< 1 Akorinto 15 >

1 Tsono abale, ndikufuna ndikukumbutseni za Uthenga Wabwino umene ndinakulalikirani. Munawulandira ndipo munawukhulupirira kolimba.
Eshi embizusya bha kolo na mwailombo juu yizu lyana bhalombeleye amba mwaliposheye na hwemelele nalyo.
2 Inu munapulumutsidwa ndi Uthenga Wabwinowu, ngati mwasunga mawu amene ndinakulalikirani. Kupanda kutero, mwangokhulupirira pachabe.
Katika izu eli mwaushe nkashele mubhalikhate imara izu lyanabhalombeleye amwe afanaje mwaheteshe wene.
3 Pakuti chimene ndinalandira ndinapereka kwa inu monga chofunika kuposa zonse, kuti Khristu anafera zoyipa zathu monga mwa Malemba,
Nkashele pawandilo shanaposheye humuhimu naletile hwilimwe: neshe shehweli aje arengane ne nsimbo, Kristi afwiye kwajili yembibhi zwetu,
4 kuti anayikidwa mʼmanda, kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu monga mwa Malemba;
alengane nensimbo asyelelwe naje azwoshele isiku elyatatu.
5 ndipo kuti anaonekera kwa Petro, ndipo kenaka kwa Atumwi khumi ndi awiriwo.
Naje abhonesha bhwa Kefa, antele hwabhala kumi na bhabhele.
6 Pambuyo pake, Iye anaonekera kwa anthu oposa 500 mwa abale pa nthawi imodzi, ndipo ambiri mwa iwo akanali ndi moyo ngakhale kuti ena anagona tulo.
Antele abhoneshe hwa wakati umo abhoneshe hwa kolo na hwayiombo zaidi ya bhantu mia zisanu. Abhinji bado bhali womi, lelo bhamo bhagonile utulo.
7 Kenaka anaonekeranso kwa Yakobo, kenaka kwa atumwi onse.
Antele abhoneshe hwa Yakobo, antele abhonesha hwa tumwa bhonti.
8 Potsiriza pa onse anaonekeranso kwa ine, monga mwana wobadwa nthawi isanakwane.
Mwisho wa gonti, abhoneshe hwiline neshe shila hwa mwana yapepwe husiku zwasezilisawa.
9 Pakuti ine ndine wamngʼono kwa atumwi ndipo sindiyenera nʼkomwe kutchedwa mtumwi chifukwa ndinazunza mpingo wa Mulungu.
Afwanaje ane endi dodo hwa mitume. Sehwanziwa akwiziwe mtume, eshabhanza esha Ngolobhe
10 Koma mwachisomo cha Mulungu, ndili mmene ndililimu, ndipo chisomo chake kwa ine sichinali chopanda ntchito. Ndinagwira ntchito kuposa ena onse a iwo. Choncho sindine koma chisomo cha Mulungu chimene chinali ndi ine.
Lelo hu neema eya Ngolobhe endi neshe shehali na neema yakwe hwaline seyali yewene. Badala yakwe nabhombile ebidii ashile wonti. Lelo senaline ne bali neema eya Ngolobhe yeli mhati yane.
11 Tsono kaya ndi ineyo kapena iwowo, izi ndi zomwe timalalikira, ndipo izi ndi zimene munakhulupirira.
Eshi nkashile nene au bhebho ulombelela esho taminile esho.
12 Koma ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa, zikutheka bwanji kuti ena mwa inu azinena kuti kulibe kuuka kwa akufa?
Eshe nkashele Kristi alombele we aje asyoshele hwa bhafwe, ebhe hwele mubhabhobho muyigo nahumo azwoshe bhabhafwiye?
13 Ngati kulibe kuuka kwa akufa, ndiye kuti ngakhale Khristu sanaukenso.
Lelo nkashele nahumo azwoshe abhafwe basi hata Kristi sagazweshele.
14 Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, ndiye kuti kulalikira kwathu nʼkopanda ntchito, ndipo chikhulupiriro chanu nʼchopandanso ntchito.
Na nkashile Kristi sagazwoshele esho alombelele hwetu hubhe hwewene imani yetu abhe yewene.
15 Kuwonjezera pamenepa, ndiye kuti ndife mboni zabodza pa za Mulungu, pakuti tikuchita umboni kuti Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa. Ngati nʼzoona kuti akufa saukitsidwa, ndiye kuti Mulungu sanaukitsenso Khristu.
Na tipatihene aje bhashahidi bhwilenka ahusu Ungolobhe kwa sababu tishuhudie Ungolobhe sha hwisalo aje azwozwe Kristi wakati sagazwozwezwe.
