< 1 Yohane 2 >

1 Inu Ana anga okondedwa, ndikukulemberani zimenezi kuti musachimwe. Koma wina akachimwa, tili nayo Nkhoswe yotinenera kwa Atate, Yesu Khristu, Wolungamayo.
Ka pahren e canaw, yonnae na sak awh hoeh nahanelah, hete ca hah ka thut teh na patawn awh. Tami buetbuet touh ni yonnae sakpayon pawiteh, maimouh na kampangkhai hanelah kalan e Bawipa Jisuh Khrih teh Pa koe ao.
2 Iyeyo ndiye nsembe yopepesera machimo athu, ndipo osati athu okha, komanso machimo onse a dziko lapansi.
Hote Bawipa teh maimae yon dueng nahoeh, talaivan pueng e yontha nahanelah, thueng e lah ao.
3 Ife timatsimikiza kuti tikumudziwa ngati tikusunga malamulo ake.
Hote Bawipa teh maimouh ni bangtelah hoi maw panue awh tetpawiteh, kâpoelawknaw hah tarawi e lahoi panue awh.
4 Munthu akamanena kuti, “Ine ndimadziwa Mulungu,” koma samvera malamulo a Mulunguyo, ndi wabodza ameneyo ndipo mwa iye mulibe choonadi.
Kâpoelawknaw hah tarawi laipalah, Bawipa ka panue toe ka tet e tami teh, a lai kathoute lah doeh o awh. Ahni dawk lawkkatang awmhoeh.
5 Koma munthu aliyense akamvera mawu ake, ndiye kuti chikondi cha Mulungu chafikadi penipeni mwa iyeyo. Pamenepo timatsimikizadi kuti tili mwa Iye.
Hote Bawipa lawk hah ka tarawi e teh, Cathut e a lungpatawnae hoi akawi katang. Maimouh ni hote Bawipa dawk o awh e hah het telah hoi panue awh.
6 Aliyense amene amati amakhala mwa Mulungu, ayenera kukhala moyo umene Yesu ankakhala.
Hote Bawipa dawk ka hring toe ka tet e tami teh, Jisuh ni a sak e patetlah a dawn van han.
7 Okondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano koma lakale lomwe lija, limene munali nalo kuyambira pachiyambi. Lamulo la kalelo ndi mawu amene munawamva kale.
Ka lungpataw e ka huinaw: nangmouh koe ka thut e kâpoelawk hateh, a katha e na hoeh. Ahmaloe hoi kaawm tangcoung e kâpoelawk hah doeh. Ahmaloe hoi kaawm tangcoung e kâpoelawk hateh na thai awh tangcoung e lawk hah doeh.
8 Komabe ndi lamulo latsopano limene ndikukulemberani. Choonadi chake chikuoneka mwa Yesu ndiponso mwa inu, chifukwa mdima ukutha ndipo kuwunika kwenikweni kwayamba kale kuwala.
Atuvah kâpoelawk katha hah nangmouh koevah ka thut. Hote kâpoelawk teh, Bawipa dawk nakunghai, nangmouh dawk nakunghai, hmu katang e lah ao. Bangkongtetpawiteh, hmonae teh a kahma teh angnae katang teh coungkacoelah a ang toe.
9 Aliyense amene amati ali mʼkuwunika, koma nʼkumadana ndi mʼbale wake ali mu mdima.
Hmaunawngha hah na hmuhma lahun nah, kai teh angnae dawk ka o ka tet e tami teh, atu sittouh hmonae thung doeh ao rah.
10 Aliyense amene amakonda mʼbale wake amakhalanso mʼkuwunika, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa.
Hmaunawngha lungpataw e tami teh angnae dawk kahring e lah ao. Kamthui teh rawp nahane ahni dawk awmhoeh.
11 Koma aliyense wodana ndi mʼbale wake ali mu mdima ndipo akuyenda mu mdima. Iyeyo sakudziwa kumene akupita, chifukwa mdima wamudetsa mʼmaso mwake.
