< 1 Samueli 20 >
1 Tsono Davide anathawa ku Nayoti ku Rama ndi kupita kwa Yonatani ndipo anamufunsa kuti, “Kodi ine ndinachita chiyani? Kodi ndinalakwa chiyani? Kodi abambo ako ndinawalakwira chiyani kuti azifuna kundipha?”
UDavida wabaleka eNayothi eRama waya kuJonathani wabuza wathi, “Kanti ngenzeni na? Icala lami ngelani na? Uyihlo ngimone kanjani, okwenza afune ukungibulala?”
2 Yonatani anayankha kuti, “Sizitheka! Iwe sufa ayi! Taona abambo anga sachita chinthu chilichonse chachikulu kapena chachingʼono wosandiwuza ine. Tsopano abambo anga angandibisire bwanji zimenezi? Sichoncho ayi.”
UJonathani waphendula wathi, “Hatshi bo! Kawuyikufa! Khangela, ubaba kenzi lutho, olukhulu loba oluncane, engangitshelanga. Kungani engangifihlela lokhu na? Akunjalo!”
3 Koma Davide analumbira kuti, “Abambo ako akudziwa bwino lomwe kuti iwe umandikonda ndipo iwo amaganiza kuti, Yonatani sayenera kudziwa zimenezi mwina adzamva chisoni kwambiri. Komabe, pali Yehova ndi pali iwe, imfa sinanditalikire.”
Kodwa uDavida wenza isifungo wathi, “Uyihlo ukwazi kakuhle ukuthi mina sengithole umusa kuwe njalo usezitshele wathi, ‘UJonathani akumelanga akwazi lokhu hlezi ezwe ubuhlungu.’ Ikanti ngeqiniso elinjengoba uThixo ekhona lanjengoba lawe ukhona, kulenyathelo elilodwa nje phakathi kwami lokufa.”
4 Yonatani anawuza Davide kuti, “Chilichonse chimene iwe ukufuna kuti ndichite, ndidzakuchitira.”
UJonathani wathi kuDavida, “Loba kuyini ofuna ukuthi ngikwenze, ngizakwenzela khona.”
5 Ndipo Davide anati, “Taona mawa ndi tsiku la chikondwerero cha mwezi watsopano, ndipo ine ndiyenera kukadya ndi mfumu. Koma undilole ndipite ndikabisale mʼmunda mpaka mkuja madzulo.
Ngakho uDavida wathi, “Khangela, kusasa kuledili lokuThwasa kweNyanga, njalo kumele ngidle lenkosi; kodwa yekela ngiyecatsha egangeni kuze kube kusihlwa phambi kwakusasa.
6 Ngati abambo ako akafunsa za ine, ukawawuze kuti, ‘Davide anandiwumiriza kuti ndimulole apite msanga kwawo ku Betelehemu, chifukwa akupereka nsembe yapachaka ya banja lonse.’
Nxa uyihlo ezangiswela, mtshele uthi, ‘UDavida ucele imvumo kimi ngokutshiseka ukuba ake agijimele eBhethilehema, idolobho lakibo, ngoba umhlatshelo wesizwana sonke sakibo uyenziwa khona.’
7 Akanena kuti, ‘Wachita bwino,’ ndiye kuti zinthu zindiyendera bwino ine mtumiki wako. Koma ngati akapsa mtima, ndiye udziwe kuti iwo atsimikiza zondichita zoyipa.
Angathi, ‘Kulungile,’ inceku yakho kayiyikuba sengozini. Kodwa angavuka ulaka woba leqiniso ukuthi uzimisele ukwenza okubi kimi.
8 Koma undikomere mtima ine mtumiki wako, pakuti unapangana nane pangano pamaso pa Yehova. Ngati ndine wolakwa undiphe ndiwe, koma usandipereke kwa abambo ako.”
Kodwa wena, bonakalisa isisa encekwini yakho ngoba uyenzise isivumelwano lawe phambi kukaThixo. Nxa ngilecala, ngibulala wena ngokwakho! Kungani ungiqhubela kuyihlo na?”
9 Yonatani anati, “Sizitheka! Ndikanadziwa kuti abambo anga atsimikiza kuti akuchite choyipa, kodi sindikanakuwuza?”
UJonathani wathi, “Hatshi bo! Kambe aluba bengilolwazi oluncane ukuthi ubaba uzimisele ukwenza okubi kuwe, kade ngingasoze ngikutshele na?”
