< 1 Mbiri 7 >
1 Ana a Isakara anali awa: Tola, Puwa, Yasubu ndi Simironi ndipo onse analipo anayi.
Quant aux fils d'Issachar, ils étaient quatre: Thola, Phua, Jasub et Sémeron.
2 Ana a Tola ndi awa: Uzi, Refaya, Yerieli, Yahimai, Ibisamu ndi Samueli. Awa anali atsogoleri a mabanja awo. Pa nthawi ya ulamuliro wa Davide zidzukulu za Tola zomwe zinali anthu odziwa kumenya nkhondo zinalipo 22,600.
Fils de Thola: Ozi, Raphaïas, Jeriel, Jamaï, Jémasan et Samuel, chefs des familles issues de Thola; dont le nombre, au temps de David, fut de vingt-deux mille six cents hommes, tous nés forts et vaillants.
3 Mwana wa Uzi anali Izirahiya. Ana a Izirahiya anali: Mikayeli, Obadiya, Yoweli ndi Isiya. Onse asanu anali atsogoleri a mabanja.
Fils d'Ozi: Jezraïe; fils de Jezraïe: Michel, Abdiu, Johel et Jésia; en tout cinq chefs.
4 Monga mwa chiwerengero cha mabanja awo, panali anthu 36,000 odziwa kumenya nkhondo, pakuti iwo anali ndi akazi ndi ana ambiri.
Et avec eux, il y eut dans leurs familles paternelles des hommes nés forts et vaillants, au nombre de trente-six mille en état de porter les armes; Car ils avaient eu beaucoup de femmes et beaucoup d'enfants.
5 Abale awo onse a mʼbanja la Isakara amene anali odziwa kumenya nkhondo analipo 87,000, olembedwa potsata mibado yawo.
Et leurs frères dans toutes les familles d'Issachar, hommes forts et vaillants aussi, étaient quatre-vingt-sept mille; tel fut leur nombre total.
6 Ana atatu a Benjamini anali awa: Bela, Bekeri ndi Yediaeli.
Fils de Benjamin: Balé, Bachir et Jediel; trois.
7 Ana a Bela anali awa: Eziboni, Uzi, Uzieli, Yerimoti ndi Iri. Iwowa anali atsogoleri a mabanja awo ndipo onse pamodzi analipo asanu. Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali anthu 22,034 odziwa kumenya nkhondo.
Fils de Balé: Esebon, Ozi, Oziel, Jerimuth et Uri; cinq. Chefs des familles issues de Balé, au nombre de vingt-deux mille trente-quatre hommes forts et vaillants.
8 Ana a Bekeri anali awa: Zemira, Yowasi, Eliezara, Eliyoenai, Omiri, Yeremoti, Abiya, Anatoti ndi Alemeti. Onsewa anali ana a Bekeri.
Fils de Bachir: Zémira, Joas, Eliézer, Elithénan, Amarias, Jerimuth, Abiud, Anathoth et Eliémeth; voilà tous les fils de Bachir.
9 Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali atsogoleri a mabanja ndi anthu 20,200 odziwa kumenya nkhondo.
Et le nombre des familles dont, selon leur naissance, ils furent les premiers chefs, s'éleva jusqu'à vingt. mille deux cents hommes forts et vaillants.
10 Mwana wa Yediaeli anali Bilihani. Ana a Bilihani anali awa: Yeusi, Benjamini, Ehudi, Kenaana, Zetani, Tarisisi ndi Ahisahara.
Fils de Jediel: Balaan, fils de Balaan; Jaiis, Benjamin, Aoth, Chanana, Zêthan, Tharsi et Achisaar.
11 Ana onsewa a Yediaeli anali atsogoleri a mabanja. Analipo anthu 17,200 amene anali okonzeka kupita ku nkhondo.
Voilà tous les fils de Jediel, vaillants chefs de familles, dont le nombre fut de dix-sept mille deux cents hommes forts et vaillants, en état de porter les armes.
12 Asupi ndi Ahupi anali zidzukulu za Iri, ndipo Ahusimu anali zidzukulu za Aheri.
Saphin et Aphin étaient fils de Hor, et Hasom était fils d'Aor.
13 Ana a Nafutali anali awa: Yahazieli, Guni, Yezeri ndi Salumu, zidzukulu za Biliha.
Fils de Nephtbali: Jasiel, Goni et Aser, Sellom, fils de ce dernier, et Balam son fils.
14 Ana a Manase anali awa: Asirieli ndi mwana amene anabereka kwa mzikazi wake wa ku Aramu. Mzikazi yemweyo anaberekanso Makiri abambo ake a Giliyadi.
Fils de Manassé: Esriel, qu'enfanta sa concubine la Syrienne, qui lui enfanta aussi Machir, père de Galaad.
15 Makiri anatenga mkazi wa banja la Ahupi ndi Asupi. Mlongo wake anali Maaka. Mwana wake wina anali Zelofehadi, amene anabereka ana aakazi okhaokha.
Et Machir maria Aphin et Saphin; sa sœur s'appelait Moocha, et le nom du second fils fut Saphaad; or, Saphaad n'eut que des filles.
16 Maaka mkazi wa Makiri anabereka mwana wamwamuna ndipo anamutcha Perezi. Mʼbale wake anamutcha Seresi, ndipo ana ake anali Ulamu ndi Rakemu.
Et Moocha, femme de Machir, enfanta un fils, et elle le nomma Pharès, et il eut un frère nommé Suros, le même que Galaad, et ses deux fils furent Ulam et Rocom.
