< 1 Samueli 15 >

1 Samueli anawuza Sauli kuti, “Yehova anandituma ine kuti ndikudzozeni kukhala mfumu ya anthu ake, Aisraeli. Tsopano imvani zimene Yehova akunena.
Samuel ni Sawl koe BAWIPA ni nang teh na taminaw lathueng Isarelnaw lathueng siangpahrang hanelah satui awi hane na patoun, hatdawkvah atu BAWIPA e lawk ngâi haw.
2 Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Ine ndidzalanga Aamaleki chifukwa cha zimene anawachita Aisraeli. Paja iwo analimbana ndi Aisraeli pa njira pamene Aisraeliwo ankachoka ku Igupto.
Kalvan ransabawi ni hettelah a dei. Izip ram hoi na tâco awh navah lamlak vah Amaleknaw ni Isarelnaw a ngang awh dawkvah, kai ni ahnimanaw hai ka pathung han.
3 Tsopano pita kathire nkhondo Aamaleki ndi kuwononga kwathunthu zinthu zonse zimene ali nazo. Musakasiyeko munthu ndi mmodzi yemwe. Mukaphe amuna ndi akazi, ana ndi makanda, ngʼombe ndi nkhosa, ngamira ndi abulu.’”
Atuvah cet nateh Amaleknaw hah tuk haw. Ahnimouh ni a tawn awh e pueng he raphoe. Buet touh hai hlung hanh. Napui, tongpa, camo, sanu ka net lahun e, maito, tu, kalauk hoi la pueng koung na thei han atipouh.
4 Kotero Sauli anayitana ankhondo ake nawawerenga ku Telaimu. Ankhondo oyenda pansi analipo 200,000 ndipo mwa iwowa 10,000 anali a fuko la Yuda.
Sawl ni taminaw a pâkhueng teh, Telaim vah a touk. Ransanaw 200, 000 touh hoi Judah tami 10, 000 touh a pha.
5 Sauli anapita ku mzinda wa Aamaleki nawubisalira mʼkhwawa.
Sawl teh Amalek khopui vah a pha teh, tanghling dawk hoi a pawp.
6 Tsono Sauli anawuza Akeni kuti, “Samukani, muchoke pakati pa Aamaleki kuti ine ndisakuwonongeni pamodzi ndi iwo pakuti inu munaonetsa kukoma mtima kwa Aisraeli onse pamene ankatuluka mʼdziko la Igupto,” Choncho Akeni anachoka pakati pa Aamaleki.
Sawl ni Ken taminaw koe, tâcawt awh haw. Amalek taminaw koehoi aloukcalah awm awh. Hottelah hoehpawiteh hmai na thet awh payon vaih. Bangkongtetpawiteh, Isarelnaw Izip ram hoi ka tâcawt e pueng na pahren awh, telah ati. Ken taminaw teh Amaleknaw koehoi a tâco awh.
7 Tsono Sauli anakantha Aamaleki kuchokera ku Havila mpaka ku Suri, kummawa kwa Igupto.
Sawl ni Amaleknaw teh Havilah hoi Izip kanîtholah kaawm e Shur kho totouh a thei awh.
8 Sauli anatenga Agagi mfumu ya Aamaleki, koma anthu ake onse anawapha ndi lupanga.
Amalek siangpahrang Agag hai a hring lah a hlung awh teh, a man e pueng tahloi hoi be a thei.
9 Koma Sauli ndi ankhondo ake sanaphe Agagi, sanaphenso nkhosa ndi ngʼombe zabwino ngakhalenso ana angʼombe ndi ana ankhosa onenepa. Chilichonse chimene chinali chabwino sanachiphe. Koma zonse zimene zinali zoyipa ndi zachabechabe anaziwononga.
Hatei Sawl hoi taminaw ni Agag teh a hlung awh teh, tu kahawi e maito kahawi e kathâw e tuca kathâwnaw hoi kahawi e pueng thei han ngai awh hoeh. Ka cungkeihoeh e, hnephnap e naw teh he a thei awh.
10 Kenaka Yehova anawuza Samueli kuti,
BAWIPA e lawk Samuel koe a pha teh,
11 “Ine ndikumva chisoni chifukwa ndinayika Sauli kukhala mfumu. Wabwerera mʼmbuyo, waleka kunditsata ndipo sanamvere malangizo anga.” Samueli anapsa mtima, ndipo analira kwa Yehova usiku wonse.
Sawl siangpahrang lah ka tawn e pan ka kângai. Ahni teh kaie ka hnuk a kâbangnae koehoi bout a kamlang toe. Kaie kâpoelawknaw hah tawk hoeh toe telah ati teh Samuel ni a lungkhuek teh BAWIPA koe a lungmathoe laihoi karum khodai a hram.
12 Samueli anadzuka mmamawa ndipo anapita kukakumana ndi Sauli. Koma anthu anamuwuza kuti, “Sauli anabwera ku Karimeli, ndipo kumeneko wadziyimikira mwala wachikumbutso cha iye mwini. Tsopano wachokako ndipo wapita ku Giligala.”