16 Pakuti ngati akufa saukitsidwa, ndiye kuti nayenso Khristu sanaukitsidwe.
Nkashile abhafwe sebhazwoha, U Yesu wape sagazwoshele.
17 Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, chikhulupiriro chanu nʼchopanda ntchito; mukanali mu machimo anu.
Nkashile Kristi sagazwoshele ahwamini hwetu ni bure na msele mlimbibhi zwenyu.
18 Ndiye kuti nawonso amene agona tulo mwa Ambuye ndi otayika.
Esho hata bhala bhabhafwiye katika Kristi bhape bhatejele.
19 Ngati kukanakhala kuti tili ndi chiyembekezo mwa Khristu mʼmoyo uno wokha, tikanakhala omvetsa chisoni kuposa anthu ena onse.
Nkashele humaisha ega gene yaje tilinoujasili hwa wakati wa wayenza mhati mwa Kristi abhantu wonti, atee tibhalongwe zaidi ya bhantu wonti.
20 Koma nʼzoonadi kuti Khristu anaukitsidwa kwa kufa, chipatso choyamba cha onse ogona tulo.
Lelo eshi Kristi azwoshele afume hwabhafwiye, madodo agahwande gabhala bhabhafwiye.
21 Pakuti monga imfa inadza kudzera mwa munthu, kuuka kwa akufa kwabweranso kudzera mwa munthu.
Afwanaje efwa ehenzele ashilile umuntu, antele ashilile muntu azwosyewe hwa bhabhafwiye.
22 Pakuti monga mwa Adamu onse amafa, chomwechonso mwa Khristu onse adzakhala ndi amoyo.
Afwatanaje nkashele katika u Adamu bhantu bhonti bhafwa, esho nantele katika Kristi bhayibhombwa womi wakati ubhenze hwakwe.
23 Koma aliyense adzauka pa nthawi yake. Khristu ndiye woyambirira, pambuyo pake, pamene Khristu adzabwera, iwo amene ali ake adzauka.
Lelo kila muntu katika shapajile hwakwe kristi madondo aga hwande antele bhala bhabhli Kristi bhayibhomba bhomi wakati uwahwenza hwakwe.
24 Pamenepo chimaliziro chidzafika, pamene Iye adzapereka ufumu kwa Mulungu Atate, atathetsa ufumu wonse, ulamuliro wonse ndi mphamvu zonse.
Ndipo waibha umalilo, pala uKristi nayibha akabidhi umwene uwa Ngolobhe uBaba. Ene pala nayibha akomesya oungozi wonti nemamlaka gonti ne nguvu zwonti.
25 Pakuti Iye ayenera kulamulira mpaka Mulungu atayika pansi pa mapazi ake adani ake onse.
Afwatanaje lazima atawale mpaka nayibhabheha abhibhibha kwe pansi eye magagakwe.
26 Mdani wotsiriza kuwonongedwa ndi imfa.
Ubhibhi uamalishile uwnankayiziwe efwa.
27 Pakuti Mulungu “wayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake.” Ponena kuti wayika “zinthu zonse pansi pa mapazi ake,” nʼchodziwikiratu kuti sakuphatikizapo ndi Mulungu yemwe, amene anayika zinthu zonse pansi pa Khristu.
Afwanaje “abheshele kila hantu pansi pamanamagakwe.” Lelo neyanga abheshele kila hantu ni wazi aje ene sehusizwa bhala bhabhabhehwelwe kila muntu pansi yakwe yoyo.
28 Pamene adzatsiriza kuchita zimenezi, Mwana weniweniyo adzakhala pansi pa ulamuliro wa Iye amene anayika zinthu zonse pansi pake, kuti Mulungu akhale zonse mu zonse.
Wakati evintu vyonti vibhehwelwe pansi yakwe, antele Umwana wakwe yoyo ayibhelwa pansi ya mwahele ambaye abheshele evintu vyonti pansi yakwe. Ene ebhoneshe ili kwamba Ungolobhe uBaba abhe gonti katika vyonti.
29 Tsono ngati kulibe kuuka kwa akufa, kodi iwo amene akubatizidwa chifukwa cha akufa, adzatani? Ngati akufa saukitsidwa nʼkomwe, bwanji nanga anthu akubatizidwa mʼmalo mwawo?
Au nantele bhabhombe yenu bhala bhabhahozwe kwajili bhabhafweye? Nkashile abhafwa sebhazwoha tee, yenu antele bhahozi wa kwajili yabho?
30 Ndipo kwa ife, tikuyikiranji moyo wathu pachiswe nthawi ndi nthawi?
Naye nu tilimhatari kila sala?
