< 1 Akorinto 4 >

1 Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu.
Keini hih Khrista tîrlâmngei, le Pathien chongtak inthup donsûipungeiin mi mindon roi.
2 Chofunika kwambiri nʼchakuti amene apatsidwa udindo oyangʼanira aonetse kukhulupirika.
Hi taka neinun ankhat anâng chu tîrlâmngei hah an pu mitmua mi taksônom an ni rang ani.
3 Ine ndilibe nazo kanthu ngati ndiweruzidwa ndi inu kapena khothi lina lililonse. Ndithu, inenso sindidziweruza ndekha.
Atûn nangnin mi nin jêkna le miriem mindonna balama mi nin jêkna hah kei rangin chu itên bê mu-ung; Ke thenin khom ko roijêk ngâi mu-ung.
4 Chikumbumtima changa sichikunditsutsa, koma sikuti ndine wolungama. Wondiweruza ine ndi Ambuye.
Ki sielesarietna chu ânthâr, hannirese mahan keima sietnaboi ki ni tatak inthârna om uol mak. Pumapa hah ku chunga roijêkpu chu ani.
5 Chomwecho musaweruze nthawi yoweruza isanakwane. Dikirani mpaka Ambuye atabwera. Iye adzaonetsa poyera zimene zabisika mu mdima ndipo adzaonetsa maganizo a mʼmitima ya anthu. Pa nthawi imeneyo aliyense adzalandira kwa Mulungu chiyamiko.
Masikin Pumapa juong nôk mâka chu azora diktak motona roi lei jêkmasat lai no roi. Azoina roijêkna chu Pumapa juong rang ngâk ngêt nîng a ta; ama'n ijînga inthup ngei hah avâra hong kêlsuong a ta, miriem mulungrîla bôkna inthup ngei khom minlang sâng atih. Male mitinin minpâkna an chang rang dôr Pathien renga an khôk rang ani.
6 Tsono abale, ndapereka chitsanzo cha ine mwini ndi Apolo kuti mupindule. Phunzirani kwa ife tanthauzo la mawu akuti, “Musamapitirire zimene Malemba akunena,” kuti musamanyade pamene wina aposa mnzake.
Ka lâibungngei le sarnungei, “Balamngei hih jôm roi,” ti hi nin inchu theina rangin keima le Apollos hih nin enton rangin ko hong târminlang ani, tutên mi inkhat songin midang enkhûm no roi.
7 Pakuti ndani amakusiyanitsani ndi wina aliyense? Nʼchiyani muli nacho chimene simunalandire? Ndipo ngati munalandira, bwanji mumadzitukumula ngati kuti simunalandire?
Tumo midang chunga ulienin nangni sin? Neinuntin nin man ngei hah Pathien'n nangni a pêk nimak mo? Asa, nin man anînte ithomo manboipêk aman loi angin omlien nin songa?
8 Inu muli nazo kale zonse zimene mufuna! Inu mwalemera kale! Inu mwayamba kale kulamulira ife! Ndilakalaka mukanakhaladi mafumu kuti ife tikhale nawo mafumu pamodzi ndi inu.
Nin nâng ngei murdi nin dôn zoi mo? Nin nei mo ani zoi? Kin om nonnom rêngngei nin chang thei mo ani zoi? Asa, rêngngei chang thei tatak ungla ku nuom ani, hanke nangni leh munkhata rêngngei ei chang thei rang.
9 Pakuti kwa ine zikuoneka ngati kuti Mulungu watiyika ife atumwi pachionetsero, kumapeto kwa mndandanda, monga anthu oweruzidwa kuti akaphedwe mʼmabwalo. Ife tayikidwa kuti tionekere ku dziko lonse, kwa angelo ndi anthu.
Pathien'n keini tîrtonngei hih thi ranga inkhâm anga anûktaka mi tîrsuokin kin bê ani; rammuol le vântîrtonngei le miriemngei mitmua enhoia sinin kin om sika hin.
10 Ife ndife opusa chifukwa cha Khristu, koma inu ndinu anzeru mwa Khristu! Ife ndife ofowoka koma inu ndinu amphamvu! Inu ndinu olemekezeka koma ife ndife opeputsidwa!