10 Davide anafunsa kuti, “Adzandiwuza ndani ngati abambo ako akuyankhe mwaukali?”
UDavida wabuza wathi, “Ngubani ozangitshela nxa uyihlo ekuphendula kubi na?”
11 Yonatani anawuza Davide kuti, “Tiyeni tikayende ku mundako.” Ndipo anapita onse awiri.
UJonathani wathi, “Woza, kasiye egangeni.” Ngakho baya khonale bobabili.
12 Kenaka Yonatani anawuza Davide kuti, “Yehova Mulungu wa Israeli akhale mboni! Ine ndikadzafunsa abambo anga nthawi yonga ino mmawa kapena mkuja, ndipo ndikadzapeza kuti akukufunira zabwino, ine ndidzatuma mawu kuti udziwe.
UJonathani wasesithi kuDavida, “Ngifunga ngoThixo, uNkulunkulu ka-Israyeli, ngempela ubaba ngizakuba sengimzwile ngalesisikhathi ngomhlomunye! Nxa elomusa kuwe, kambe kangiyikuthumela ilizwi ngikwazise na?
13 Koma ngati abambo anga atsimikiza kukuchita choyipa, Yehova andilange ine Yonatani, ndipotu kwambiri ngati sindidzakudziwitsa ndi kukulola kuti upite mu mtendere. Yehova akhale nawe monga anakhalira ndi abambo anga.
Kodwa nxa ubaba ehlose ukwenza okubi kuwe, uThixo kangijezise, kube nzima kakhulu, nxa ngingakwazisi njalo ngikususe kungekho ngozi. Sengathi uThixo angaba lawe njengoba kade elobaba.
14 Ndikakhalabe ndi moyo udzandionetse kukoma mtima monga kwa Yehova nthawi yonse ya moyo wanga, kuti ine ndisaphedwe.
Kodwa ngibonise umusa ongapheliyo onjengokaThixo isikhathi sonke ngisaphila, ukuze ngingabulawa,
15 Ndipo usadzaleke kuchitira chifundo banja langa. Pamene Yehova adzawatha adani onse a Davide pa dziko lapansi.”
njalo ungasusi umusa wakho kwabendlu yakwethu lanxa uThixo eseziqede du zonke izitha zikaDavida ebusweni bomhlaba.”
16 “Dzina la ine Yonatani lisadzafafanizidwe nawo pamodzi. Yehova alange adani onse a Davide.”
Ngakho uJonathani wenza isivumelwano labendlu kaDavida, esithi, “Sengathi uThixo angazethesa amacala izitha zikaDavida.”
17 Kenaka Yonatani anamulumbiritsanso Davide kuti asaleke kumukonda, pakuti ankamukonda monga ankadzikondera yekha.
UJonathani wabuya wamfungisa futhi uDavida isifungo sakhe ngenxa yothando lwakhe kuye, ngoba wayemthanda njengokuzithanda kwakhe.
18 Kenaka Yonatani anawuzanso Davide kuti, “Mawa ndi tsiku la chikondwerero cha mwezi watsopano. Zidzadziwika kuti iwe palibe chifukwa mpando wako udzakhala wopanda munthu.
UJonathani wasesithi kuDavida, “Kusasa kuledili lokuThwasa kweNyanga. Uzaswelakala ngoba isihlalo sakho sizabe singelamuntu.
19 Mkuja adzakufunafuna. Tsono udzapite pamalo pamene unabisala poyamba paja ndipo ukadikire pa mulu wa miyala uli apowo.
Phambi kwakusasa, sekuzakuhlwa, yana lapho owacatsha khona ekuqaliseni kwaloluhlupho, ulinde elitsheni e-Ezeli.
20 Ine ndidzaponya mivi itatu pambali pake, ngati ndikulasa chinthu.
Mina ngizatshokela imitshoko emithathu eceleni kwalo angathi ngitshokela kwengihlose kukho.
21 Ndipo ndidzatuma mnyamata ndi kuti, ‘Pita ukatole miviyo!’ Ngati ndidzanena kwa iye kuti, ‘Taona, mivi ili mbali yakuno, kayitole,’ iwe ukatuluke, pakuti ndikulumbira, pali Yehova Wamoyo, ndiye kuti zako zili bwino, palibe choopsa chilichonse.
Emva kwalokho ngizathuma umfana ngithi, ‘Hamba uyedinga imitshoko.’ Ngingathi kuye, ‘Khangela, imitshoko ingakuleli icele lakho, ilethe lapha,’ lapho-ke woza, ngoba ngeqiniso elinjengoba uThixo ekhona, uphephile, akulangozi.
