< 1 Samueli 12 >

1 Pambuyo pake Samueli anawuza Aisraeli onse kuti, “Ine ndamvera zonse zimene munandiwuza ndipo ndakupatsani mfumu kuti izikulamulirani.
Şamuelee İzrailybışde gırgıng'uk'le eyhen: – Haane, zı şu eyhençil k'ırı alixhxhı şos paççah gixhxhına.
2 Tsopano muli ndi mfumu imene izikutsogolerani, koma ine ndakalamba, kumutu kwanga kuli imvi zokhazokha ndipo ana anga ali pamodzi ndi inu. Ndakhala ndili mtsogoleri wanu kuyambira ndili mnyamata mpaka lero.
Həşde şoqa vuşda paççah vor, zımee q'əs qıxha, ç'ərbı cagvara qeetxha. Yizın dixbımee şoka vob. Zı cehilyranang'ançile g'iyniyne yiğılqamee vuşde ögee ark'ın.
3 Ine ndili pano. Ngati ndinalakwa chilichonse nditsutseni pamaso pa Yehova ndi wodzozedwa wake. Kodi ndinalanda ngʼombe ya yani? Kodi ndinalanda bulu wa yani? Kodi ndani amene ndinamudyera masuku pa mutu? Kodi ndinazunza yani? Kodi ndinalandira kwa yani chiphuphu choti nʼkundidetsa mʼmaso? Ngati ndinachita chilichonse cha izi, ine ndidzakubwezerani.”
G'iyna zı vuşde ögil ulyorzuling'a, şu zak'le eyhelan, zı şavna yatsne, əməlene alyapt'ı? Vuşune zı horç'un? Vuşuyiy zı azırda hı'ı? Şavuke pıl alyaat'uye, mang'une pisde işilqa ul gyapxı? Rəbbineyiy Mangv'ee g'əyxı'ne paççahne ögee, yizde aq'veeqa aqqe. Zı şoke alyat'uyn sak'al ha'as.
4 Iwo anayankha kuti, “Inu simunatidyere masuku pamutu kapena kutizunza. Simunalande kanthu kalikonse ka munthu.”
Manbışe mang'us inəxüd alidghıniy qele: – Ğu şi mısacab hopç'un deş, azırbab g'alyav'uynbı deş, şavnecad xılençe vuççudud g'ayşuyn deş.
5 Samueli anawawuza kuti, “Yehova ndiye mboni pakati pa inu ndi ine, ndiponso wodzozedwa wake ndi mboni kuti lero simunapeze chilichonse mʼdzanja langa.” Iwo anati, “Inde, Yehova ndiye mboni.”
Şamuelee manbışik'le eyhen: – Şok'le g'iyna yizde aq'vee aqqasın vuççud ivdeeke ıxhay, Rəbbik'led, Mang'vee g'əyxı'yne paççahık'led g'acuyn. Manbışed «Ho'o, şaqa yiğne aq'vee aqqasın kar deşinva» eyhe.
6 Samueli anawawuzanso kuti, “Yehova ndiye amene anasankha Mose ndi Aaroni kuti atulutse makolo anu mʼdziko la Igupto.
Şamueleecad meed milletık'le eyhen: – Mane Rəbbee Haruniy Mısa g'əvxü, vuşun dekkarıb Misirğançe Mang'veecab qığav'u.
7 Nʼchifukwa chake tsopano imani pomwepa kuti ndikufotokozereni pamaso pa Yehova, za ntchito za chipulumutso zimene Yehova anachitira inu ndi makolo anu.
Həşde Rəbbine ögil ulyoozre. Zı şok'le Rəbbee şosiy vuşde dekkaaşis hav'una yugvalla eyhes, mana vuşde aq'val avqas.
8 “Yakobo atapita ku dziko la Igupto, Aiguptowo akuwazunza, iwo analirira kwa Yehova kuti awathandize, ndipo Yehova anatumiza Mose ndi Aaroni, amene anatulutsa makolo anu mʼdziko la Igupto ndi kudzawakhazika pa malo ano.