17 Mwana wa Ulamu anali Bedani. Awa anali ana a Giliyadi mwana wa Makiri, mwana wa Manase.
Fils d'Ulam: Badam; voilà les fils de Galaad, fils de Machir, fils de Manassé.
18 Mlongo wake Hamoleketi anabereka Isihodi, Abiezeri ndi Mahila.
Et sa sœur Malécheth enfanta Isud, Abiézer et Maéla;
19 Ana a Semida anali: Ahiyani, Sekemu, Likihi ndi Aniyamu.
Et Semira eut pour fils Kim, Sichem, Lacim et Anian.
20 Ana a Efereimu anali awa: Sutela, Beredi, Tahati, Eliada, Tahati,
Fils d'Ephraïm: Sothalath, Barad, Thaath, Elada, Saath,
21 Zabadi, Sutela. Ezeri ndi Eladi anaphedwa ndi anthu a ku Gati, pamene anabwera kudzalanda zoweta zawo.
Zabad, Sothelé, Azer et Eléad. Et des hommes de Geth les tuèrent tous, parce qu'ils s'étaient mis en campagne pour enlever leurs troupeaux.
22 Efereimu, abambo awo, anawalira masiku ambiri, ndipo abale ake anabwera kudzamutonthoza.
Et leur père Ephraïm s'affligea longtemps, et ses frères vinrent le consoler.
23 Kenaka anagona ndi mkazi wake, ndipo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Anamutcha dzina lake Beriya, chifukwa tsoka linagwera banja lake.
Et il s'approcha de sa femme, et elle conçut, et elle eut un fils, et il le nomma Beria, parce que, dit-il, il est venu en ma maison dans notre malheur.
24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera.
Et sa fille s'appelait Saraa, et elle fut de ceux qui survécurent, et elle bâtit Béthoron-la-Haute et Béthoron-la-Basse. Fils d'Ozan: Seïra,
25 Mwana wina wa Efereimu anali Refa amene zidzukulu zake zinali Resefu, Tela, Tahani,
Et Raphé son fils, Saraph et Thaléès ses fils, et Thaen son fils.
26 Ladani, Amihudi, Elisama,
A Laadan, son fils, naquit Amiud, père d'Elisamai,
Père de Nun, père de Josué; tels furent ses fils.
28 Malo amene ankakhala anali Beteli ndi midzi yozungulira, cha kummawa kunali Naarani, Gezeri ndi midzi yake ya kumadzulo ndi Sekemu ndi midzi yake mpaka ku Aya ndi midzi yake.
Et leur demeure était Béthel et ses bourgs, et Noaran à l'est, et à l'occident Gazer et ses bourgs. Et Sichem et ses bourgs, jusqu'à Gazar et ses bourgs,
29 Mʼmbali mwa malire a Manase munali Beti-Seani, Taanaki, Megido ndi Dori, pamodzi ndi midzi yake. Zidzukulu za Yosefe mwana wa Israeli zimakhala mʼmizinda imeneyi.
Et jusqu'aux confins des fils de Manassé, Bethsan et ses bourgs, Thanach et ses bourgs, Mageddo et ses bourgs, Dor et ses bourgs. C'est là qu'étaient établis les fils de Joseph, fils d'Israél.
30 Ana a Aseri anali awa: Imuna, Isiva, Isivi ndi Beriya. Mlongo wawo anali Sera.
Enfants d'Aser: Jemna, Suïa, Isuï, Beria et Soré, sa sœur.
31 Ana a Beriya anali awa: Heberi ndi Malikieli amene anabereka Birizaiti.
Fils de Beria: Haber, Melchiel; ce dernier père de Berthaïth.
32 Heberi anabereka Yafuleti, Someri, Hotamu ndi Suwa, mlongo wawo.
Et Haber engendra Japhlet, Samer, Hothan et Sola, leur sœur.
33 Ana a Yafuleti anali awa: Pasaki, Bimuhali ndi Asivati. Awa anali ana a Yafuleti.
Fils de Japhlet: Phasec, Bamahel et Asith; voilà les fils de Japhlet.
34 Ana a Someri anali awa: Ahi, Rohiga, Yehuba ndi Aramu.
Fils de Samer: Achi, Rooga, Joba et Aram.
35 Ana a mʼbale wake Helemu anali awa: Zofa, Imuna, Selesi ndi Amali.
Fils de son frère Banehelam: Sopha, Imala, Sellés et Amal.
36 Ana a Zofa anali awa: Suwa, Harineferi, Suwali, Beri, Imula,
Fils de Sopha: Sué, Arnaphar, Suda, Barin, Imran,
37 Bezeri, Hodi, Sama, Silisa, Itirani ndi Bera.
Basan, Hod, Sama, Salisa, Jethra et Bééra.
38 Ana a Yeteri anali awa: Yefune, Pisipa ndi Ara.
Fils de 'éther: Jephina, Phaspha et Ara.
39 Ana a Ula anali awa: Ara, Hanieli ndi Riziya.
Fils d'Ola: Orech, Aniel et Rasia;
40 Onsewa anali zidzukulu za Aseri, atsogoleri a mabanja, anthu omveka, ankhondo olimba mtima, ndi akuluakulu pakati pa atsogoleri anzawo. Chiwerengero cha anthu odziwa kumenya nkhondo chomwe chinalembedwa chinali 26,000.
Tels furent les fils d'Aser, tous chefs de familles, dont le nombre fut de vingt-six mille hommes d'élite, forts et vaillants, en état de porter les armes.