Samuel ni Sawl kâhmo hanelah amom a thaw navah, Sawl teh Karmel kho lah a cei, haw vah pahnim hoeh nahan talung a ung hnukkhu bout a ban. Pou a cei teh Gilgal kho lah pou a ceicathuk telah Samuel koe a dei pouh awh.
13 Samueli atamupeza Sauli, Sauliyo anati kwa Samueli, “Yehova akudalitseni! Ndachita zonse zimene Yehova analamula.”
Samuel Sawl koe a cei teh Sawl ni BAWIPA ni yawhawi na poe e lah na o. BAWIPA e kâpoelawk pueng be ka tarawi telah a ti.
14 Koma Samueli anati, “Nanga bwanji ndikumva kulira kwa nkhosa ndi ngʼombe?”
Samuel ni hah pawiteh kaie ka hnâ dawk hram pawlawk ka thai e maito parawng lawk hah teh bangtelah atipouh.
15 Sauli anayankha, “Zimenezi Asilikali azitenga kuchokera kwa Aamaleki. Iwo anasungako nkhosa ndi ngʼombe zabwino kuti akapereke nsembe kwa Yehova Mulungu wanu, koma zina zonse anaziwononga.”
Sawl ni Amaleknaw koe e hetnaw ka la toe. Bangkongtetpawiteh BAWIPA na Cathut koehoi thuengnae sak nahanelah taminaw ni tu kahawi maito kahawi kahawi a pâhlung awh e doeh, alouknaw teh koung ka thei awh telah a ti.
16 Koma Samueli anati kwa Sauli, “Khala chete! Ima ndikuwuze zimene Yehova wandiwuza usiku wathawu.” Sauli anayankha kuti, “Ndiwuzeni.”
Samuel ni Sawl koevah awm ei, paduem tangmin BAWIPA ni kai koe a dei e na dei pouh han atipouh, Sawl ni dei haw atipouh.
17 Apo Samueli anati, “Munali wamngʼono pa maso pa anthu, koma tsopano mwasanduka mtsogoleri wa mafuko a Israeli. Yehova anakudzozani kuti mukhale mfumu yolamulira Aisraeli.
Samuel ni nange na hmunae lah tami ka thoungca nakunghai, Isarel miphunnaw e lû lah na awm hoeh namaw. Isarel siangpahrang lah BAWIPA ni satui na awi e nahoehmaw.
18 Ndipo Yehova anakutumani kuti, ‘Pitani mukawononge kwathunthu Aamaleki, anthu oyipa aja. Mukachite nawo nkhondo mpaka kuwatheratu.’
BAWIPA ni na patoun teh, cet nateh tamikayon Amaleknaw hah be thet lawih, he kahma hoehroukrak thet lawih telah ati nahoehmaw.
19 Chifukwa chiyani simunamvere mawu a Yehova? Chifukwa chiyani munathamangira zofunkha ndi kuchita choyipira Yehova?”
Bangkongmaw BAWIPA e lawk na ngâi laipalah hnopai na lawp teh BAWIPA mithmu hno kahawihoeh na sak telah atipouh.
20 Koma Saulo anawuza Samueli kuti, “Ine ndinamveradi mawu a Yehova. Ndinapita kukachita zimene Yehova anandituma. Ndinabwera naye Agagi, mfumu ya Amaleki, koma Aamaleki ena onse anaphedwa.
Sawl ni Samuel koevah BAWIPA e lawk atangcalah ka tarawi toe. BAWIPA ni na patoun e thaw ka tawk teh Amalek siangpahrang Agag ka thokhai teh, Amalek taminaw he ka pâmit.
21 Koma pa zofunkhazo anthu anatengapo nkhosa, ngʼombe ndi zabwino zina zoyenera kuwonongedwa kuti akapereke ngati nsembe kwa Yehova Mulungu wanu ku Giligala.”
Taminaw ni BAWIPA na Cathut Koe gilgal kho dawk thueng nahane lawp e hno thung dawk hoi maito, tunaw kahawipoung e ka la toe telah a dei.
22 Koma Samueli anayankha kuti, “Kodi Yehova amakondwera ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zina kapena kumvera mawu a ake? Taona, kumvera ndi kwabwino kuposa nsembe, ndipo kutchera khutu ndi kwabwino kuposa kupereka mafuta a nkhosa.
Samuel ni BAWIPA lawkngainae dawk a lunghawi e patetlah hmaisawi thuengnae dawk a lunghawi han na ou, thai haw lawkngainae teh thuengnae hlak ahawihnawn. Tarawinae teh tu kathâw hlak hoe ahawihnawn.
23 Pakuti kuwukira kuli ngati tchimo lowombeza, ndipo kukhala nkhutukumve kuli ngati tchimo lopembedza mafano. Chifukwa mwakana mawu a Yehova. Iyenso wakukana kuti iweyo ukhale mfumu.”
