< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam gendride Seth; Enos,
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Chaynan, Malaleel, Jared,
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch, Matussale, Lameth;
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noe gendride Sem, Cham, and Japhet.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
The sones of Japhat weren Gomer, Magog, Magdai, and Jauan, Tubal, Mosoch, and Tiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
Forsothe the sones of Gomer weren Asceneth, and Riphat, and Thogorma.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
Sotheli the sones of Jauan weren Helisa, and Tharsis, Cethym, and Dodanym.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
The sones of Cham weren Chus, and Mesraym, Phuth, and Chanaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
Sotheli the sones of Chus weren Saba, and Euila, Sabatha, and Regma, and Sabathaca. Forsothe the sones of Regma weren Saba, and Dadan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
Sotheli Chus gendride Nemroth; this Nemroth bigan to be myyti in erthe.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
Forsothe Mesraym gendride Ludym, and Ananyn, and Labaym,
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
and Neptoym, and Phetrusym, and Casluym, of whiche the Philisteis and Capthureis yeden out.
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
Sotheli Chanaan gendride Sidon his first gendrid sone,
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
and Ethei, and Jebusei, and Ammorrei, and Gergesei,
15 Ahivi, Aariki, Asini
and Euei, and Arachei, and Synei,
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
and Aradye, and Samathei, and Emathei.
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
The sones of Sem weren Elam, and Assur, and Arphaxat, and Luth, and Aram. Forsothe the sones of Aram weren Hus, and Hul, and Gothor, and Mosoch.
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
Forsothe Arphaxat gendride Sale; which hym silf gendride Heber.
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
Sotheli to Heber weren borun twei sones; name of oon was Phaleg, for the lond was departid in hise daies; and the name of his brother was Jectan.
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
Forsothe Jectan gendride Elmodad, and Salech, and Aselmod,
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
and Jare, and Adoram, and Vzal,
22 Obali, Abimaeli, Seba,
and Deda, Hebal, and Ameth, and Abymael,
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
and Saba, also and Ophir, and Euila, and Jobab; alle these weren the sones of Jectan.
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Sem, Arphaxat, Sale,
25 Eberi, Pelegi, Reu
Heber, Phalech, Ragau,
26 Serugi, Nahori, Tera
Seruth, Nachor, Thare, Abram;
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
forsothe this is Abraham.
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
The sones of Abraham weren Isaac and Ismael.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
And these the generaciouns of hem; the firste gendrid of Ismael Nabioth, and Cedar, and Abdahel, and Mapsam,
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
and Masma, and Duma, and Massa, Adad, and Themar, Jahur, Naphis, Cedma;
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
these ben the sones of Ismael.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
Forsothe the sones of Cethure, secoundarie wijf of Abraham, whiche sche gendride, weren Zamram, Jersan, Madan, Madian, Jelboe, Sue. Sotheli the sones of Jersan weren Saba, and Dadan. Forsothe the sones of Dadan weren Assurym, and Latusym, and Laomym.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
Sotheli the sones of Madian weren Epha, Ethei, and Enoch, and Abdia, and Heldaa. Alle these weren the sones of Cethure.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
Forsothe Abraham gendride Isaac; whose sones weren Esau and Israel.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
The sones of Esau weren Eliphat, Rahuel, Semyaus, and Elam, and Chore.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
The sones of Eliphath weren Theman, Omer, Sephi, Gethem, Genez, Cenez, Thanna, Amalech.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
The sones of Rahuel weren Naab, Gazara, Samma, Masa.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
The sones of Seir weren Lothan, Sobal, Sebeon, Ana, Dison, Eser, Disan.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
The sones of Lothan weren Horry, Huma; sotheli the sistir of Lothan was Thanna.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
The sones of Sobal weren Alian, and Manaath, and Ebal, and Sephi, and Onam. The sones of Sebeon weren Ana, and Anna. The sone of Ana was Dison.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
The sones of Dison weren Amaram, and Hesabam, and Lecram, and Caram.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
The sones of Eser weren Balaam, and Jaban, and Jesan. The sones of Disan weren Hus and Aram.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
These ben the kyngis that regneden in the lond of Edom, bifor that a kyng was on the sones of Israel. Bale, the sone of Beor; and the name of his citee was Danaba.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
Sotheli Bale was deed; and Jobab, sone of Zare of Basra, regnyde for hym.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
And whanne Jobab was deed, Husam of the lond of Themayns regnede for hym.
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
And Husam diede; and Adad, sone of Badad, that smoot Madian in the lond of Moab, regnyde for hym; and the name of the citee of `hym, that is, of Adad, was Abyud.
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
And whanne Adad was deed, Semela of Maserecha, regnede for hym.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
But also Semela was deed, and Saul of Robooth, which is set bisidis the ryuer, regnyde for hym.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
Also whanne Saul was deed, Balanam, the sone of Achabor, regnyde for him.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
But also he was deed, and Adad, the name of whos citee was Phou, regnede for hym; and his wijf was clepid Methesael, the douyter of Mathred, douyter of Mezaab.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
Forsothe whanne Adad was deed, dukis bigunnen to be in Edom for kyngis; duyk Thanna, duyk Alia, duyk Jetheth,
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
duyk Olibama, duyk Ela, duyk Phynon,
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
duik Ceneth, duyk Theman, duyk Mabsar,
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
duyk Magdiel, duyk Iram. These weren the duykis of Edom.

< 1 Mbiri 1 >