< 1 Mafumu 12 >
1 Rehobowamu anapita ku Sekemu, pakuti Aisraeli onse nʼkuti atapita kumeneko kukamulonga ufumu.
Aa le nomb’e Sekeme añe t’i Rekhavame, ie fa niheo mb’e Sekeme mb’eo t’Israele iaby hañory aze ho mpanjaka.
2 Yeroboamu mwana wa Nebati anamva zimenezi. Nthawi imeneyo nʼkuti Yeroboamuyo akukhala ku Igupto, pakuti atathawa Mfumu Solomoni iyeyo anakakhala ku Igupto.
Ie amy zao, naho jinanji’ Iarovame ana’ i Nebate e Mitsraime añe—ie fa nitriban-day boak’ añatrefa’ i Selomò mpanjaka vaho nimoneñe e Mitsraime añe
3 Tsono anthu anayitanitsa Yeroboamu, ndipo iye pamodzi ndi gulu lonse la ku Israeli anapita kwa Rehobowamu ndipo anamuwuza kuti,
le nañitrike naho nikoik’ aze iereo naho niheo mb’ amy Rekhavame mb’eo t’Iarovame rekets’ i valobohò’ Israeley, nanao ty hoe:
4 “Abambo anu anatisenzetsa goli lolemetsa kwambiri, koma inu chepetsani ntchito yowawa pa ife ndipo peputsani goli lolemetsa limene anatisenzetsa. Mukatero tidzakutumikirani.”
Nanoan-drae’o jokan-tsarererake; aa le hamaivaño ty fitoloñan-tsarererahan-drae’o, naho i joka mavesatse nampitarazoe’e anaiy, le hitoroñ’ azo zahay.
5 Rehobowamu anayankha kuti, “Pitani, ndipo pakatha masiku atatu, mudzabwerenso.” Choncho anthuwo anapitadi.
Le hoe re am’ iereo: Misitaha telo andro heike, le mibaliha amako. Le nienga ondatio.
6 Ndipo Mfumu Rehobowamu anapempha nzeru kwa akuluakulu amene ankatumikira Solomoni abambo ake pamene anali ndi moyo. Iye anawafunsa kuti, “Kodi mungandilangize zotani kuti ndiwayankhe anthu amenewa?”
Nisafiry amo androanavy nijohañe añatrefa’ i Selomò rae’e, ie mbe niveloñe, t’i Rekhavame, ami’ty hoe: Ino ty fanoroañe hatolo’ areo amako hamaleako ondatio?
7 Iwo anayankha kuti, “Ngati lero mudzakhala mtumiki wa anthu amenewa ndi kuwatumikira ndipo mukawayankha bwino, iwowo adzakhala atumiki anu nthawi zonse.”
Le hoe ty nisaontsia’ iareo: Naho toe ho mpitoro’ ondatio irehe te anito hitoroña’o naho hihaoña’o vaho hisaontsia’o mora, le ho mpitoro’o nainai’e iereo.
8 Koma Rehobowamu anakana malangizo amene akuluakuluwo anamupatsa ndipo anafunsira nzeru kwa anyamata anzake amene anakulira nawo limodzi omwe ankamutumikira.
Fe nifarie’e ty safiry natolo’ o androanavio aze, vaho nandrambe ty fanoroa’ o ajalahy nindre nibey ama’e naho nijohañe añatrefa’eo.
9 Iye anawafunsa kuti, “Kodi malangizo anu ngotani? Kodi ndiwayankhe chiyani anthu amene akunena kwa ine kuti, ‘Peputsani goli limene abambo anu anatisenzetsa’?”
Fa hoe re am’ iereo: Akore ty safiri’ areo, hamalean-tika ondaty nisaontsy amako ami’ty hoe: Hamaivaño ty joka nampitarazoen-drae’o anaio?
