< 1 Samueli 2 >
1 Ndipo Hana anapemphera nati, “Moyo wanga ukukondwera mwa Yehova; Ndiyenda mwa tukumutukumu chifukwa cha Yehova. Pakamwa panga pakula ndi kuseka adani anga mowanyogodola. Ndikukondwa chifukwa mwandipulumutsa.
Hannah rezou, e disse, “Meu coração exulta em Yahweh! Meu chifre é exaltado em Yahweh. Minha boca está dilatada sobre meus inimigos, porque me regozijo com a sua salvação.
2 “Palibe wina woyera ngati Yehova, palibe wina koma inu nokha, palibe thanthwe lofanana ndi Mulungu wathu.
Não há ninguém tão santo como Yahweh, pois não há ninguém além de você, nem existe nenhuma rocha como nosso Deus.
3 “Musandiyankhulenso modzitama, pakamwa panu pasatuluke zonyada, pakuti Yehova ndi Mulungu wanzeru, ndipo ndiye amene amayesa ntchito za anthu onse.
“Não continue falando de forma tão orgulhosa. Não deixe que a arrogância saia de sua boca, pois Yahweh é um Deus de conhecimento. Por ele, as ações são pesadas.
4 “Mauta a anthu ankhondo athyoka koma anthu ofowoka avala dzilimbe.
“Os arcos dos homens poderosos estão quebrados. Aqueles que tropeçaram estão armados com força.
5 Amene kale anali okhuta tsopano akukagula chakudya, koma iwo amene anali ndi njala sakumvanso njala. Amene anali wosabereka, wabereka ana aamuna asanu ndi awiri, koma iye wobereka ana ambiri watsala yekha.
Aqueles que estavam cheios se alugaram para o pão. Aqueles que estavam com fome estão satisfeitos. Sim, a árida suportou sete. Ela, que tem muitos filhos, definha.
6 “Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
“Yahweh mata e dá vida. Ele traz para baixo para Sheol e traz para cima. (Sheol )
7 Yehova amasaukitsa ndipo amalemeretsa, amatsitsa ndipo amakweza.
Yahweh faz pobre e faz rico. Ele traz baixo, ele também se eleva.
8 Iye amakweza osauka kuwachotsa pa fumbi, ndipo amachotsa anthu osowa pa dzala. Iye amawakhazika pamodzi ndi ana a mafumu, amawapatsa mpando waulemu. “Pakuti nsanamira za dziko lapansi ndi za Yehova, anakhazika dziko lapansi pa nsanamirazo.
Ele levanta os pobres da poeira. Ele levanta os necessitados do monte de estrume para fazê-los sentar com príncipes e herdar o trono da glória. Pois os pilares da terra são os de Yahweh. Ele colocou o mundo sobre eles.
9 Iye adzateteza moyo wa anthu okhulupirika koma anthu oyipa adzawonongedwa mu mdima. “Pakuti munthu sapambana ndi mphamvu zake.
Ele manterá os pés de seus santos, mas os ímpios serão colocados em silêncio na escuridão; pois nenhum homem prevalecerá pela força.
10 Yehova adzaphwanya omutsutsa. Adzawaopsa ndi bingu kuchokera kumwamba; Yehova adzaweruza mathero a dziko lapansi. “Koma adzapereka mphamvu kwa mfumu yake, adzakuza mphamvu za odzozedwa wake.”
Aqueles que lutam com Yahweh serão despedaçados. Ele vai trovejar contra eles no céu. “Yahweh julgará os confins da terra”. Ele dará força ao seu rei, e exaltar o chifre de seu ungido”.
11 Tsono Elikana anapita ku mudzi kwawo ku Rama, koma mnyamatayo amatumikira Yehova pansi pa ulamuliro wa wansembe Eli.
Elkanah foi a Ramah para sua casa. A criança serviu a Yahweh antes de Eli, o padre.
12 Ana a Eli anali ana achabechabe pakuti samasamala za Yehova.
Now os filhos de Eli eram homens perversos. Eles não conheciam Yahweh.
13 Ndipo chizolowezi cha ansembe pakati pa anthu chinali motere kuti pamene munthu aliyense ankapereka nsembe ndipo nyama ija ikuwira pa moto, mtumiki wa wansembe ankabwera ndi chifoloko cha mano atatu mʼdzanja lake.
O costume dos sacerdotes com o povo era que quando alguém oferecia um sacrifício, o servo do sacerdote vinha enquanto a carne fervia, com um garfo de três dentes na mão;
14 Iye ankachipisa mu mʼphikamo, ndipo wansembeyo amatenga chilichonse chimene folokoyo yabaya. Umu ndi mmene ansembewo amachitira ndi Aisraeli onse amene amabwera ku Silo.
e ele o apunhalava na panela, ou chaleira, ou caldeirão, ou panela. O padre pegou tudo o que o garfo trouxe para si. Fizeram isso com todos os israelitas que vieram para Shiloh.
