< 1 Mafumu 13 >
1 Ndipo taonani, munthu wa Mulungu wochokera ku Yuda anapita ku Beteli molamulidwa ndi Yehova. Nthawi imeneyo nʼkuti Yeroboamu atayimirira pambali pa guwa akufukiza lubani.
Ie amy zao nihirike e Iehoda ty ondatin’ Añahare, ami’ty tsara’ Iehovà, mb’e Betele mb’eo; ie nijohañe marine’ i kitreliy t’Iarovame hañemboke.
2 Mneneriyo anatemberera guwalo mofuwula potsata mawu a Yehova nati: “Guwa iwe, guwa iwe! Yehova akuti, ‘Taonani mʼbanja la Davide mudzabadwa mwana dzina lake Yosiya. Pa iwe, iyeyo adzaperekapo ngati nsembe, ansembe otumikira ku malo achipembedzo amene tsopano akufukiza lubani pa iwe, ndipo pa iwe adzatenthapo mafupa a anthu.’”
Le nikoihe’e amy kitreliy ty tsara’ Iehovà, ami’ty hoe: Ry kitrely, kitrely, hoe t’Iehovà: Maharendreha te hasamak’ añ’ anjomba’ i Davide ty ana-dahy; Iosià ty tahina’e; le ama’o ty hisoroña’e o mpisoron-toets’ abo misoroñe ama’oo le haforehetse ama’o eo ty taola’ondaty.
3 Tsiku lomwelo munthu wa Mulungu uja anapereka chizindikiro ichi: “Chizindikiro chimene Yehova wanena ndi ichi: Taonani guwali lidzangʼambika pakati ndipo phulusa lili pamenepo lidzamwazika.”
Nanolo-biloñe ka re amy andro zay, ami’ty hoe: Zao ty viloñe nitsarà’ Iehovà; Inao! ho riateñe o kitrelio vaho hadoañe ty lavenok’ ama’e.
4 Mfumu Yeroboamu atamva zimene munthu wa Mulungu ananena motemberera guwa lansembe ku Beteli, anatambasula dzanja lake ali ku guwako ndipo anati, “Mugwireni!” Koma dzanja limene anatambasula kuloza munthu wa Mulunguyo linawuma kuti gwaa, kotero kuti sanathenso kulibweza.
Aa ie jinanji’ i mpanjakay ty saontsi’ indatin’Añaharey, i nikoiha’e amy kitreli’ i Beteleiy, le natora-kitsi’ Iarovame boak’ amy kitreliy ty fità’e nanao ty hoe: Fihino re. Fe niforejeje i sirañe natora-kitsi’ey, le tsy nahafitarik’ aze mb’ ama’e.
5 Nthawi yomweyo guwa lija linangʼambika pakati ndipo phulusa lake linamwazika molingana ndi chizindikiro chimene munthu wa Mulungu anapereka potsata mawu a Yehova.
Nidreatse ka i kitreliy naho nidoañe boak’amy kitreliy o laveno’eo ty amy viloñe nitaroñe’ indatin’ Añaharey tie nitsara’ Iehovày.
6 Pamenepo mfumu inati kwa munthu wa Mulunguyo, “Undipempherere kwa Yehova Mulungu wako kuti andikomere mtima ndipo undipempherere kuti dzanja langa lichire.” Choncho munthu wa Mulungu anapempha kwa Yehova, ndipo dzanja la mfumu linachiritsidwa nʼkukhala ngati momwe linalili kale.
Aa le hoe ty natoi’ i mpanjakay am’ indatin’ Añaharey: Mihalalia am’ Iehovà Andrianañahare’o ho ahiko, misolohoa ho ahy hañereña’e ty sirako. Aa le nihalaly am’ Iehovà indatin’ Añaharey naho niareñe ty fità’ i mpanjakay vaho nibalike ho amy do’e taoloy.
