< 1 Akorinto 5 >

1 Mbiri yamveka kuti pakati panu pakuchitika chigololo. Ndipo chigololo cha mtunduwu ngakhale pakati pa akunja sichingapezeke; munthu akumagonana ndi mkazi wa abambo ake.
Fa miboele te ama’ areo ty fifampirañaotañe, toe hakarapiloañe tsy amo kilakila’ ndatio: te eo ty miharo-lamba amy valin-drae’ey!
2 Ndipo inu mukudzitukumulabe. Kodi simukanayenera kudzazidwa ndi chisoni ndipo mukanamuchotsa pa chiyanjano chanu munthu wochita zimenezi?
Akore te iebotsebora’ areo! tsy hamake ho nandala? soa te ho naitòañe i nanao zay.
3 Ngakhale sindili nanu mʼthupi, ndili nanu mu mzimu. Ndipo ineyo ndapereka kale chiweruzo pa munthu amene amachita zotere, ngati kuti ndili komweko.
Aa naho izaho, ndra te tsy eo am-batañe, le miatreke an-troke vaho fa zinakako i nanao zay, manahake t’ie eo.
4 Mukasonkhana mu dzina la Ambuye athu Yesu, ine ndili nanu mu mzimu, ndipo mphamvu ya Ambuye athu Yesu ili pomwepo,
Ie mivory amy tahina’ Iesoà Talèntikañey, le ama’ areo an-troke iraho, ami’ty haozara’ Iesoà Talèntikañey,
5 mumupereke munthuyu kwa Satana, kuti chikhalidwe chake cha uchimo chiwonongedwe ndikuti mzimu wake udzapulumuke pa tsiku la Ambuye.
aa le aseseo amy mpañìnjey indatiy handro­tsahañe i haondati’e hambo’ey, soa te ho rombaheñe ami’ty andro’ i Talè Iesoà i arofo’ey.
6 Kudziwa kwanu si kwabwino. Kodi simukudziwa kuti yisiti wochepa amafufumitsa mphumphu yaufa wonse wa tirigu?
Tsy mete ty firoharohà’ areo; tsy fohi’ areo hao te mahatsi­tsike ty boko’e ty lalivay kede.
7 Chotsani yisiti wakale kuti mukhale ndi mphumphu yopanda yisiti, monga inu muli. Pakuti Khristu, Mwana Wankhosa wa Paska wathu, anaperekedwa nsembe.
Kohezo soa o lalivay hambo’eo soa t’ie ho boko’e vao, manahake t’ie tsy aman-dalivay, fa nisoroñañe ho antika i Norizañey, i Fihelan-tikañey
8 Choncho, tiyeni tisunge chikondwererochi, osati ndi yisiti wakale, wowononga ndi woyipa, koma ndi buledi wopanda yisiti, buledi woona mtima ndi choonadi.
Aa le antao hiambeñe i sabadidakey, tsy aman-dalivay hambo’e, tsy aman-dalivain-kalo-tserehañe naho haratiañe, fa ami’ty tsy aman-dalivai’ i hatsò-troke naho hatòy.
9 Ndakulemberani mʼkalata yanga kuti musayanjane nawo anthu achigololo.
Nisokirako amy taratasikoy te tsy hitrao-drehake amo manao hakarapiloañeo,
10 Pamenepatu sindikutanthauzatu anthu a dziko lapansi lino amene ndi achigololo, kapena aumbombo, kapena opeza ndalama mwachinyengo, kapena opembedza mafano. Kukanatero mukanangochoka mʼdziko lapansi lino.
fe tsy t’ie ze fonga karapilo’ an’ tane atoy ndra ze mpihàñe naho mpikatramo ndra ze mpañori-pahasive, amy t’ie tsy mahay tsy ho niakatse an-tane atoy.
11 Koma tsopano ndikukulemberani kuti musayanjane ndi aliyense amene adzitcha mʼbale koma ndi wachigololo, kapena waumbombo, kapena wopembedza mafano, kapena wonamizira anzake, woledzera kapena wopeza ndalama mwachinyengo. Munthu wotere ngakhale kudya, osadya naye pamodzi.
Fe nisokirako te tsy hitraofa’areo ty miantoñoñe ho longo, te mone mpañarapilo ndra mpitsikirìke, ndra mpitorom-pahasive, ndra mpañinje, ndra mpijike, ndra mpikatramo. Ko itraofam-pikama. ­
12 Kodi ndipindulanji kuti ndiweruze anthu amene si a mu mpingo? Kodi simuyenera kuweruza iwo amene ali mu mpingo?
Inoñe ty izakako o alafe’eo? Tsy zakae’ areo hao o ama’ areoo?
13 Mulungu adzaweruza akunja. “Chotsani woyipayo pakati panu.”
I Andrianañahare ty hizaka o alafe’eo, fe Aitò ama’ areo i tsivokatsey.

< 1 Akorinto 5 >