< 1 Akorinto 11 >

1 Tsatirani chitsanzo changa, monga inenso nditsatira chitsanzo cha Khristu.
Tsikombeo iraho hambañe amy te izaho ka ro mpiamy Norizañey.
2 Ndikukuyamikani chifukwa chondikumbukira pa zonse ndiponso posunga ziphunzitso monga ndinakuphunzitsirani.
Ty andrengeako anahareo ry longo, le t’ie mahatiahy ahy amy ze he’e, naho tambozore’ areo o nafèn-droaeo, ami’ty do’e nitaroñako.
3 Tsopano ndikufuna muzindikire kuti Khristu ndiye mutu wa munthu aliyense, ndipo mwamuna ndiye mutu wamkazi, ndipo mutu wa Khristu ndi Mulungu.
Fa teako ho fohi’ areo te lohà’ ze hene ‘ndaty i Norizañey, le lohà’ ty rakemba ty lahilahy; le lohà’ i Norizañey t’i Andrianañahare.
4 Mwamuna aliyense wopemphera kapena kunenera ataphimba mutu wake akunyoza mutu wakewo.
Toe manalatse ty añambone’e ze lahilahy mikolopoke naho mihalaly ndra mitoky.
5 Ndipo mkazi aliyense wopemphera kapena kunenera asanaphimbe mutu wake sakulemekeza mutu wakewo. Kuli chimodzimodzi kumeta mutu wake.
Fa manalatse ty añambone’e ka ze rakemba tsy mampikolopoke ty añambone’e t’ie miloloke ndra mitoky—fa hambañe amy te niharatse.
6 Ngati mkazi saphimba kumutu kwake, ndiye kuti amete tsitsi lake. Ngati nʼchamanyazi kwa mkazi kungoyepula kapena kumeta mpala, ndiye kuti aphimbe kumutu kwake.
Aa naho tsy mete mikolopo-doha ty rakemba, le hamake te hiharatse. Fe naho maha­salatse i rakembay te ho harateñe ndra hitsifañe le soa re te hikolopo-doha.
7 Mwamuna sayenera kuphimba kumutu popeza ndi chifaniziro ndi ulemerero wa Mulungu; pamene mkazi ndi ulemerero wa mwamuna.
Tsy kolopofa’ ty lahilahy ka ty añambone’e, amy t’ie ty vintan’ Añahare naho ty enge’e; le ty rakemba ro engen-dahilahy.
8 Pakuti mwamuna sachokera kwa mkazi, koma mkazi kwa mwamuna.
(Toe tsy niboak’ami’ty rakemba ty lahilahy, fa ami’ty lahilahy ty rakemba.)
9 Ndipo mwamuna sanalengedwe chifukwa cha mkazi, koma mkazi analengedwera mwamuna.
Eka, tsy nitsenèñe ho a ty rakemba ty lahilahy, fa ty rakemba ho a ty lahilahy.
10 Pa chifukwa ichi, ndiponso pa chifukwa cha angelo, mkazi akuyenera kukhala ndi chizindikiro cha ulamuliro wake.
Ty amy tsraeñey le soa re te añambone’ i rakemba ty viloñe t’ie aman-dily, ty amo anjelio.
11 Komabe mwa Ambuye, mkazi amadalira mwamuna ndipo mwamuna amadalira mkazi.
Ie amy zao, amy Talè ao, le tsy mifampiria ami’ty lahilahy ty rakemba, vaho tsy mihaha ami’ty rakemba ty lahilahy.
12 Pakuti monga mkazi anachokera kwa mwamuna, momwemonso mwamuna anabadwa mwa mkazi. Koma zonse zichokera kwa Mulungu.
Le hambañe amy te boak’ami’ty lahilahy ty rakemba te añamy rakemba ka o lahilahio; vaho kila boak’ aman’ Añahare.
13 Dziweruzeni. Kodi nʼchabwino kuti mkazi apemphere kwa Mulungu wopanda chophimba kumutu?
Mifañaraharà: Mañeva ty rakemba hao ty miloloke aman’ Añahare tsy mikolopoke?
14 Kodi chikhalidwe chathu sichitiphunzitsa kuti nʼchamanyazi kuti mwamuna akhale ndi tsitsi lalitali,
Aa tsy anare’ o sata’ ty tane toio hao te manalatse o lahilahio ty maròy lava?
15 koma mkazi akakhala ndi tsitsi lalitali ndi ulemerero wake? Pakuti mkazi anapatsidwa tsitsi lalitali monga chophimba kumutu.
Fe naho apò’ ty rakemba ho lava ty maroi’e, le enge’e; amy te nitoloreñe aze ho fandrakofañe o maroi’eo.
16 Ngati wina akufuna kutsutsapo pa zimenezi, ife ndiponso mipingo ya Mulungu tilibe machitidwe ena apadera koma ndi omwewa.
Aa naho eo ty te handietse, tsy aman-dilitse ila’e tika ndra o Fivorin’ Añahareo.
17 Koma popereka malangizo awa sindikufuna kukuyamikirani popeza mʼmisonkhano yanu mumachita zoyipa kuposa zabwino.
Fe amo taroñeñe zao, tsy rengeko nahareo; ie tsy mifanontoñe ho ami’ty hasoa, fa ho ami’ty haraty.