7 Mfumu inati kwa munthu wa Mulunguyo, “Tiye kwathu kuti ukadye chakudya, ndipo ndidzakupatsa mphatso.”
Aa hoe i mpanjakay am’ indatin’ Añaharey; Mihova amako ao, hanintsiña’o, le ho tolorako ravoravo.
8 Koma munthu wa Mulunguyo anayankha mfumu kuti, “Ngakhale mutandipatsa theka la chuma chanu, sindingapite nanu, kapena kudya chakudya, kapenanso kumwa madzi kuno.
Le hoe t’indatin’Añahare amy mpanjakay: Ndra te natolo’o ahy ty an-tsasa’ i anjomba’oy, tsy ho nindrezako vaho tsy ho nihinañe mofo ndra rano ami’ ty toetse toy.
9 Pakuti Yehova anandilamula kuti, ‘Usakadye chakudya kapena kumwa madzi kapena kubwerera podzera njira imene unayendamo kale.’”
Amy te nafanto’ i tsara’ Iehovày amako ty hoe: Ko mikama mofo ndra rano vaho ko mimpoly mb’amy lalañe nimbà’o mb’eoy.
10 Choncho munthu wa Mulunguyo anadzera njira ina ndipo sanatsate njira imene anayendamo pobwera ku Beteliko.
Aa le nionjomb’ an-dalan-kafa mb’eo re, tsy nimpoly mb’amy lalañe nionjona’e mb’e Betele mb’eoy.
11 Tsono ku Beteli kunkakhala mneneri wina wokalamba. Mmodzi mwa ana ake anamufotokozera zonse zomwe munthu wa Mulungu anachita kumeneko tsiku limenelo. Anawuzanso abambo ake zimene ananena kwa mfumu.
Ie amy zao nimoneñe e Betele ao ty androanavy mpitoky; le niheo ama’e mb’eo ty ana’e raik’ nitalily ze hene fitoloñañe nanoe’ indatin’ Añaharey e Betele ao; naho nitalilie’ iereo an-drae’ iareo ka i lañonañe sinaontsi’e amy mpanjakaiy.
12 Abambo awo aja anawafunsa kuti, “Kodi wadzera njira iti?” Ana akewo anamufotokozera njira imene munthu wa Mulungu wochokera ku Yudayo anadzera.
Le hoe ty nanoen-drae’ am’iareo; Nimb’aia re? Toe nitrea’ o ana’eo ty lala’ nomba’ indatin’ Añahare hirik’e Iehoday.
13 Ndipo abambo aja anati kwa ana akewo, “Mangireni chishalo pa bulu.” Anawo atamangirira chishalo pa bulu, nkhalambayo inakwera buluyo
Le hoe re amo ana-dahi’eo: Adiaño ho ahy i borìkey. Aa le nidiañe’ iereo i borìkey naho niningira’e;
14 ndipo inalondola munthu wa Mulunguyo. Inamupeza atakhala pansi pa mtengo wa thundu ndipo inamufunsa kuti, “Kodi ndiwe munthu wa Mulungu amene anabwera kuchokera ku Yuda?” Munthuyo anayankha kuti, “Inde, ndineyo.”
vaho niheañe’e indatin’ Añaharey, le nitendrek’ aze niambesatse ambane’ ty kobaiñe eo, vaho nanoa’e ty hoe: Ihe hao indatin’Añahare boake Iehoday? Le hoe re, Ie.
15 Choncho mneneri wokalambayo anati kwa iye, “Tiye kwathu kuti ukadye chakudya.”
Aa le hoe re tama’e, Molia mb’amako vaho mikamà mofo.
16 Munthu wa Mulungu uja anati, “Sindingabwerere nanu kapena kudya chakudya kapenanso kumwa madzi kuno.
Le hoe re: Tsy hindre himpoly ama’o iraho, vaho tsy hitraofako lia; mbore tsy hiharo hihinañe mofo ndra hinon-drano ama’o an-toetse atoy.