22 Koma ndikadzati, ‘Taona mivi ili patsogolo pako,’ iwe udzachoke chifukwa Yehova ndiye walola kuti uchokepo.
Kodwa ngingathi emfaneni, ‘Khangela, imitshoko ingale kwakho,’ lapho-ke kumele uhambe, ngoba uThixo uthe suka uhambe.
23 Tsono zimene tapanganazi Yehova ndiye mboni pakati pa iwe ndi ine mpaka muyaya.”
Njalo mayelana lalindaba esiyikhulumileyo mina lawe, khumbula ukuthi uThixo ungufakazi phakathi kwakho lami nini lanini.”
24 Choncho Davide anakabisala mʼmunda ndipo nthawi ya chikondwerero cha mwezi watsopano itakwana mfumu Sauli anadzakhala pansi kuti adye.
Ngakho uDavida wacatsha egangeni, njalo kwathi idili lokuThwasa kweNyanga selifikile, inkosi yahlala phansi yadla.
25 Iye anakhala pa malo ake a nthawi zonse pafupi ndi khoma moyangʼanana ndi Yonatani, ndipo Abineri anakhala moyandikana ndi Sauli, koma pa malo a Davide panalibe munthu.
Yayihlezi endaweni yayo yezikhathi zonke phansi komduli, maqondana loJonathani, u-Abhineri ehlezi eduze loSawuli, kodwa indawo kaDavida yayingelamuntu.
26 Sauli sananene chilichonse tsiku limenelo pakuti ankaganiza kuti “Chilipo chimene chachitika ndi Davide. Mwina mwake ngosayenera za chipembedzo.”
USawuli katshongo lutho mhlalokho, ngoba wacabanga wathi, “Mhlawumbe kulento ethile eyehlele kuDavida yamenza waba ngongahlambulukanga ngokomkhuba, ngeqiniso kahlambulukanga.”
27 Koma pa tsiku lachiwiri la chikondwerero cha mwezi watsopano pamalo pa Davide panalibenso munthu. Kenaka Sauli anafunsa Yonatani kuti, “Nʼchifukwa chiyani mwana wa Yese sanabwere kudzadya, dzulo ngakhale lero?”
Kodwa ngelanga elilandelayo, ilanga lesibili lenyanga, indawo kaDavida yayingelamuntu futhi. Lapho-ke uSawuli wathi endodaneni yakhe uJonathani, “Kungani indodana kaJese ingezanga ekudleni, izolo kumbe lamuhla na?”
28 Yonatani anayankha kuti, “Davide anandiwumiriza kuti ndimulole kuti apite ku Betelehemu.
UJonathani waphendula wathi, “UDavida ucele imvumo kimi ngokutshiseka ukuba aye eBhethilehema.
29 Anati, ‘Undilole ndipite, chifukwa banja lathu likupereka nsembe mu mzindamo ndipo mʼbale wanga wandiwumiriza kuti ndikakhale nawo. Ngati wandikomera mtima, chonde ndilole ndipite ndikaone abale anga.’ Nʼchifukwa chake sanabwere kudzadya ndi mfumu.”
Uthe, ‘Ngivumela ngihambe ngoba abendlu yakwethu balomkhosi womhlatshelo edolobheni njalo umnewethu ungilaye ukuba ngibe khona. Nxa ngithole umusa kuwe, ngivumela ngihambe ngiyebona abafowethu.’ Yikho-nje engezanga ukuzakudla lenkosi.”
30 Sauli anamupsera mtima Yonatani ndipo namuwuza kuti, “Iwe mwana wobadwa mwa mkazi wamakhalidwe oyipa ndi wowukira! Kodi ukuyesa kuti ine sindikudziwa kuti umagwirizana ndi mwana wa Yese, amene akufuna kukuchititsa manyazi iwe ndi amayi ako?
Ulaka lukaSawuli lwavutha kuJonathani wathi kuye, “Wena ndodana yomfazi olihlongandlebe lolenkani! Uthi kangazi yini ukuthi wena ususekelane lendodana kaJese okulihlazo kuwe njalo okulihlazo lakunyoko owakuzalayo na?
31 Mwana wa Yese akakhala ndi moyo pa dziko lapansi lino, iwe sudzakhala mfumu. Tsopano tumiza munthu akamutenge kubwera naye kwa ine, pakuti Davide ayenera kufa basi!”