Yaaq'ub Misireeqa qarayle. Qiyğa mang'uke g'abıynbışilqa Misirbışe yiğbı examee, manbışe Rəbbilqa xıleppı aaqa. Rəbbeeyib, Haruniy Mısa vuşun dekkar Misirğançe qığav'u, inyaqa qavaalesva g'uxoole.
9 “Koma iwo anayiwala Yehova Mulungu wawo, choncho Yehova anawapereka mʼdzanja la Sisera mkulu wa ankhondo wa mzinda wa Hazori, ndiponso mʼmanja mwa Afilisti ndi mfumu ya Mowabu. Mafumu onsewa anathira nkhondo makolo anu.
Manbışemee Rəbb, cona Allah, yik'el hixan ha'a. Rəbbeeyib manbı Xatsorne g'oşunne xərıng'une Sisrayne, Moavne paççahne sayib Filiştinaaşde xılyaqa qoole. Manbışe vuşde dekkaaşika dəv'ə haa'a.
10 Tsono iwo analira kwa Yehova nati, ‘Ife tachimwa, chifukwa tamusiya Yehova ndi kumatumikira mafano a Baala ndi Asiteroti. Koma tsopano tilanditseni mʼmanja mwa adani athu ndipo tidzakutumikirani.’
Manke milletın gyaaşe-gyaaşe Rəbbilqa xıleppı aaqı, eyhen: «Rəbb, şi Ğu yik'el hixan hı'ı, Ba'aliy Aştoret donane byuttyaaşis ı'bəədat hı'ı, bınah hav'u. Ğu şi həşde duşmanaaşine xılençe g'attivxhan hav'uynxhiy, şi Vas ı'bəədat ha'ayiy».
11 Choncho Yehova anatumiza Yeru-Baala, Bedani, Yefita ndi Samueli ndipo anakulanditsani mʼmanja mwa adani anu amene anakuzungulirani, kotero munakhala mwamtendere.
Rəbbeeyib manke Yerubba'al, Bedan, İftah, Şamuel g'uxoole. Şu nişilecab qı'məəq'ənceva Mang'vee şu məxüb hiqiy-allane duşmanaaşine xılençe g'attivxhan haa'a.
12 “Koma mutaona kuti Nahasi mfumu ya Amoni inkabwera kudzamenyana nanu, inu munandiwuza kuti, ‘Ayi, ife tikufuna mfumu kuti itilamulire,’ ngakhale kuti Yehova Mulungu wanu ndiye anali mfumu yanu.
Şok'le Ammonbışda paççah, Naxaş, şolqa ı'qqə g'acumee, vuşda paççah Rəbb Allah ıxhayka, şu ilydyaakkı, zak'le uvhuyn: «De'eş, şaqa yişda paççah ıxha ıkkan».
13 Tsopano nayi mfumu imene mwayisankha, imene munayipempha. Onani, Yehova wakupatsani mfumu.
Haane şos ıkkiykın, şu g'əyxı'na paççah. İlyaake Rəbbee şos paççah gixhxhına.
14 Ngati muziopa Yehova ndi kumamutumikira ndi kumamumvera, osamupandukira ndiponso ngati inu pamodzi ndi mfumu yanu mudzatsata Yehova Mulungu wanu, ndiye zinthu zonse zidzakuyenderani bwino.
Rəbbile qəpq'ı'n Mang'us ı'bəədat he'eene, Mang'vee eyhençil k'ırıbı alixhxhı, Mang'une əmrbışeençe qığdepç'eene, şunab şol oğa gixhxhına paççahır vuşde Allahee, Rəbbee, eyhençika gyuv'ur oza qeepxheene, geed yugda ixhes!
15 Koma mukapanda kumvera Yehova ndi kumupandukira, ndiye adzakulangani pamodzi ndi mfumu yanu yomwe.
De'eş, şu Rəbbine cuvabıl k'ırı ilydiyxhı, Rəbbine əmreençe qığeepç'eene, nəxdiy Rəbbin xıl vuşde dekkaaşilqa satk'ıl, həməxdıd şolqad sak'alas.
16 “Tsono imani pomwepa kuti muone chinthu chachikulu chimene Yehova ali pafupi kuchita pamaso panu!
