< 1 Akorinto 2 >
1 Pamene ndinabwera kwa inu, abale, sindinabwere ndi luntha lodziwa kuyankhula kapena nzeru zapamwamba pamene ndinachitira umboni chinsinsi cha Mulungu.
Ka lâibungngei le sarnungei, Pathien chongtak inthup, misîra nin lâia ko hong lâihan, chong roiinpui le rietna roiinpui mang mu-ung.
2 Pakuti ndinatsimikiza pamene ndinali ndi inu kuti ndisadziwe kanthu kena kupatula Yesu Khristu wopachikidwayo.
Nin lâia ko om han khom neinun dang murdi mingil riein Jisua Khrista jêmdela aom roi vai kêng nin riet rang ku nuom ngâi.
3 Ndinabwera kwa inu wofowoka ndi wamantha, ndiponso wonjenjemera kwambiri.
Ma anghan nin lâia han râtloi le innîk pumin leh ichin ko oma,
4 Uthenga ndi ulaliki wanga sunali wa mawu anzeru ndi onyengerera koma woonetsa mphamvu za Mzimu,
male ka bâi renga minchuna chong asuok le ku thurchi misîr ngei khom hah miriem vârna methêmna chong nimaka, Pathien Ratha sinthotheina chong kêng ani uol.
5 kuti chikhulupiriro chanu chisatsamire pa nzeru ya anthu koma pa mphamvu za Mulungu.
Masikin nin taksônna hah miriem vârna han inngam maka, Pathien sinthotheina han kêng ânngam ani.
6 Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
Hannoma rathatienga mitungsuo ngei kôm chu vârna chong ki misîr ngâi. Hannirese hi rammuol vârna chong chu nimaka, hi rammuol roijêkpungei an inlalna ânmang tir ngei vârna chong khom nimak. (aiōn )
7 Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
Pathien vârna chong inthup ha kêng ki misîr ngâi, vârna chong inthup ei roiinpuina ranga Pathien'n rammuol om mânna a lei thangsai hah kêng ani. (aiōn )
8 Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
Ma vârna hah hi rammuol roijêkpungei rengin riet mak ngei. Riet senla ngei chu roiinpuina Pumapa hah jêmdel noni ngei. (aiōn )
9 Komabe monga zalembedwa kuti, “Palibe diso linaona, palibe khutu linamva, palibe amene anaganizira, zimene Mulungu anakonzera amene amukonda”
Hannoma Pathien lekhabu'n, “Tutên an mu ngâiloi le an riet ngâiloi, Ma anga tung ranga tutên an mindon loi, Pathien'n a lungkham ngei ta ranga a mintuosai ngân chu,” ati anghan.
10 koma Mulungu waululira ife mwa Mzimu wake. Mzimu amafufuza zinthu zonse, ndi zozama za Mulungu zomwe.
Aniatachu Pathien'n eini rangin chu a chongtak inthup hah Ratha'n mi min riet zoi. Ratha han jâttin a sûisuok ngâi, Pathien neinunkhînngei inthûktaka inthup khom.
11 Kodi ndani mwa anthu angadziwe maganizo a munthu wina, kupatula mzimu wa munthuyo wokhala mʼkati mwake? Chimodzimodzinso palibe amene adziwa maganizo a Mulungu kupatula Mzimu wa Mulunguyo.
Ei sûnga om ei ratha lelê hih vai kêng ei chungroi a riet ngâia; ma angdên han, Pathien Ratha vai kêng Pathien chungroi murdi a riet thei ngâi.
12 Mzimu amene tinalandira ife si wa dziko lapansi koma Mzimu wochokera kwa Mulungu wotipatsa ife mwaulere.
Ei man hih rammuol Ratha nimaka; manêkin, Pathien'n neinun mi pêk ngei murdi ei riet theina rangin, Pathien juongtîr Ratha ha kêng ei man ani.
13 Izi ndi zimene timayankhula osati mʼmawu wophunzitsidwa ndi nzeru za munthu koma mʼmawu wophunzitsidwa ndi Mzimu, kufotokozera zoonadi zauzimu mʼmawu auzimu.
Masika han miriem vârna minchûn, misîr ngâi mak mea, Ratha minchûn kêng kin misîr ngâi, rathatienga chongtakngei hah Ratha dônngei kôm kin rilsensâi ngâi.
14 Munthu wopanda Mzimu savomereza zinthu zimene zichokera kwa Mzimu wa Mulungu, popeza ndi zopusa kwa iyeyo, ndipo sangazimvetsetse chifukwa zimazindikirika mwa Mzimu.
Tukhom Ratha dôn loiin chu Pathien Ratha renga manboipêkngei hah man thei ngâi mak ngei. Ma anga mingei han chu ma neinunngei hah riet thei ngâi mak ngeia; ama ta rangin chu inmôlna vai kêng ani, a luttie hah Ratha'n vai kêng a riet thei sikin.
15 Munthu wauzimu amaweruza pa zinthu zonse, koma iye mwini saweruzidwa ndi munthu aliyense.
Tutu khom Ratha man ngei chu neinuntin aluttie an riet ngâi, hannirese, ama chu tutên jêk thei ngâi mak ngei.
16 Pakuti “Ndani anadziwa malingaliro a Ambuye, kuti akhoza kumulangiza Iye.” Koma tili nawo mtima wa Khristu.
Pathien lekhabu'n ati anghan: “Tu'n mo Pumapa mulungrîl a riet? Tu mo minchuna chong a pêk thei rang?” Nikhomrese, einin chu Khrista mulungbôk ei pêl ani.