17 Pakuti ndawuzidwa ndi Yehova kuti, ‘Usadye chakudya kapena kumwa madzi kumeneko kapenanso kubwerera poyenda njira imene unayendamo popita.’”
Fa hoe ty tsara’ Iehovà nitsaraeñ’ amako: Tsy hikama mofo ndra hikama rano ao irehe, ndra mimpoly amy lalañe nionjona’o mb’eoy.
18 Mneneri wokalambayo anayankha kuti, “Inenso ndine mneneri ngati iwe. Ndipo mngelo wa Yehova anayankhula nane mawu a Yehova kuti, ‘Kamubweze abwere ku nyumba yako kuti akadye chakudya ndi kumwa madzi.’” Koma anamunamiza.
Le hoe re ama’e: Mpitoky manahak’ azo ka ‘ni-raho; le nitsara amako ty anjely amy tsara’ Iehovày, ty hoe: Ampolio mb’añ’ anjomba’o mb’eo re hikama mofo naho hinon-drano; inay ty lañi’e.
19 Choncho munthu wa Mulungu uja anabwerera naye ndipo anakadya ndi kumwa madzi mʼnyumba mwake.
Aa le nindreza’e fimpoly, nikama mofo naho ninon-drano.
20 Ali pa tebulo, Yehova anayankhula ndi mneneri wokalambayo amene anamubweza munthu wa Mulunguyo.
Ie niambesatse am-pandambañañe eo, le niheo amy mpitoky ninday aze noliy ty tsara’ Iehovà.
21 Iye anafuwulira munthu wa Mulungu wochokera ku Yudayo kuti, “Yehova akuti, ‘Iwe wanyoza mawu a Yehova ndipo sunasunge lamulo limene Yehova Mulungu wako anakupatsa.
Le napaza’e ty hoe am’ indatin’ Añahare hirik’e Iehoday, Hoe ty nafè’ Iehovà; Amy te ihe nanjehatse i falie’ Iehovày, naho tsy nambena’o i fañè nafanto’ Iehovà Andrianañahare’oy,
22 Iwe wabwerera ndi kudya chakudya ndiponso kumwa madzi ku malo amene Iye anakuwuza kuti usadye chakudya kapena kumwa madzi. Choncho mtembo wako sadzawuyika mʼmanda a makolo ako.’”
te mone nibalike naho nikama mofo vaho ninon-drano an-toetse nitsarae’e ty hoe: Ko mikama mofo naho ko minon-drano; le tsy higodañe an-kiborin-droae’o ao ty fañova’o.
23 Munthu wa Mulungu atatha kudya ndi kumwa, mneneri amene anamubweza uja anamangirira chishalo pa bulu wa munthu wa Mulunguyo.
Aa ie amy zao, naho fa nikama mofo naho ninon-drano, le nadia’e ho aze i borìke’ey, ho a i mpitoky nampihovae’ey.
24 Akupita, anakumana ndi mkango pa msewu ndipo unamupha, mtembo wake unagwera pansi pa msewu, bulu uja anayima pambali pake ndipo mkango unayima pafupi ndi mtembowo.
Aa ie nienga mb’eo, nitendreke liona nanjevoñ’ aze, ie nañifike i fañova’ey an-dalañey; nitsangañe añ’ila’e eo i borìkey, vaho nijohañe marine’ i fañovay i lionay.
25 Ndipo taonani, anthu ena amene ankapita mu msewumo anaona mtembowo uli pansi potero, mkango utayima pa mbali pa mtembo uja ndipo anapita nakafotokozera anthu mu mzinda umene mumakhala mneneri wokalamba uja.
Inge amy zao ondaty niary eio, ie niisa’ iareo i fañova navokovoko an-dalañey, naho i liona nijagarodoñe marine’ i fañovaiy, le nimb’eo nitalily an-drova nimoneña’ i androanavy mpitokiy.