Həşdemee ulyobzur, Rəbbee vuşde ulene ögil haa'asde xənne işiqa ilyaake!
17 Kodi ino si nthawi yokolola tirigu? Komabe ndipemphera kwa Yehova kuti agwetse mvula ya mabingu. Zikatero mudzadziwa kuti tchimo lanu limene mwachita popempha mfumu kwa Yehova ndi lalikulu.”
G'iyna suk qiviyşalan yiğ dişde vod? Zı həşde Rəbbilqa xıleppı aaqı, Mang'uk'le xəybı g'əhətqe'eva, gyoğiy g'axıleva eyhes. Manke şok'lecad ats'axhxhesın, şos paççah heqqıyka, şu Rəbbine ögil nimeena bınahiy hav'uva.
18 Choncho Samueli anapemphera, ndipo Yehova anatumiza mvula ya mabingu tsiku lomwelo. Apo anthu aja anaopa kwambiri Yehova ndi Samueli.
Şamuelee Rəbbilqa ona'a, Rəbbeyid manecad yiğıl xəybı g'əhətqı'ı, gyoğiy gyoğa'a. Manke millet Rəbbiled, Şamueliled qətqı'niyn.
19 Tsono anamupempha Samueli nati, “Chonde mutipempherere kwa Yehova, ife atumiki kuti tingafe pakuti pa machimo athu onse tawonjezapo tchimo lopempha mfumu.”
Milletıncad Şamuelik'le eyhen: – Yişdemee, yiğne g'ulaaşinemee, yiğne Allahılqa, Rəbbilqa, düə hee'e, Mang'vee şi gimabat'acen. Şi yişde manisa bınahbışilqa, paççah heqqıyka sayıb hexxav'una.
20 Samueli anayankha kuti, “Musaope, inu mwachitadi tchimo ili, koma musaleke kumutsata Yehova ndi kumutumikira ndi mtima wanu wonse.
Şamuelemee milletık'le eyhen: – Qı'məəq'ən, şu mana bınah hav'u vuxheeyib, Rəbbile sivmiyk'al, Rəbbis ı'bəədat yik'eençe he'e.
21 Ndipo musatsate mafano achabechabe amene alibe phindu ndipo sangakupulumutseni popeza ndi achabechabe.
Nişiscad karaı'dəəne byutyaaşinemee, Rəbbile sivmiyk'al. Manbı nişiscad karaı'dəən karbı ıxhayke, mançisse şos nəxbınacab yugvallab haa'as vəəxəs deş, nişikecabıb g'attivxhan haa'as deş.
22 Yehova adzakana anthu ake kuopa kuti dzina lake lamphamvu linganyozeke, pakuti chinamukondweretsa Yehova kuti akusandutseni inu kukhala anthu ake.
Rəbbee Cune xənne doyunemee, şu dağaa'as deş. Rəbbis Cus ıkkiykın, şoke Cun millet hı'ı.
23 Ndiponso kunena za ine, zisachitike kuti ndichimwire Yehova pakulephera kukupemphererani. Ndipo ine ndidzakuphunzitsani njira yabwino ndi yolungama kuti muziyendamo.
Zalqa axvee, zı şol-alla düə hav'uy g'aleççes deş. Mançike zas Rəbbine ögil bınah vuxhes. Zı şos yugna, qopkuna yəq haagvas.
24 Koma onetsetsani kuti mukuopa Yehova ndi kumutumikira mokhulupirika ndi mtima wanu wonse. Nthawi zonse muziganizira zinthu zazikulu wakhala akukuchitirani.
Saccu Rəbbile qəvəq'ne, Mang'us gırgıne gahbışil yik'eençe ı'bəədat he'e. Yik'el aqqe, Rəbbee vuşdemee nəxdın ç'ak'ın işbı hı'ı ıxhay.
25 Komabe mukapitirira kuchita zoyipa, ndiye kuti inu pamodzi ndi mfumu yanu mudzachotsedwa.”
Şu pisvalybışike xıl ts'its'dyav'eene, şunab, vuşda paççahır ç'iyene aq'vayle havaakal haa'asınbı.

< 1 Samueli 12 >