Hmaunawngha kahmawt ngai hoeh e tami teh, hmonae dawk kaawm niteh hmonae dawk doeh a hring rah. Hmonae ni a mit a dawn sak teh, na maw ka cei tie hai panuek hoeh.
12 Inu ana okondedwa, ndikukulemberani popeza kuti machimo anu akhululukidwa chifukwa cha dzina la Yesu.
Ka lungpataw e canaw: nangmouh teh hote Bawipa min lahoi yon thoungsak lah na o awh toung dawkvah, hete ca ka thut teh na patawn awh.
13 Inu abambo, ndikukulemberani popeza kuti munamudziwa Iye amene analipo kuyambira pachiyambi. Inu anyamata, ndikukulemberani popeza kuti munagonjetsa woyipayo.
Apanaw: nangmouh teh apuengcue hoi kaawm tangcoung e hah, na panue awh dawkvah, hete ca ka thut teh na patawn awh. Thoundounnaw: nangmouh teh, kahrai hah na tâ awh dawkvah hete ca ka thut teh na patawn awh. Camonaw: nangmouh teh Pa hah na panue awh dawkvah hete ca ka thut teh na patawn awh.
14 Ana okondedwa, ndikukulemberani chifukwa mumawadziwa Atate. Abambo, ndikukulemberani chifukwa munamudziwa Iye amene analipo kuyambira pachiyambi. Inu anyamata, ndikukulemberani chifukwa ndinu amphamvu. Mawu a Mulungu amakhala mwa inu ndipo mumamugonjetsa woyipayo.
Napanaw: nangmouh ni apuengcue hoi kaawm tangcoung e hah, na panue awh dawkvah hete ca ka thut teh na patawn awh. Thoundounnaw: nangmouh na thasai awh teh, Cathut lawk na thung a hring teh, kahrai hah na tâ awh dawkvah, hete ca ka thut teh na patawn awh.
15 Musamakonde dziko lapansi kapena chilichonse cha dziko lapansi. Ngati munthu wina aliyense akonda dziko lapansi, mwa iyeyo mulibe chikondi chokonda Atate.
Talaivan hoi talaivan dawk kaawm e hnonaw hah lungpataw awh hanh. Talai lungpataw e teh, Pa lungpatawnae tawn hoeh.
16 Pakuti zonse za mʼdziko lapansi, zilakolako za thupi, zinthu zimene maso amakhumbira ndiponso kuyandikira zinthu za moyo uno, zonsezi sizichokera kwa Atate, koma ku dziko lapansi.
Talaivan dawk kaawm e hnonaw teh: takngainae, mitnoenae, talai hno dawk kâoupnae hah doeh. Hotnaw teh, Pa koehoi ka tho e nahoeh. Talai lahoi ka tho e doeh.
17 Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Talaivan hoi talaivan hno noenae teh kahmat han. Cathut ngainae patetlah ka tarawi e tami teh a yungyoe a kangning. (aiōn g165)
18 Ana anga, ino ndi nthawi yotsiriza, ndipo monga munamva kale kuti anthu okana Khristu akubwera, ngakhale tsopano okana Khristu ambiri afika kale. Zimenezi zikutisonyeza kuti ino ndi nthawi yotsiriza.
Ka lungpataw e canaw: atu e tueng teh, a hnukteng e atueng lah ao. Khrih e a taran khrihkaphawk a tâco e na thai awh e patetlah atu rawraw khrihkaphawknaw moi ao toe. Hatdawkvah, atu e tueng teh a hnukteng e atueng doeh toe tie panue thai.
19 Anthu amenewa anachoka pakati pathu, komatu sanali a mʼgulu lathu. Pakuti akanakhala a mʼgulu lathu, akanakhalabe nafe, koma kuchoka kwawo kunatisonyeza kuti sanali a mʼgulu lathu.