Nxa indodana kaJese isekhona kulo umhlaba, wena kawuyikuma kumbe umbuso wakho. Ngakho thumela ilizwi umlethe kimi, ngoba umele afe!”
32 Yonatani anafunsa abambo ake kuti, “Nʼchifukwa chiyani mufuna kuti Davide aphedwe? Iye walakwa chiyani?”
UJonathani wabuza uyise wathi, “Kungani kumele abulawe? Wenzeni na?”
33 Apo Sauli anamuponyera mkondo wake kuti amuphe. Tsono Yonatani anadziwa kuti abambo ake atsimikiza mtima kuti aphe Davide.
Kodwa uSawuli waphosa umkhonto wakhe kuye ukuba ambulale. Ngakho uJonathani wakwazi ukuthi uyise wayehlose ukubulala uDavida.
34 Yonatani anachoka pa tebulopo ali wopsa mtima kwambiri. Tsiku lachiwiri la chikondwererocho Yonatani sanadye chakudya. Iye anawawidwa mtima chifukwa abambo ake anatsimikiza zakupha Davide.
UJonathani wasuka etafuleni ethukuthele kakhulu; ngosuku lwesibili lwedili kazange adle, ngoba wayebuhlungu ngehlazo uyise ayephatha ngalo uDavida.
35 Tsono mmawa Yonatani anapita ku munda kumene anapangana ndi Davide. Anali ndi mnyamata wake.
Ekuseni uJonathani waphuma waya egangeni ukuyahlangana loDavida. Wayelomfana omncinyane,
36 Tsono anawuza mnyamatayo kuti, “Thamanga ukatole muvi umene nditi ndiponye.” Mnyamatayo akuthamanga Yonatani anaponya muvi patsogolo pa mnyamatayo.
njalo wathi emfaneni, “Gijima uyedobha imitshoko engiyitshokayo.” Umfana esagijima, watshokela umtshoko ngale kwakhe.
37 Mnyamatayo atafika pamene muvi wa Yonatani unagwera,
Kwathi umfana esefike lapho umtshoko kaJonathani owawuwele khona, uJonathani wamemeza wathi, “Umtshoko kawukho ngale kwakho na?”
38 Yonatani anayitananso mnyamatayo kuti, “Fulumira, pita msanga usayime.” Choncho mnyamatayo anatola muvi uja ndi kubwera nayo kwa mbuye wake.
Wabuye wamemeza wathi, “Phangisa! Ukhawuleze! Ungemi!” Umfana wadobha umtshoko wabuyela enkosini yakhe.
39 (Mnyamatayo sanadziwe chimene chimachitika koma Yonatani ndi Davide ndiwo ankadziwa).
(Umfana wayengazi lutho ngakho konke lokhu; kusazi uJonathani loDavida kuphela.)
40 Pambuyo pake Yonatani anapereka zida zake za nkhondo kwa mnyamatayo ndipo anati, “Pita, nyamula ubwerere nazo ku mzinda.”
Emva kwalokho uJonathani wanika umfana izikhali zakhe wathi, “Hamba, zithwale ubuyele lazo edolobheni.”
41 Mnyamatayo anapita. Kenaka Davide anatuluka ku mbali ina ya mulu wa miyala uja, nadzigwetsa pansi ndi kugunditsa nkhope yake pansi katatu. Anapsompsona nayamba kulira onse awiri, koma Davide analira kwambiri.
Umfana esehambile uDavida wasukuma eceleni langaseningizimu kwelitshe, wakhothama kathathu phambi kukaJonathani, ubuso bakhe bukhangele phansi. Emva kwalokho bangana, bakhala bendawonye kodwa uDavida wakhala kakhulu.
42 Yonatani anawuza Davide kuti, “Pita mu mtendere pakuti ife awiri tinalumbira mʼdzina la Yehova kuti, ‘Yehova ndiye akhale mboni pakati pa iwe ndi ine ndiponso pakati pa zidzukulu zako ndi zidzukulu zanga kwa nthawi yonse.’” Kenaka Davide anachoka, ndipo Yonatani anabwerera ku mzinda kuja.
UJonathani wasesithi kuDavida, “Hamba ngokuthula, ngoba sifungelane ubungane omunye komunye ebizweni likaThixo sisithi, ‘Uthixo ungufakazi phakathi kwami lawe, laphakathi kwenzalo yakho leyami nini lanini.’” UDavida wasesuka, loJonathani wasebuyela edolobheni.