10 Anyamata anzake amene anakula nawo limodzi aja anamuyankha kuti, “Anthu amene ananena kwa iwe kuti, ‘Abambo anu anatisenzetsa goli lolemetsa, koma inu peputsani goli lathu,’ uwawuze kuti ‘Chala changa chakanise nʼchachikulu kupambana chiwuno cha abambo anga.
Aa le hoe ty asa’ o ajalahy nindre nibey ama’eo: Inao ty ho saontsie’o am’ondaty nisaontsy ama’o nanao ty hoe: Nanoen-drae’o mavesatse ty joka’ay, aa le hamaivaño ama’ay; Inao ty hilañona’o: Bey ta i fisafoan-draekoy ty anakikiko.
11 Abambo anga ankakusenzetsani goli lolemetsa koma ine ndidzachititsa kuti likhale lolemera kwambiri. Abambo anga ankakukwapulani ndi zikoti wamba koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.’”
Aa ndra t’ie nampijinien-draeko joka mavesatse, mbe ho tompeako ka o joka’ areoo; ie nandafa anahareo an-karavantsy, fa an-kalengo ka ty ihamofohako.
12 Patapita masiku atatu, Yeroboamu pamodzi ndi anthu onse anabwera kwa Rehobowamu, monga momwe inanenera mfumu kuti, “Mudzabwere pakatha masiku atatu.”
Aa le nomb’ amy Rekhavame amy andro fahateloy t’Iarovame rekets’ ondaty iabio, ty amy saontsi’ i mpanjakaiy, vaho nanao ty hoe: Mibaliha amako ami’ty andro fahatelo.
13 Mfumuyo inawayankha anthuwo mwankhanza. Kukana malangizo amene akuluakulu anayipatsa.
Le sinotra’ i mpanjakay ondatio, vaho napo’e i fanoroañe natolo’ o androanavioy;
14 Anatsatira malangizo amene anyamata anzake anamupatsa ndipo anati “Abambo anga ankakusenzetsani goli lolemetsa. Ine ndidzachititsa kuti likhale lolemera kwambiri. Abambo anga ankakukwapulani ndi zikoti wamba koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.”
fa i fanoroa’ o ajalahioo ty nilañonà’e ami’ty hoe: Nanoen-draeko mavesatse ty joka’ areo, fe ho tovoñako o joka’ areoo, nandafa anahareo an-karavantsy ty raeko f’ie ho fofoheko an-kalengo.
15 Choncho mfumu sinamvere pempho la anthuwo, pakuti zinthu izi zinali zochokera kwa Yehova, kukwaniritsa mawu amene Yehova anayankhula kwa Yeroboamu mwana wa Nebati kudzera mwa Ahiya wa ku Silo.
Aa le tsy hinao’ i mpanjakay ondatio; ie toe fandahara’ Iehovà, hampijadoñe i enta’ey, i tsinara’ Iehovà am-pità’ i Akià nte Silò am’ Iarovame, ana’ i Nebatey.
16 Aisraeli onse ataona kuti mfumu yakana kumva zopempha zawo, iwo anayankha mfumu kuti, “Kodi ife tili ndi gawo lanji mwa Davide, ndi gawo lanjinso mwa mwana wa Yese? Inu Aisraeli, bwererani ku matenti anu! Ziyangʼanira nyumba yako, Iwe Davide!” Kotero Aisraeli anachoka napita ku nyumba zawo.
Aa ie nioni’ Israele iaby te tsy nihaoñe’ i mpanjakay, le hoe ty natoi’ ondatio amy mpanjakay: Ino ty anay amy Davide ao? Aman-dova amy ana’ Isaý hao zahay? Akia mb’an-kivoho’ areo ry Israele! Hajario i akiba’oy ry Davide. Aa le niavotse mb’ an-kiboho’ iareo mb’eo t’Israele.
17 Koma Aisraeli amene ankakhala mʼmizinda ya Yuda ankalamuliridwa ndi Rehobowamu.
Fe mbe nifehe o ana’ Israele nimoneñe amo rova’ Iehodaoo t’i Rekhavame.