Ahnimanaw teh, maimouh koehoi a tâco awh teh, a cei awh toe. Hatei, ahmaloe hoi maimouh hoi kâkuen awh hoeh. Maimouh hoi kâkuen awh pawiteh maimouh hoi doeh rei awm a tih. Maimouh hoi kâkuen awh hoeh tie hah a kamnue nahanelah, maimouh koehoi a tâco awh toe.
20 Koma inu muli ndi kudzoza kochokera kwa Woyerayo, ndipo nonsenu mukudziwa choonadi.
Nangmouh teh, kathounge Cathut kut dawk hoi, satui awi lah na o awh. Hno cawngca pueng teh na panue awh.
21 Sindikukulemberani chifukwa choti simudziwa choonadi ayi, koma chifukwa choti mumadziwa choonadicho, ndipo mukudziwanso kuti bodza silichokera pa choonadi.
Lawkkatang na panue awh hoeh dawk ca na patawn awh e na hoeh. Nangmouh ni na panue awh teh, laithoe e pueng teh lawkkatang hoi kâkuen hoeh tie na panue awh dawkvah ca na patawn awh e doeh ka tho.
22 Wabodzayo ndani? Ndi munthu aliyense amene amanena kuti Yesu si Mpulumutsi. Munthu woteroyo ndi wokana Khristu, ndiponso amakana Atate, ndi Mwana.
Laithoe ka dei e teh apimaw. Jisuh teh Khrih nahoeh ka tet e tami hah doeh. Pa hoi Capa ka taran e teh khrihkaphawk doeh.
23 Aliyense wokana Mwana alibenso Atate. Wovomereza Mwana alinso ndi Atate.
Capa ka taran e tami teh, Pa panuek hoeh. Capa ka dâw e tami teh Pa hah a panue.
24 Onetsetsani kuti zimene munazimva kuyambira pachiyambi zikhalebe mwa inu. Ngati zikhala mwa inu, inunso mudzakhala mwa Mwana ndiponso mwa Atate.
Hatdawkvah, ahmaloe hoi na thai awh e phung lawk hah nangmouh dawk hring sak awh. Hote phung lawk teh, nangmouh dawk hring pawiteh, nangmouh teh Capa hoi Pa dawk kahring e lah na o awh han.
25 Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
Maimouh koe, na poe e lawkkam teh, a yungyoe hringnae hah doeh. (aiōnios g166)
26 Ine ndikukulemberani zimenezi kuti ndikuwuzeni za amene akufuna kukusocheretsani.
Nangmouh na ka dum e naw e a kong teh, hettelah kathut teh na patawn awh.
27 Koma za inu, kudzoza kumene munalandira kwa Khristu kuli mwa inu, ndipo sipafunika wina aliyense kuti akuphunzitseni. Koma kudzozako kumakuphunzitsani zinthu zonse, ndipo popeza kudzoza kwakeko nʼkoona osati konama, monga munaphunzira, khalani mwa Iyeyo.
Cathut koehoi na coe awh e satui awi lungmanae teh nangmouh dawk a hring dawkvah nangmouh teh apinihai bout cangkhai ngai hoeh toe. Hote satui awi lungmanae teh laithoe e nahoeh. A katang e na cangkhai dawkvah, na cangkhai e patetlah nangmouh ni Capa dawk hring awh.
28 Tsopano ana okondedwa, khalani mwa Yesu, kuti pamene adzaonekera, ife tidzakhale otsimikizika mu mtima ndi wopanda manyazi pamaso pake akamadzabwera.
Ka lungpataw e canaw: Capa a kamnue toteh, maimouh hai ama koe pha awh toteh, taranhawi laihoi, kayanae ao hoeh nahanelah, Capa dawk pou hring awh.
29 Popeza mukudziwa kuti Khristu ndi wolungama, choncho mukudziwanso kuti aliyense amene amachita chilungamo ndi mwana wa Mulungu.
Cathut teh a lan tie na panuek awh pawiteh, lannae ka sak e tami pueng hah Cathut ni a khe e doeh tie teh panue awh.

< 1 Yohane 2 >