< 1 Yohane 5 >
1 Aliyense amene amakhulupirira kuti Yesu ndi Khristu, iyeyo ndi mwana wa Mulungu, ndipo aliyense amene amakonda Atate amakondanso Mwana wake.
Wowoti wahuposhela uYesu uKiristi huje apepwe nungolobhe. Wowoti wagene huje afumile hwa Daada nantele abhagene abhana bhakwe.
2 Chodziwira kuti timakonda ana a Mulungu nʼchakuti timakonda Mulungu ndi kusunga malamulo ake.
Huhweli timenye huje tibhagene abhana bhangolobhe petuhugana ongolobhe nembombo zyakwe.
3 Pakuti kukonda Mulungu ndiye kusunga malamulo ake. Ndipo malamulo ake siwolemetsa,
Hwahuje petihugana Ongolobhe tibhomba nembombo zyakwe embombo zyakwe nyororo.
4 chifukwa aliyense amene ndi mwana wa Mulungu amagonjetsa dziko lapansi. Chikhulupiriro chathu ndicho timagonjetsera dziko lapansi.
Hwahuje wapepwe nu Ngolobhe aimenile eensi. Ohwo huimene huimene eensi ulweteshelo lwetu.
5 Ndani amagonjetsa dziko lapansi? Yekhayo amene amakhulupirira kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu.
Yonanu waimenile eensi? Yeyola wamweteshe huje Mwana wa Ngolobhe.
6 Uyu ndiye anabwera mwa madzi ndi magazi, ndiye Yesu Khristu. Sanabwere mwa madzi okha, koma mwa madzi ndi magazi. Ndipo ndi Mzimu Woyera amene akuchitira umboni, chifukwa Mzimu Woyera ndi choonadi.
Ono wahenzele humenze ni danda O Yesu U Kiristi. Sagaahenzele namenze gene ahenzele namenze ni danda.
7 Pakuti pali atatu amene amachitira umboni.
Hwahuje bhatatu bhabhayanga.
8 Mzimu Woyera, madzi ndi magazi; ndipo atatu amavomerezana.
Ompepo amenze nidanda ebha bhatatu bhahwetehana.
9 Timalandira umboni wa anthu, koma umboni wa Mulungu ndi wopambana. Umboniwo ndi umene anachitira Mwana wake.
Nkashile mtejezya usimishizwo gwabhantu usimishizwo ogwangolobhe gosi ashile ego. Hwahuje usimishizwo ogwa golobhe gwagogu huje alinagwo usimishizwo gwa Mwana wakwe.
10 Aliyense amene amakhulupirira Mwana wa Mulungu ali nawo umboniwu mu mtima mwake, koma aliyense amene sanakhulupirire Mulungu amayesa kuti Mulunguyo ndi wonama, chifukwa sanakhulupirire umboni umene Mulungu anachitira wa Mwana wake.
Ola wahuposhela Omwana wa Ngolobhe alinagwo usimishizwi mhati yakwe yuyo. Wowoti wasaga huposhela Ongolobhe ubheshe aje wilenga hwahuje sagaposheye usimishizwo ogwa Ngolobhe auletile ashilile Omwana wakwe.
11 Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
Usimishizwo gwa Ngolobhe atipiye owomi ogwa wila, owomi ogwo guli mhati ya Mwana wakwe. (aiōnios )
12 Iye amene ali ndi Mwana ali ndi moyo, amene alibe Mwana wa Mulungu alibe moyo.
Wali numwana wakwe ai nuwomi wasagali numwana owa Ngolobhe sagali nuwomi.
13 Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Embasimbiye ega mmanye huje mli nuwomi ogwo wila amwe mwemhutejezya hwitawa lya Mwana wa Ngolobhe. (aiōnios )
14 Ife timalimba mtima tikamafika pamaso pa Mulungu, popeza kuti ngati tipempha kanthu kalikonse monga mwa chifuniro chake, amatimvera.
Elitinalyo tibagaje hwitagalila lyakwe huje nkatilabhe ahatu hohoti shishiza mlugano lwakwe ahonvwa.
15 Ndipo ngati tikudziwa kuti amatimvera, chilichonse chimene timapempha, tikudziwanso kuti tili nacho chimene tamupempha Iye.
Nkashile timenye huje ontovwa hohoti hetihulabha timenye huje tilinalyo lyatilaabhile.
16 Ngati wina aona mʼbale wake akuchita tchimo losadzetsa imfa, apemphere ndipo Mulungu adzamupatsa moyo mʼbale wakeyo. Ndikunena za ochita tchimo losadzetsa imfa. Pali tchimo lodzetsa imfa. Ine sindikunena kuti apemphere ayi.
Nkashile omuntu alolile uwomba embibhi yasagahutwale afwe, hahwanziwa alabhe hwa Ngolobhe abhapele owomi. Iyanga nabhala embibhi zyawo saga ziwatwala afwe sayanga huje ahwaziwa alabhe humbibhi ezwo.
17 Chilichonse chosalungama ndi tchimo ndipo pali tchimo losadzetsa imfa.
Nkakosele embibhi hwahiye zihweli embibhi zyasaga zya aafwe.
18 Tikudziwa kuti aliyense amene ndi mwana wa Mulungu sachimwirachimwirabe. Yesu, Mwana wa Mulungu, amamusunga ndipo woyipa uja sangamukhudze.
Hwahuje wapepwe nu Ngolobhe saga bhabhomba embibhi. Wapepwe nu Ngolobhe, alelwa abhapinza wila nula ohwimbibhi hawezizye huvwalazye.
19 Tikudziwa kuti ndife ana a Mulungu ndi kuti dziko lonse lapansi lili pansi pa ulamuliro wa woyipayo.
Timenye huje ante tili bhana bhangolobhe ensi yonti pansi elogozya nuula obhibhi.
20 Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Hwahuje Omwana wa Ngolobhe ayezele atipiye enjele hwahuje timenye omwene lyoli, huyetili mhati yakwe umwene lyoli hwoyo Umwana wakwe uYesu Kiristi nu Ngolobhe uwelyoli nowomi weiwene. (aiōnios )
21 Ana okondedwa, dzisungeni bwino, osapembedza mafano.
Mubhana mwaganwa muhwiyetwe neshifwani.