15 Ndipo ngakhale mafuta asanatenthedwe, mtumiki wansembe amabwera ndi kunena kwa munthu amene akupereka nsembeyo kuti, “Ndipatse nyama kuti ndiwotche, pakuti Yehova salandira nyama yophika koma yayiwisi.”
Sim, antes que queimassem a gordura, veio o servo do sacerdote, e disse ao homem que se sacrificou: “Dê carne para assar para o sacerdote; pois ele não aceitará carne cozida de você, mas crua”.
16 Ngati munthuyo anena kuti, “Apseretu mafuta poyamba, ndipo kenaka mutenge mmene mufunira,” mtumikiyo amayankha kuti, “Ayi ndipatse tsopano lino. Ngati sutero, ine nditenga molanda.”
Se o homem lhe dissesse: “Queime primeiro a gordura e depois leve o quanto sua alma desejar;” então ele diria: “Não, mas você a dará agora; e se não, eu a levarei pela força”.
17 Tchimo la ana a Eli linali lalikulu kwambiri pamaso pa Yehova pakuti iwo amanyoza nsembe za Yehova.
O pecado dos jovens era muito grande antes de Yahweh; pois os homens desprezavam a oferta de Yahweh.
18 Koma Samueli amatumikira pamaso pa Yehova atavala efodi ya nsalu yofewa yosalala.
Mas Samuel ministrou antes de Iavé, sendo uma criança, vestida com um éfode de linho.
19 Chaka chilichonse amayi ake ankamusokera kamkanjo ndi kukamupatsa akamapita ndi mwamuna wake kukapereka nsembe za pa chaka.
Moreover sua mãe lhe fez um roupãozinho e o trouxe de ano em ano, quando ela veio com seu marido para oferecer o sacrifício anual.
20 Tsono Eli amadalitsa Elikana ndi mkazi wake ndi mawu akuti “Yehova akupatseni ana mwa mkazi uyu kulowa mʼmalo mwa amene anapempha ndi kumupereka kwa Yehova.”
Eli abençoou Elkanah e sua esposa, e disse: “Que Yahweh lhe dê descendência desta mulher para a petição que foi pedida a Yahweh”. Então eles foram para sua própria casa.
21 Ndipo Yehova anamukomera mtima Hana. Anakhala ndi pathupi ndi kubereka ana aamuna atatu ndi ana aakazi awiri. Ndipo Samueli ankakula pamaso pa Yehova.
Yahweh visitou Hannah, e ela concebeu e deu à luz três filhos e duas filhas. A criança Samuel cresceu antes de Yahweh.
22 Tsono Eli anakalamba kwambiri. Iye ankamva zonse zimene ana ake aamuna ankachitira Aisraeli onse, ndiponso kuti ankagona ndi akazi pa chipata cha tenti ya msonkhano.
Agora Eli era muito velho; e ouvia tudo o que seus filhos faziam com todo Israel, e como dormiam com as mulheres que serviam à porta da Tenda da Reunião.
23 Choncho anawafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukuchita zinthu zotere? Ine ndikumva kuchokera kwa anthu onse za zoyipa zanuzo.
Ele disse a elas: “Por que vocês fazem tais coisas? Pois ouvi falar de seus maus tratos por parte de todas essas pessoas.
24 Ayi, ana anga si mbiri yabwino imene ndikumva anthu a Mulungu akufalitsa.
Não, meus filhos; pois não é um bom relatório que ouço! Vocês fazem o povo de Yahweh desobedecer.
25 Ngati munthu alakwira munthu mnzake, mwina Mulungu adzamupepesera, koma ngati munthu achimwira Yehova adzamupepesera ndani?” Koma ana ake sanamvere kudzudzula kwa abambo awo, pakuti chinali cholinga cha Yehova kuti awaphe.
Se um homem pecar contra outro, Deus o julgará; mas se um homem pecar contra Javé, quem intercederá por ele?”. Não obstante, eles não ouviram a voz de seu pai, porque Yahweh pretendia matá-los.
26 Ndipo mnyamata Samueli anapitirira kukula mu msinkhu, ndipo ankapeza kuyanja pamaso pa Yehova ndi anthu.
A criança Samuel cresceu, e aumentou a favor tanto com Yahweh quanto com os homens.