31 Abale, ndimafa tsiku ndi tsiku, ndikunenetsa zimenezi, mongotsimikizira monga ndimakunyadirani mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
Kolo na Yilombo bhane ashilile ahwisifu hwane katika amwe ambayo endinayo o katika Kristi Yesu Gosi wetu etangazwa eshe efwa kila lisiku.
32 Ngati ndinalimbana ndi zirombo za kuthengo ku Efeso pa zifukwa za umunthu chabe, ndapindulanji? Ngati akufa sadzaukitsidwa, “Tiyeni tidye ndi kumwa, pakuti mawa tifa.”
Esaidila yenu katika enyelezwo ezwe bhanadamu nkashele nakhomene wanyama akhali ohwo hwa Efeso, nkashile bhabhafwiye? “Sebhazwoha leha basi tilyaje na mwele, afwanaje sandabho taifwa.”
33 Musasocheretsedwe, “Kukhala mʼmagulu oyipa kumawononga makhalidwe abwino.”
Mganje akhopelwe sololile amabhibhi gunankanya etabia enyinza.
34 Ganizani bwino monga kuyenerera, ndiye lekani kuchimwa; pakuti pali ena amene sadziwa Mulungu. Ndikunena izi kuti muchite manyazi.
“Mubhanje nekiasi! mkhalaje katika lyoli mgaje ahwendele abhombo embibhi. Afwanaje bhamobhamo kati yenyu sebhanowelewa uwa Ngolobhe eyanga eshi kwa esoni zwenyu.
35 Koma wina akhoza kufunsa kuti, “Kodi akufa amaukitsidwa motani? Adzauka ndi thupi la mtundu wanji?”
Lelo umuntu uhwenje abhayanje, Hwele abhafwe bhazwoha? Wape bhayenza neshe hwelebhwele nobele?”
36 Wopusa iwe! Chimene mudzala sichikhala ndi moyo pokhapokha chitayamba chafa.
Awe ulilema tee! shila shahatotile seshiwezizwe ahwande amele isipokua shifwiye.
37 Mukadzala, simudzala thupi limene lidzamere, koma mbewu chabe, mwina ya tirigu kapena ya china chake.
Na shila shotota se bele ambao gwaibha bali mbeyu yechi puye ahwezizwe abhengano au hantu ahamwao.
38 Koma Mulungu amayipatsa thupi monga Iye wafunira, ku mbewu ya mtundu uliwonse amapereka thupi lakelake.
Lelo Ungolobhe ayipela ubele shasongwelwe umwahale na katika kila mbeyu bele ngwakwe mwenyewe.
39 Mnofu siwofanana. Anthu ali ndi mnofu wa mtundu wina, nyama zili ndi wina, mbalame zili ndi wina, nsomba zili ndi winanso.
Amabele gonti segelengene isipokuwa gahweli amabele gwa bhantu ubele gumo gwe makoko na ubele gumo wenyonyi gumo kwe samaki.
40 Palinso matupi akumwamba ndipo palinso matupi a dziko lapansi; koma ulemerero wa matupi akumwamba ndi wina, ndi wa matupi a dziko lapansi ndi winanso.
Antele gahweli amabele amwanya na mabele agapansi. Lelo uhwinza wakwe ubele ugwamwanya ni halimo nowa pansi hwenje.
41 Dzuwa lili ndi ulemerero wake, ndipo pali ulemerero wina wa mwezi, palinso ulemerero winanso wa nyenyezi. Ulemerero wa nyenyezi ndi wosiyanasiyana.
Huli uwinza umo wisaya na uwinza umo wemwezi, na uwinza umo wentondwe afwatanaje entondwe emo elegene nento ndwe uwinza.
42 Zidzaterenso pamene akufa adzauka. Thupi loyikidwa mʼnthaka ngati mbewu limavunda, koma likadzauka lidzakhala losavunda.
Esho shashihweli nante azwozwewe bhabhafwiye shitotwa shinanjiha shashimela seshinanjiha.
43 Limayikidwa mʼmanda mopanda ulemu, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi ulemerero. Limayikidwa mʼmanda lili lofowoka, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi mphamvu.
Shitolilwe katika amatumizi agekawada shimezewa katika uwinza shitotilwa katika uswogusu shimezewa katika enguvu.
44 Limayikidwa mʼmanda thupi la mnofu chabe, koma likadzaukitsidwa lidzakhala lauzimu. Ngati pali thupi la mnofu, palinso thupi lauzimu.