18 Mfumu Rehobowamu anatuma Adoramu amene ankayangʼanira ntchito yathangata, koma Aisraeli onse anamugeda ndi miyala mpaka kumupha. Koma Mfumu Rehobowamu anakwera msangamsanga galeta wake nathawira ku Yerusalemu.
Nirahe’ i Rekhavame mpanjaka mb’eo, t’i Adorame, mpifeleke ty haba; f’ie finetsa’ Israele iaby vato le nihomake vaho nipitsike mb’ an-tsarete’e añe t’i Rekhavame nitsondemboke mb’e Ierosalaime mb’eo.
19 Choncho Aisraeli akhala akuwukira nyumba ya Davide mpaka lero lino.
Aa le niola amy anjomba’ i Davidey t’Israele pake henane.
20 Aisraeli onse atamva kuti Yeroboamu wabwerera kuchokera ku Igupto, anatumiza mawu okamuyitana kuti abwere ku msonkhano ndipo anamuyika kukhala mfumu ya Aisraeli onse. Fuko la Yuda lokha ndi lomwe linkatsatira nyumba ya Davide.
Ie amy zao, naho jinanji’ Israele iaby te tafampoly t’Iarovame, le nampisangitrife’ iereo mb’am-pivori-bey vaho nanoe’ iereo mpanjaka’ Israele iaby; leo raike tsy nañorike ty anjomba’ i Davide naho tsy Iehodà avao.
21 Rehobowamu atafika ku Yerusalemu, anasonkhanitsa nyumba yonse ya Yuda ndi fuko la Benjamini, nasankha ankhondo okwanira 180,000, kuti akamenyane ndi nyumba ya Israeli kuti amubwezere Rehobowamu mwana wa Solomoni ufumu wake.
Aa ie niheo mb’e Ierosalaime mb’eo t’i Rekhavame, le hene natonto’e ty anjomba’ Iehoda naho ty fifokoa’ i Beniamine, lahindefoñe soa-joboñe rai-hetse-tsi-valo-ale, hialy amy anjomba’ Israeley, hampolia’e amy Rekhavame ana’ i Selomò i fifeheañey.
22 Koma Mulungu anayankhula ndi Semaya, munthu wa Mulungu kuti,
Fe niheo amy Semaià, ondatin’ Añahare, ty tsaran’ Añahare nanao ty hoe:
23 “Nena kwa Rehobowamu mwana wa Solomoni mfumu ya Yuda, kwa nyumba yonse ya Yuda ndi Benjamini, ndiponso kwa anthu ena onse kuti,
Saontsio t’i Rekhavame, ana’ i Selomò mpanjaka’ Iehoday naho i anjomba’ Iehoda naho Beniamine iabiy vaho o ila’ ondatio, ty hoe;
24 ‘Yehova akuti: Musapite kukamenyana ndi abale anu Aisraeli. Aliyense wa inu abwerere kwawo, pakuti zimenezi ndachita ndine.’” Choncho anthuwo anamvera mawu a Yehova ndi kubwerera kwawo, monga analamulira Yehova.
Hoe ty nafè’ Iehovà: Tsy hionjoñe mb’eo nahareo, tsy hialy amo ana’ Israele roahalahi’ areoo; songa mimpolia mb’an-kiboho’e añe, fa amako o raha zao. Aa le hinao’ iereo ty tsara’ Iehovà, vaho nimpoly, ty amy tsara’ Iehovày.
25 Tsono Yeroboamu anamanga mzinda wa Sekemu mʼdziko la mapiri la Efereimu ndipo anakhala kumeneko. Kuchokera kumeneko anapita kukamanga mzinda wa Penueli.
Namboare’ Iarovame am-bohibohi’ i Efraime ao t’i Sekeme, le nimoneñe ao; vaho niavotse ama’e namboatse i Penoele.