26 Mneneri amene anamubweza mnzake ku njira uja atamva zimenezi, anati, “Ameneyo ndi munthu wa Mulungu amene wanyoza mawu a Yehova. Yehova wamupereka kwa mkango umene wamukhadzula ndi kumupha, monga momwe Yehova anamuchenjezera.”
Aa ie jinanji’ i mpitoky ninday aze moly boak’ amy lalañeiy, le hoe ty asa’e: Ie t’indatin’ Añahare nanjehatse i tsara’ Iehovày, toly ndra natolo’ Iehovà amy lionay, nirimite’e naho vinono’e ty amy tsara’ Iehovà nafe’e ama’ey.
27 Mneneri wokalambayo anati kwa ana ake, “Mundimangire chishalo pa bulu,” ndipo anaterodi.
Aa hoe ty natao’e amy ana’e rey: Diaño ho ahy i borikey. Aa le nidiañe’ iereo.
28 Ndipo anapita, nakapezadi mtembo utagwera pansi mu msewu, bulu pamodzi ndi mkango atayima pambali pake. Koma mkangowo sunadye mtembowo kapena kukhadzula buluyo.
Ie nimb’eo le nanjo i fañovay te nahifik’ an-dalañe eo, naho i borìkey, vaho i liona nijohañe marine’ i fañovaiy. Tsy nihane’ i lionay i fañovay vaho tsy nirimite’e i borìkey.
29 Choncho mneneri wokalambayo anatenga mtembo wa munthu wa Mulunguyo, nawuyika pa bulu, ndipo anabwera nawo ku mzinda kuti alire maliro ndi kuyika mtembowo mʼmanda.
Rinambe’ i mpitokiy ty fañova’ indatin’ Añaharey, le nasampe’e amy borìkey, vaho nendese’e nibalike mb’eo; ie nivotrak’ an-drova’ i androanavy mpitokiy, le nandala naho nandentek’ aze.
30 Tsono anayika mtembowo mʼmanda amene mneneri wokalamba uja anadzikonzera, ndipo anamulira pomanena kuti, “Mʼbale wanga ine! Mʼbale wanga ine!”
Natsalalampa’e amy kibori’ey i fañova’ey; le nandala’ iareo ami’ty hoe: Hoke, ry rahalahiko!
31 Atamuyika mʼmanda, iye anati kwa ana ake, “Ine ndikafa, mudzandiyike mʼmanda amene munthu wa Mulungu wayikidwa. Mudzayike mafupa anga pambali pa mafupa ake.
Ie nandentek’ aze, le nafanto’e amy ana’e rey ty hoe, Naho mikenkan-draho, aleveño amy kibory nandentehañe indatin’ Añaharey; apoho marine’ o taola’eo o taolakoo.
32 Pakuti uthenga umene Yehova anamuyankhulitsa, wotsutsana ndi guwa lansembe la ku Beteli ndi nyumba zonse za chipembedzo za mʼmizinda ya ku Samariya, zidzachitika ndithu.”
Amy te tsy mete tsy hifetsake i tsara’ Iehovà nipazahe’e amy kitrely e Beteley naho amo fonga anjomba an-toets’ abo an-drova’ i Someroneo.
33 Ngakhale izi zinachitika, Yeroboamu sanasiye njira zake zoyipa, koma anasankhanso anthu wamba kukhala ansembe pa malo ake achipembedzo. Aliyense amene ankafuna kukhala wansembe iye anamupatula kukhala wansembe.
Ie añe, tsy nibalintoa amy sata-rati’ey t’Iarovame, fa nanoe’e mpisoroñe an-toets’ abo o boak’ am’ondaty tsotra iabio; toe noriza’e ho mpisoroñe an-toets’ abo ze hene nimete.
34 Limeneli ndiye linali tchimo la nyumba ya Yeroboamu limene linabweretsa kugwa kwake ndiponso chiwonongeko mʼdzikomo.
Ie nampanan-kakeo ty anjomba’ Iarovame, hañitoañe aze, naho hamongorañ’ aze ambone’ ty tane toy.