18 Choyamba, ndikumva kuti mukasonkhana mu mpingo mumasankhana ndipo ndikukhulupirira kuti zimenezi kwinaku nʼzoona.
Valoha’e, naho mifanontoñe ho Fivory, inao t’ie mifampiriaria, fe mete hiantofako.
19 Nʼzosakayikitsa kuti pali kugawikana pakati panu kuti adziwike amene ndi ovomerezeka ndi Mulungu.
(Toe tsy mahay tsy ama’ areo avao ty fifampitolahañe hampidodeàñe o niventèñe ama’ areoo.)
20 Tsono, mukasonkhana pamodzi, chimene mumadya si Mgonero wa Ambuye.
F’ie mifanontoñe, toe tsy ty hikama i sabadidak’ i Talèy,
21 Pakuti mukamadya, aliyense amangodzidyera zomwe anakonza. Wina amakhala ndi njala pamene wina amaledzera.
f’ie mikama, songa mandrambe ty mahakama’e heike; le ao ty kerè vaho ao ty jike.
22 Kodi mulibe nyumba zanu kumene mungamadyere ndi kumwa? Kapena mumapeputsa mpingo wa Mulungu ndi kuchititsa manyazi amene alibe kalikonse? Ndikunena chiyani kwa inu? Moti ndikuyamikireni pa zimenezi? Ayi, pa zinthu izi sindingakuyamikireni.
Hete! Tsy songa manañe anjomba hao hikamà’e naho hinoma’e? Ke rabioñe’ areo ty Fivorin’ Añahare, naho salare’ areo o rarakeo? Aa ino ty hitaroñako? Ho rengèko amy zay hao nahareo? Tsy hirengèako!
23 Pakuti zimene ndinalandira kwa Ambuye ndi zomwe ndinakupatsani. Ambuye Yesu, usiku umene anaperekedwa uja, anatenga buledi.
Fa rinambeko amy Talè, i nitaro­ñakoy, te nandrambe mofo t’i Talè Iesoà amy haleñe nifoterañe azey;
24 Atayamika ndi kumunyema ananena kuti, “Ili ndi thupi langa lomwe laperekedwa kwa inu; muzichita zimenezi pokumbukira Ine.”
nañandriañe re le finola’e vaho nanao ty hoe: Intoy ty sandriko ho anahareo, anò zao ho fitiahiañe ahy.
25 Chimodzimodzi, atatha kudya, anatenga chikho, nati, “Chikho ichi ndi pangano latsopano la magazi anga; imwani nthawi zonse pokumbukira Ine.”
Hambañ’ amy zay, rinambe’e i fitoviy, ie fa nikama, le nanao ty hoe: Fañina vao ami’ty lioko ty fitovy toy. Anò zao amy fikama’ areo aze ho fitiahiañe ahiko.
26 Pakuti nthawi zonse pamene mudya bulediyu ndikumwa chikhochi, mukulalikira imfa ya Ambuye mpaka Iye adzabweranso.
Aa le amy ikama’ areo ty mofo toy naho inomañe ty fitovy toy, ro mitaroñe ty havilasi’ i Talè ampara’ ty fitotsaha’e.
27 Chifukwa chake, aliyense amene adya buledi kapena kumwa chikho cha Ambuye mʼnjira yosayenera adzachimwira thupi ndi magazi a Ambuye.
Aa ndra ia ia mikama amy mofoy ndra minoñe amy fitovi’ i Talèy ami’ty tsy fañeva’e, le aman-kakeo ami’ty fañòva naho ami’ty lio’ i Talè.
28 Munthu adzisanthule yekha asanadye buledi kapena kumwa chikhochi.
Aa le tsy mete tsy hitso-batañe heike ondatio vaho hikama amy mofoy naho hinoñe amy fitoviy.
29 Popeza aliyense amene adya kapena kumwa mosazindikira thupi la Ambuye, amadya ndi kumwa chiweruzo chake chomwe.
Amy t’ie mikama naho minoñe ro mikama naho minoñe fàtse ami’ty vata’e naho ie tsy maharedreke i fañovay.
30 Nʼchifukwa chake pakati panu ambiri mwa inu ndi ofowoka ndi odwala, ndipo ambirinso agona tulo.
Izay ty mampaifoifo naho mahasiloke maro ama’areo, mbore nampiròtse ty ila’e.
31 Koma tikanadziyesa tokha sitikaweruzidwanso.
Ie mahafitsò-batañe ami’ty hatò tika le tsy ho zakaeñe.
32 Pamene tiweruzidwa ndi Ambuye, ndiye kuti akukonza khalidwe lathu kupewa kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi anthu osakhulupirira.
F’ie zakaeñe, lilove’ i Talè tsy mone hatrao-pàtse ami’ty voatse toy.
33 Ndiye tsono abale anga, pamene musonkhana pa chakudya, mudikirirane.
Ie amy zao, ry longo naho mifanontoñe hikama, mifandiñisa.
34 Ngati wina ali ndi njala, adye ku nyumba kwake kuti pamene musonkhana pamodzi zisafike poti muweruzidwe nazo. Ndipo ndikabwera ndidzakupatsani malangizo ena owonjezera.
Naho eo ty saliko, soa re te hikama añ’anjomba’e añe, tsy mone hivory hafàtse. Halahareko ho anahareo ami’ty fiàviko o raha ila’eo.

< 1 Akorinto 11 >