Shitotilwe katika ubele wa silishimezwa katika ubele ushiroho nkashile kuguhweli ubele ugwe asili gwape ugweshiro guhweli.
45 Kwalembedwa kuti, “Munthu woyamba Adamu anakhala wamoyo,” Adamu wotsiriza anakhala wopatsa moyo.
Esho antele esimbwilwe muntu uwa hwanda yuadamu abhombwelwe roho yekhala.” u Adamu uwamalisholo abhombeshe roho yefumya owomi.
46 Zauzimu sizinabwere koyambirira, koma zachilengedwe, pambuyo pake zauzimu.
Lelo uwe shiroho sagahenzele kwanza bali uwe asili napande uweshiroho.
47 Munthu woyamba anali wa dziko lapansi, wochokera mʼnthaka koma munthu wachiwiri anali wochokera kumwamba.
Umuntu uwa hwande wa pansi alengenyezewe humankondi. Umuntu uwabhele afumile umwanya.
48 Monga analili munthu wa dziko lapansi, momwemonso anthu onse amene ndi a dziko lapansi. Ndipo monga alili munthu wakumwamba, momwemonso anthu onse amene ndi akumwamba.
Neshe ula yalenganyiziwe humana ondi shesho antele bhala bhabhale ngenywe humankondi. Nkashile ula umuntu umbinguni shahweli nantele bhala abhamwanya.
49 Ndipo monga momwe tinabadwa ofanana ndi munthu wa dziko lapansi uja, momwemonso tidzakhala ofanana ndi munthu wakumwamba.
Kama ambavyo tumebeba mfano wa mtu wa mavumbi, tutabeba pia mfano wa mtu wa mbinguni.
50 Ndikunenetsa, abale, kuti thupi ndi magazi sizingathe kulowa mu ufumu wa Mulungu, ndipo zimene zimavunda sizingathe kulowa kumene zinthu sizivunda.
Eshe embabhola kolo na yilombo bhane aje ubele nedanda seviwezizwa aghale umwene uwa Ngolobhe, hata uwanankaye uwaghale wasiunajiha.
51 Tamverani, ndikuwuzeni chinsinsi. Tonse sitidzagona tulo, koma tonse tidzasandulika.
Enye! Embabhola amwe esiri eyelyoli: Hetaifwa ntenti bali tenti bhonti bhaigalunyiwa.
52 Zidzachitika mwadzidzidzi, mʼkamphindi kochepa, monga ngati kuphethira kwa diso, pa lipenga lotsiriza. Pakuti lipenga lidzalira, akufa adzaukitsidwa opanda chovunda, ndipo ife tidzasandulika.
Taigalunyizwa katika uwa sizue na damlehwiliso katika endundwe eyahumalisho, afwatanale endundwe zwailila na bhabhafwiye bhaizwoha nehali eyesitenachishe.
53 Pakuti chovunda chiyenera kuvala chosavunda, ndi thupi ili lakufa liyenera kuvala losafa.
Maana uu wananjishe lazima ukwate waseunanjiha nogu wa fwa lazima ukwate wasegwa fwe.
54 Pamene thupi lovundali likadzasanduka losavunda, ndipo thupi lotha kufali likadzasanduka losatha kufa, pamenepo zidzakwaniritsidwa zimene zinalembedwa zakuti, “Imfa yogonjetsedwa kwathunthu.”
Lelo uwakati owo wa nachishe wakwatiziwa sintenachishe huu uwafwe nkaukwate usintefwe, ndipo gwayenza enjango ambao usibwilwe, “Efwa emililwe katika ashindwe.”
55 “Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
“Efwa umenezwe waho ulihwi? Fwa ulihwi ulwoyo ulihwi?” (Hadēs g86)
56 Ululu wa imfa ndi tchimo, ndipo mphamvu ya tchimo ndi lamulo.
Ulyoyo uwefwa ni ubhibhi na enguvu ye ubhibhi ni sheria.
57 Koma tiyamike Mulungu amene amatipambanitsa mwa Ambuye athu Yesu Khristu.
Lelo ehusalifwa Ungolobhe, atipela ate amene ashilile uGosi wetu uYesu Kristi!
58 Choncho, abale anga okondedwa imani njii. Musasunthike ndi chilichonse. Nthawi zonse mudzipereke kwathunthu ku ntchito ya Ambuye, chifukwa mukudziwa kuti ntchito zanu mwa Ambuye sizili zopanda phindu.
Eshi bhasungwena bhakolo na mwailombo bhanji imara na mgaje ayinje. Antele yibhombi embombo eya Gosi, kwa sababu mumenye aje embombo yenyu katika Gosi sio wene.

< 1 Akorinto 15 >