< 1 Samueli 29 >
1 Afilisti anasonkhanitsa asilikali awo onse ku Afeki, ndipo Israeli anamanga misasa yawo pa chitsime cha Yezireeli.
Hot patetlah Filistinnaw ni a ransanaw hah Aphek kho a pâkhueng. Hahoi Isarelnaw Jezreel vah kaawm e tuikhu koe a tungpup awh.
2 Pamene atsogoleri a Afilisti ankatsogolera magulu awo ankhondo a miyandamiyanda, Davide ndi ankhondo ake ankayenda pambuyo pamodzi ndi Akisi.
Filistin bawinaw teh, a cum lahoi a thong lahoi a cei parai teh, Devit hoi a taminaw teh Akhish hoi a hnuklah a tho awh.
3 Tsono atsogoleri a Afilisti aja anafunsa kuti, “Kodi Ahebri awa akufuna chiyani?” Akisi anayankha kuti, “Uyu ndi Davide, mtumiki wa Sauli mfumu ya Israeli. Iye wakhala ndi ine kwa masiku ndithu, kapena titi zaka ndipo kuyambira tsiku limene anachoka kwa Sauli mpaka lero, ine sindinapeze cholakwa mwa iye.”
Hot patetlah Filistin bawinaw ni hete Hebru taminaw ni bangmaw a sak awh telah ati. Akhish ni Filistin bawinaw koevah, hete Devit Isarel siangpahrang Sawl e a san, kasawlah kai koe ao toe, kai koe a poung hnin hoi sahnin totouh a yonnae ka hmawt hoeh telah atipouh.
4 Koma atsogoleri a ankhondo a Afilisti anamukwiyira Akisi kwambiri ndipo anati, “Mubweze munthuyu kuti abwerere ku malo amene unamupatsa. Iye asapite nafe ku nkhondo kuopa kuti angadzasanduke mdani wathu. Kodi iyeyu adzadziyanjanitsa bwanji ndi mbuye wake? Iyeyutu adzadziyanjanitsa ndi mbuye wake pakupha anthu ali panowa?
Hatei Filistin bawinaw ni ahni dawk a lungphuen awh teh, hote tami teh hmuen na poe e koe koung ban sak. Taran tuk nah maimouh koe tho nahanh seh, telah hoehpawiteh, taran tuknae koe tarannaw koelah kambawng vaiteh, maimae taminaw lûkalatkung lah awm payon vaih, a bawipa hoi bout kâpo roi vaih.
5 Paja ameneyu ndi Davide yemwe ankamuvinira namuyimbira kuti, “‘Sauli wapha anthu 1,000 koma Davide wapha miyandamiyanda?’”
Hete Devit nahoehmaw, lam laihoi, Sawl thong touh thong touh, Devit thong hra, thong hra titeh ahni hah la lah a sak awh e hah ati awh.
6 Kotero Akisi anayitana Davide ndipo anamuwuza kuti, “Pali Yehova wamoyo, iwe wakhala wodalirika ndipo chikanakhala chinthu chabwino kuti uzimenya nkhondo pamodzi nane popeza chibwerere iwe kuno ine sindinapeze cholakwa chilichonse ndi iwe. Koma atsogoleri enawa ndiwo sakukufuna.
Hat torei teh, Akhish ni Devit teh ama koe a kaw teh, BAWIPA a hring e patetlah tamikalan lah na o tangngak, ransa thung hoi kai koe na tho na cei e ka hmu navah ahawi toungloung. Kai koe na tho hoi sahnin totouh nang koe hawihoehnae bangcahai ka hmawt hoeh. Hatei, bawinaw ni na kângue awh hoeh.
7 Tsono bwerera. Upite mu mtendere kuopa kuti ungachite kanthu kena koyipira atsogoleri a Afilistiwa.”
Hatdawkvah, bawinaw ni a lungkuep nahanlah ban nateh lungkuepcalah ban lawih atipouh.
8 Davide anafunsa Akisi kuti, “Kodi ndachita chiyani? Kodi mwapeza cholakwa chotani mwa ine mtumiki wanu chiyambire kukutumikirani mpaka lero? Tsono chifukwa chiyani sindingapite kukamenya nkhondo ndi adani a mbuye wanga mfumu?”
Devit ni, Akhish koevah, telah pawiteh bang hno maw ouk ka sak. Nang koe ka o yunglam sahnin totouh ka bawipa ka bawi poung taran hah tuk laipalah ka ban nahane hah na sannaw koe bangmaw a panue awh e kaawm telah atipouh.
9 Akisi anayankha kuti, “Ine ndikudziwa kuti ndiwe wangwiro ngati mngelo wa Mulungu. Komabe atsogoleri a ankhondo a Afilisti akuti, ‘Davide asapite nafe ku nkhondo.’
Akhish ni Devit ma koe, ka mithmu teh Cathut kalvantami patetlah na hawi. Hatei, Filistin bawinaw ni taran tuknae koe kaimouh koe cet hanh naseh ati awh dawk doeh.
10 Tsono udzuke mmamawa, pamodzi ndi ankhondo ako amene unabwera nawo, ndipo unyamuke kukangocha.”
Hatdawkvah, nang koe ka cet e na bawipa sannaw hoiyah amom vah thaw awh. Amom vah na thaw awh teh, khodai tahma vah na cettakhai awh lawih telah atipouh.
11 Choncho Davide ndi anthu ake anadzuka mmamawa kubwerera ku dziko la Afilisti. Koma Afilistiwo anapita ku Yezireeli.
Hahoi teh Devit hoi a taminaw hah Filistin ram vah amom ban hanelah palang a thaw awh teh, Filistinnaw teh Jezreel lah a takhang awh.