27 Tsiku lina munthu wa Mulungu anabwera kwa Eli ndipo anamuwuza kuti, “Yehova akuti, ‘Kodi Ine sindinadziwulule ndekha kwa banja la kholo lako pamene iwo anali akapolo a Farao ku Igupto?
Um homem de Deus veio a Eli e lhe disse: “Javé diz: 'Será que eu me revelei à casa de seu pai quando eles estavam no Egito em cativeiro à casa do Faraó?
28 Ndipo ndinamusankha pakati pa mafuko a Israeli kuti akhale wansembe wanga ndi kuti azipita pa guwa langa la nsembe, kufukiza Lubani ndi kuvala efodi pamaso panga. Ndinapatsa banja la abambo ako gawo la nsembe zonse zopsereza zimene Aisraeli amapereka.
Didn'Não o escolhi dentre todas as tribos de Israel para ser meu sacerdote, para subir ao meu altar, para queimar incenso, para usar um éfode diante de mim? Eu não dei à casa de seu pai todas as ofertas dos filhos de Israel feitas pelo fogo?
29 Nʼchifukwa chiyani ukunyoza nsembe ndi zopereka zanga zimene ndinalamula? Nʼchifukwa chiyani ukupereka ulemu kwa ana ako kuposa Ine podzinenepetsa nokha ndi zopereka zabwino kwambiri za nsembe zimene Aisraeli amapereka?’”
Por que chutais ao meu sacrifício e à minha oferta, que ordenei em minha habitação, e honrais vossos filhos acima de mim, para vos fazerdes gordos com o melhor de todas as ofertas de Israel, meu povo”
30 “Paja Ine Yehova Mulungu wa Israeli ‘Ndinalonjeza kuti anthu a pa banja lako ndi a pa banja la abambo ako azidzanditumikira nthawi zonse.’ Koma tsopano ndikuti, ‘Zonsezi zithe!’ Tsopano anthu amene amandilemekeza Inenso ndidzawalemekeza koma iwo amene amandinyoza Ine ndidzawanyoza.
“Portanto, Javé, o Deus de Israel, diz: “Eu disse, de fato, que vossa casa e a casa de vosso pai deveriam caminhar diante de mim para sempre”. Mas agora Javé diz: “Longe de mim; pois aqueles que me honram, eu os honrarei, e aqueles que me desprezam serão amaldiçoados”.
31 Nthawi ikubwera imene ndidzachotsa anyamata ako ndi anyamata a pa banja la abambo ako, kotero kuti sipadzakhala munthu wokalamba pa banja lako.
Eis que vêm os dias em que cortarei seu braço e o braço da casa de seu pai, para que não haja um homem velho em sua casa.
32 Pa mavuto ako udzayangʼana ndi maso ansanje zabwino zimene ndidzachitira Aisraeli ena. Mʼbanja lako simudzapezeka munthu wokalamba.
Você verá a aflição de minha habitação, em toda a riqueza que eu vou dar a Israel. Não haverá um homem velho em sua casa para sempre.
33 Komabe pa banja lako mmodzi yekha ndidzamuleka wosamuchotsa kuti azidzanditumikira. Iyeyu azidzakuliritsa ndi kukumvetsa chisoni. Koma ena onse pa banja lako adzafa akanali aangʼono.”
O homem de vocês que eu não cortar de meu altar consumirá seus olhos e chorará seu coração. Todo o aumento de sua casa morrerá na flor da idade deles.
34 “‘Ndipo chimene chidzachitike kwa ana ako awiriwa, Hofini ndi Finehasi, chidzakhala chizindikiro kwa iwe. Onse awiri adzafa pa tsiku limodzi.
Este será o sinal para você que virá sobre seus dois filhos, sobre Hophni e Phinehas: em um dia, ambos morrerão.
35 Pambuyo pake ndidzasankha wansembe wokhulupirika, amene adzachita zimene zili mu mtima ndi mʼmaganizo mwanga. Ndidzakhazikitsa banja lako kolimba ndipo adzatumikira pamaso pa wodzozedwa wanga nthawi zonse.
Eu levantarei para mim um padre fiel que fará de acordo com o que está em meu coração e em minha mente. Construirei para ele uma casa segura. Ele andará para sempre diante do meu ungido.
36 Ndipo aliyense wotsala wa banja lako adzabwera ndi kugwada pamaso pake kupempha ndalama kapena chakudya.’ Adzati, ‘Chonde ndiloleni kuti ndizithandizako pa ntchito iliyonse ya unsembe kuti ndipeze chakudya.’”
Acontecerá que todos que ficarem em sua casa virão e se curvarão diante dele por um pedaço de prata e um pão, e dirão: “Por favor, coloque-me em um dos escritórios dos sacerdotes, para que eu possa comer um pedaço de pão””.