Keini chu Khrista jârin amo kin ni; aniatachu nangni chu Khrista jârin mivâr nin ni! Keini chu kin doka, hannirese nangni chu nin rât! keini chu mingeiin min enkhûma, nangni chu mirit nangni an tho!
11 Mpaka pano tili ndi njala ndi ludzu, tili ndi sanza, tikuzunzidwa, tilibe nyumba.
Atûn ten vonchâm le tui inrâlin kin oma; rovo chetin kin invoa; mi tôkmol kin tuonga; ommun invâiin kin chai titir ani;
12 Timagwira ntchito molimbika ndi manja athu. Akamatitemberera, ife timadalitsa; tikasautsidwa, ife timapirira.
Kin kuta sinthôn dûktong takin kin invâi ani. Mîn khomâk min sâm khomin sat kin vur ngâia; dûk min mintong khomin diertakin kan tuonga;
13 Pamene atilalatira timayankha mwachifundo. Mpaka pano takhala ngati zinyalala za dziko, monga zakudzala za dziko lapansi.
Mi min êro khomin chong dâiriemin kin thuon ngâi. Hi rammuola ronok leh tei uol khâi mak meh; hi zora ten khom hin rammuola pornôngkok angin kin ni.
14 Sindikulemba izi kuti ndikuchititseni manyazi, koma kukuchenjezani monga ana anga okondedwa.
Hi chong ki miziek hih nin inzakpuina ranga ki ti niloiin, Ka nâi moroi ngei angin nangni minchu ku nuom sika ani.
15 Ngakhale muli ndi anthu 10,000 okutsogolerani mwa Khristu, mulibe abambo ambiri, popeza mwa Khristu Yesu, ine ndakhala abambo anu kudzera mu Uthenga Wabwino.
Khristien ringnuna enkolpu isâng sôm dôn khom ungla, Pa chu inkhat vai kêng nin dôn. Nan lâia Thurchi Sa hong mintunga Khrista Jisua leh inzoma nin ringna han nin pa ko hongni ani.
16 Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.
Masikin keima ku nunchan jûi rangin nangni ke ngên.
17 Chifukwa cha ichi ndikutumiza kwa inu Timoteyo, mwana wanga amene ndimamukonda, amene ndi wokhulupirika mwa Ambuye. Adzakukumbutsani inuyo za moyo wanga mwa Khristu Yesu, umene ukugwirizana ndi zimene ndimaphunzitsa paliponse mu mpingo uliwonse.
Hi chungroia hin Timothy, khristien ringnun jâra ka nâipasal moroi le taksônom hih nin kôm ko hongtîr. Ama'n Khrista leh inzomin ringna thara ku nunchan muntina koiindangngei murdi ki minchu ngâi anghan nangni min riet nôk atih.
18 Ena mwa inu mukudzitukumula, ngati kuti sindingabwere kwanu.
Nin lâia ko hong khâi loi rang mini ti nin bôk sikin, mi senkhatin chu omlien nan song ani.
19 Koma ndibwera kwanuko posachedwapa, ngati Ambuye alola, ndipo ndi pamene ndidzadziwe osati zimene anthu odzitukumulawa akuyankhula, koma kuti mphamvu zawo nʼzotani.
Nikhomrese, Pumapa'n asa a tiin chu nan lâia hong lai ki tih, Hanchu hi mi ânsong ngei hih an mûrra an ti vai niloiin, sinthotheina an dôn khom mu thei ki ti zoi.
20 Pakuti ufumu wa Mulungu si mawu chabe koma mphamvu.
Pathien Rêngram chu chongbâingei vaia om niloiin sinthotheinân aom kêng ani uol.
21 Kodi musankha chiyani? Kodi ndidzabwere ndi chikwapu, kapena mu chikondi ndiponso mwa mzimu wofatsa?
Imo nin nuom uol? Tôkmol leh mo nin kôm ku juong rang, aninônchu ratha lungkhamna le nuninnêmin mo?

< 1 Akorinto 4 >