpe wa ki bla hla ni yiwu ahe ni nkoh Bachi Yesu.
3 Ndi chifuniro cha Mulungu kuti muyeretsedwe: kuti mupewe dama;
Wayi mba ahi tie u Irji, ndi nglah iddri mbi, don dun yi wru-hleh ni ittre u kru ni-mbah,
4 aliyense wa inu aphunzire kulamulira thupi lake mʼnjira yoyera ndi yaulemu,
don dun wawu-mbi toh ndi nji kpambi ni nkoh wa abi,
5 osati yotsata chilakolako chonyansa monga amachitira akunja, amene sadziwa Mulungu.
ana ndi dun yi tie memme na biwa bana toh Irji ba tie na.
6 Pa zimenezi munthu asachimwire mʼbale wake kapena kumuonerera. Ambuye adzalanga anthu onse amene amachita machimo amenewa, monga tinakuwuzani kale ndi kukuchenjezani.
Dun ndjro na ya mri vayi ma grjigrji nitu-ttre yi na. Don Irji mba ni kpa nyu mba toh bi tie naki, na wa ki gbii-tohn mbi ndi bla hla.
7 Pakuti Mulungu sanatiyitane kuti tizichita zonyansa, koma kuti tikhale oyera mtima.
U Irji yoh ta rhi ni-ikpahn ddri, ana kpa iddri mbu tie-rji na.
8 Choncho, aliyense amene akukana malangizo awa sakukana munthu koma Mulungu, Mulungu weniweniyo amene amakupatsani Mzimu Woyera.
Nitu kii, indji wa a kama ni ttre yi, ana kama ni ndji na, a kama ni Irji, waa ka suron ndindima nu.
9 Tsono kunena za kukondana wina ndi mnzake, nʼkosafunikira kuti tikulembereni, popeza ndi Mulungu amene anakuphunzitsani za kukondana wina ndi mnzake.
Ni mgbala'u sohn mmri vayi'a, ana ndi dun ndjori ngna noh yi rhi bika toh na, u biyi kimbi bi toh ndi ahi Irji nikima a tsuro yi dun yi sohn kpambi.
10 Ndipo kunena zoona, mumakonda abale onse a mʼbanja la Mulungu a ku Makedoniya. Komabe, abale tikukulimbikitsani kuti muzichita zimenezi koposa kale.
Naki, bi ka tie wayi ni wawu mmri vayi wa ba he ni wawu Masidoniya. U kina ka chuwo ni hla niyiwu dun yi vu tre yi nji mgbamgba me na, mmri vayi.
11 Yesetsani kuti mukhale moyo wofatsa. Aliyense asamale ntchito yakeyake ndi kugwira ntchito ndi manja ake.
Ki hla yiwu ngari ndi dun ki noyi gbemgblen dun yi soh bi, ndi vu-kpeh wa'a he ko shishi mbi, ndi tie ndu nì-wóh mbi, nawa ki bla zi yiwu,
12 Mukatero akunja adzalemekeza makhalidwe anu a tsiku ndi tsiku, ndi kuti inuyo mukhale osadalira wina aliyense.
don dun yi zrehn ni nkoh ndindima ni shishi ndji bi kora u ndi na rhii ni-yyá na.
13 Abale, ife sitikufuna mukhale osadziwa za amene akugona, kapena kumva chisoni ngati anthu ena opanda chiyembekezo.
Kita kina son dun yi kado na, immri vayi, nitu biwa ba krunna, don dun yi na yih na imbru-ndji biwa bana toh nitu njanji u ko-sshi'a na.
14 Ife timakhulupirira kuti Yesu anamwalira naukanso. Moteronso timakhulupirira kuti amene anamwalira ali mwa Yesu, Mulungu adzawaukitsa nʼkubwera nawo pamodzi ndi Yesuyo.
U tó bi kpa-nyime ndi Yesu kwu nda tashime rji ni kwu-a ngari, naki, Irji ni nji ivvri biwa ba krunna ni nkoh ma kmaye.
15 Molingana ndi mawu a Ambuye mwini, tikukuwuzani kuti, ife amene tikanali ndi moyo, otsala mpaka kubwera kwa Ambuye, sitidzawasiya kumbuyo amene anagona kale.
Wayi ki bla hla ni yiwu ni-ttre Bachi, ndi kita biwa ki ri si vvri-a, wa a don ta ki toh ye u Bachi-a, kina guchi ni biwa ba krunna-a na.
16 Pakuti Ambuye mwini adzatsika kuchokera kumwamba, ndi mfuwu waulamuliro, ndi liwu la mngelo wamkulu, ndi kulira kwa lipenga la Mulungu, ndipo akufa amene ali mwa Yesu adzauka poyamba.
Irji kima ani grji ye ni meme rji ni shulu. Ani ye nda yo gbamgba, ni lan u nigra bi gben ni koh Irji, u nda ni nvrih injon u Irji, u biwa ba kwu nimi Yesu'a ba rju guchi.
17 Kenaka, ife amene tili ndi moyo, otsalafe, tidzakwatulidwa pamodzi ndi iwo mʼmitambo kukakumana ndi Ambuye mlengalenga. Tsono ife tidzakhala ndi Ambuye mpaka muyaya.
U kita biwa ki ri si vri'a, wa ki ri he ni gbumgblu'a, kita ni biwa ba kwu'a ki lu hon hi toh Bachi ni shulu. ni naki ki sita sohn ni Bachi.
18 Nʼchifukwa chake tsono muzilimbikitsana ndi mawu amenewa.
Nitu ki, bika si kpa suron mbi kusi ni-ttre bi yí.