Lawkeknae teh taân sin e patetlah thoseh, lungpatanae teh meikaphawk bawknae patetlah thoseh yonnae kalenpounge doeh. BAWIPA e lawk na pahnawt dawkvah, BAWIPA ni hai siangpahrang lah na onae koehoi na pahnawt toe telah atipouh.
24 Tsono Sauli anati kwa Samueli, “Ine ndachimwa. Ndaphwanya malamulo a Yehova ndiponso malangizo anu. Ndinkaopa anthu ndipo ndinawamvera.
Sawl ni Samuel koevah yonnae ka sak katang toe. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA kâpoelawk hai ka ek toe. Bangkongtetpawiteh, tamimaya ka taki dawkvah a lawk ka ngâi pouh toe.
25 Tsopano ndikukupemphani, khululukireni tchimo langa ndipo mubwerere nane kuti ndikapembedze Yehova.”
Hatdawkvah na pahren nateh ka yonnae ngaithoum haw, BAWIPA ka bawk thai nahanlah bout na bankhai loe atipouh.
26 Koma Samueli anawuza Sauli kuti, “Ine sindibwerera nawe. Inu mwakana mawu a Yehova. Choncho Iyenso wakukanani kuti musakhale mfumu yolamulira Aisraeli.”
Hatei Samuel ni Sawl koevah, na bankhai mahoeh. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA e lawk na pahnawt toe. BAWIPA ni hai Isarel siangpahrang dawk hoi na pahnawt toe atipouh.
27 Samueli akutembenuka kuti azipita, Sauli anagwira mpendero wa mkanjo wake, ndipo unangʼambika.
Samuel a cei hane a kamlang navah, Sawl ni a hni a kuet pouh teh a pawi a kâphi.
28 Samueli anati kwa iye, “Yehova wangʼamba ufumu wanu kuchoka kwa inu, ndipo waupereka kwa mnzanu woposa inu.
Samuel ni sahnin vah nang koehoi BAWIPA ni Isarel uknaeram a ravei toe. Nang hlak kahawi e na imri hah a poe toe.
29 Mulungu wa ulemerero wa Israeli sanama kapena kusintha maganizo ake; pakuti iye si munthu, kuti asinthe maganizo ake.”
Isarel miphun e pou kacakpounge BAWIPA teh a laithout hoeh. A lung hai kâthung hoeh a lungkâthung e tami patet nahoeh telah a ti.
30 Sauli anati, “Ine ndachimwa. Komabe, chonde mundilemekeze pamaso pa akuluakulu, anthu anga, ndiponso pamaso pa Israeli. Mubwerere nane kuti ndikapembedze Yehova Mulungu wanu.”
Sawl ni ka yon toe. Hateiteh pahren lahoi ka tami kacuenaw e hmalah hoi Isarel hmalah atu barinae na poe haw, BAWIPA na Cathut ka bawk thai nahan na bankhai haw, hottelah a kâhei.
31 Pamenepo Samueli anabwerera ndi Sauli, ndipo Sauli anapembedza Yehova.
Samuel ni Sawl a bankhai teh Sawl ni BAWIPA a bawk.
32 Kenaka Samueli anati, “Bwera nayeni kuno Agagi, mfumu ya Amaleki ija.” Choncho Agagi anapita kwa Samueli mokondwa chifukwa ankaganiza kuti, “Ndithu zowawa za imfa zapita.”
Samuel ni Amalek siangpahrang Agag teh kai koe thokhai awh haw telah ati. Hatnavah Agag teh kâhruetcuet lahoi a cei. Agag ni duenae kakhat e teh ka tapoung toe a ti.
33 Koma Samueli anati, “Monga momwe lupanga lako linasandutsira amayi kukhala wopanda ana, momwemonso amayi ako adzakhala opanda mwana pakati pa amayi.” Ndipo Samueli anapha Agagi pamaso pa Yehova ku Giligala.
Hatei Samuel ni na tahloi ni napuinaw ca sak apout sak e patetlah na manu hai napui thung dawk ca ka tawn hoeh e lah ao van han telah ati. Samuel ni Agag hah Gilgal vah BAWIPA hmalah tawntarawn lah a tâtueng.
34 Ndipo Samueli anapita ku Rama, koma Sauli anapita ku mudzi kwawo ku Gibeya wa Sauli.
Samuel teh Ramah kho vah a cei teh Sawl teh, Gibeah kho ama im vah a cei takhang.
35 Samueli sanamuonenso Sauli mpaka imfa yake ngakhale kuti ankamulira Sauliyo. Yehova anamva chisoni kuti anasankha Sauli kuti akhale mfumu ya Israeli.
Sawl a due totouh Samuel ni bout hloe hoeh toe. Hatei Samuel ni Sawl kong dawk a lungmathoe. BAWIPA teh Isarel siangpahrang lah Sawl a rawi e pan a kângai.

< 1 Samueli 15 >