< 1 Akorinto 5 >

1 Mbiri yamveka kuti pakati panu pakuchitika chigololo. Ndipo chigololo cha mtunduwu ngakhale pakati pa akunja sichingapezeke; munthu akumagonana ndi mkazi wa abambo ake.
Slyšel jsem, že se dokonce u vás vyskytla nemravnost, jakou by člověk i mezi pohany těžko hledal: že si totiž jeden z vás udělal milenku z nevlastní matky.
2 Ndipo inu mukudzitukumulabe. Kodi simukanayenera kudzazidwa ndi chisoni ndipo mukanamuchotsa pa chiyanjano chanu munthu wochita zimenezi?
A to se ještě nestydíte zdvihat nos až k nebi, místo abyste se zhrozili a vyloučili takového člověka ze svého společenství!
3 Ngakhale sindili nanu mʼthupi, ndili nanu mu mzimu. Ndipo ineyo ndapereka kale chiweruzo pa munthu amene amachita zotere, ngati kuti ndili komweko.
Ačkoliv nejsem mezi vámi, mnoho jsem o tom přemýšlel a jako služebník Ježíše Krista jsem už rozhodl, co je třeba udělat. Svolejte shromáždění všech věřících, moc Pána Ježíše bude s vámi – a já v jeho Duchu také –
4 Mukasonkhana mu dzina la Ambuye athu Yesu, ine ndili nanu mu mzimu, ndipo mphamvu ya Ambuye athu Yesu ili pomwepo,
5 mumupereke munthuyu kwa Satana, kuti chikhalidwe chake cha uchimo chiwonongedwe ndikuti mzimu wake udzapulumuke pa tsiku la Ambuye.
a ten člověk ať je vyloučen ze společenství křesťanů a ať je ponechán moci zla. Vždyť může být zachráněn, až Ježíš Kristus přijde soudit svět.
6 Kudziwa kwanu si kwabwino. Kodi simukudziwa kuti yisiti wochepa amafufumitsa mphumphu yaufa wonse wa tirigu?
Nechápu, jak se můžete chlubit svou dokonalostí a přitom mezi sebou trpět takovou špínu. Cožpak nechápete, že nákaza, když se jí neučiní přítrž, může brzy zachvátit i ostatní?
7 Chotsani yisiti wakale kuti mukhale ndi mphumphu yopanda yisiti, monga inu muli. Pakuti Khristu, Mwana Wankhosa wa Paska wathu, anaperekedwa nsembe.
Ložisko rozkladu musíte odstranit, chcete-li sami zůstat čistí. Kristus byl zabit za nás! Nechme už tedy toho starého, hříchem prolezlého života a oslavujeme Krista v čistotě, upřímnosti a pravdivosti.
8 Choncho, tiyeni tisunge chikondwererochi, osati ndi yisiti wakale, wowononga ndi woyipa, koma ndi buledi wopanda yisiti, buledi woona mtima ndi choonadi.
9 Ndakulemberani mʼkalata yanga kuti musayanjane nawo anthu achigololo.
Napsal jsem, že od špatných lidí se máte držet co nejdál.
10 Pamenepatu sindikutanthauzatu anthu a dziko lapansi lino amene ndi achigololo, kapena aumbombo, kapena opeza ndalama mwachinyengo, kapena opembedza mafano. Kukanatero mukanangochoka mʼdziko lapansi lino.
Nemyslel jsem to ovšem tak, že se máte vyhýbat všem nepoctivým, chamtivým, oplzlým a bezbožným lidem. To byste se museli vystěhovat na pustý ostrov.
11 Koma tsopano ndikukulemberani kuti musayanjane ndi aliyense amene adzitcha mʼbale koma ndi wachigololo, kapena waumbombo, kapena wopembedza mafano, kapena wonamizira anzake, woledzera kapena wopeza ndalama mwachinyengo. Munthu wotere ngakhale kudya, osadya naye pamodzi.
Jestliže se však někdo vydává za křesťana, ale je nepoctivý a chamtivý, holduje kariéře a majetku, alkoholu, pohlavní nevázanosti nebo jiným neřestem, pak s ním ani nesedejte k jednomu stolu.
12 Kodi ndipindulanji kuti ndiweruze anthu amene si a mu mpingo? Kodi simuyenera kuweruza iwo amene ali mu mpingo?
Soudit nekřesťany – na to právo nemáte, ty ať soudí Bůh. Ale z našich řad musí být takový člověk vyloučen!
13 Mulungu adzaweruza akunja. “Chotsani woyipayo pakati panu.”

< 1 Akorinto 5 >