26 Yeroboamu anaganiza mu mtima mwake kuti, “Ndithu, ufumuwu udzabwereranso ku nyumba ya Davide.
Le hoe ty fitsakorean-tro’ Iarovame, Himpoly amy anjomba’ i Davidey henane zao i fifeheañey,
27 Ngati anthuwa azipitabe kukapereka nsembe ku Nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, adzayambanso kutsatira mbuye wawo Rehobowamu, mfumu ya Yuda. Adzandipha ndi kubwerera kwa Mfumu Rehobowamu.”
naho hionjomb’ amy anjomba’ Iehovà e Ierosalaimey ondatio hanao soroñe; le hitolik’ amy talè’ iareoy, homb’amy Rekhavame mpanjaka’ Iehoda ty arofo’ ondatio vaho havetra’ iareo iraho, ie himpoly mb’ an-dRekhavame mpanjaka’ Iehoda ao.
28 Itapempha nzeru, mfumuyo inapanga mafano awiri a ana angʼombe. Mfumuyo inati kwa anthuwo, “Mwakhala mukupita ku Yerusalemu nthawi yayitali. Iwe Israeli, nayi milungu yako imene inakutulutsa mʼdziko la Igupto.”
Aa le nisafiry i mpanjakay, naho nandranjy bania volamena roe, vaho nanao ty hoe am’ondatio, Loho sarotse ty fionjona’ areo mb’e Ierosalaime mb’eo: ingo o ‘ndrahare’oo ry Israele, o ninday azo boak’ an-tane Mitsraimeo.
29 Fano lina analiyika ku Beteli ndipo lina analiyika ku Dani.
Napo’e e Betele ao ty raike le napo’e e Dane ao ty raike.
30 Ndipo zimenezi zinachimwitsa anthu pakuti anthu ankapita mpaka ku Dani kukapembedza fano limene linali kumeneko.
F’ie toe hakeo; amy te nionjoñe hitalaho ami’ty raik’ ama’e ondaty pake Daneo.
31 Yeroboamu anamanga Nyumba za Mulungu pa malo azipembedzo nasankha ansembe kuchokera pakati pa anthu wamba, ngakhale sanali Alevi.
Namboara’e kijà ka o haboañeo, vaho boak’ am’ ondaty tsotra iabio ty nanoe’e mpisoroñe fa tsy amo ana’ i Levio.
32 Iye anakhazikitsa chikondwerero pa tsiku la 15 la mwezi wachisanu ndi chitatu, lofanana ndi tsiku la chikondwerero cha ku Yuda, ndipo ankapereka nsembe pa guwa. Izi ankachita ku Beteli, kupereka nsembe kwa ana angʼombe amene anapanga. Ndipo ku Beteliko anayikako ansembe pa malo achipembedzo amene anamanga.
Noriza’ Iarovame ty sabadidak’ ami’ty volam-paha-valo, ami’ty androm-paha-folo-lime ambi’ i volañey, hambañe amy sabadidake e Iehoday, ie nañenga amy kitreliy; izay ty e Betele ao, ie nanoa’e soroñe i bania namboare’e rey; vaho najado’e e Betele ao o mpisoro’ o toets’ abo namboare’eoo.
33 Tsiku la 15 la mwezi wachisanu ndi chitatu, mwezi umene anawusankha yekha, anapereka nsembe pa guwa limene analimanga ku Beteli. Motero anakhazikitsa chikondwerero cha Aisraeli ndipo iye ankapita kukapereka nsembe yofukiza lubani pa guwa.
Aa le niañambone mb’amy kitrely niranjie’e e Betele ao amy faha-folo-lime ambi’ i volam-paha-valoiy, i volañe nitsakorè’e an-tro’ey avao; le nañoriza’e sabadidake o ana’ Israeleo, vaho niañambone mb’amy kitrely fañemboha’ey.