< 1 Mbiri 3 >
1 Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa: Woyamba anali Amnoni, amayi ake anali Ahinoamu wa ku Yezireeli; wachiwiri anali Danieli, amayi ake anali Abigayeli wa ku Karimeli;
大衛在希伯崙所生的兒子記在下面:長子暗嫩是耶斯列人亞希暖生的。次子但以利是迦密人亞比該生的。
2 wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri; wachinayi anali Adoniya amayi ake anali Hagiti;
三子押沙龍是基述王達買的女兒瑪迦生的。四子亞多尼雅是哈及生的。
3 wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali; wachisanu ndi chimodzi anali Itireamu, amayi ake anali Egila.
五子示法提雅是亞比她生的。六子以特念是大衛的妻以格拉生的。
4 Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi. Davide analamuliranso mu Yerusalemu kwa zaka 33,
這六人都是大衛在希伯崙生的。大衛在希伯崙作王七年零六個月,在耶路撒冷作王三十三年。
5 ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa: Samua, Sobabu, Natani ndi Solomoni. Ana anayi awa anali a Batisuwa mwana wa Amieli.
大衛在耶路撒冷所生的兒子是示米亞、朔罷、拿單、所羅門。這四人是亞米利的女兒拔‧書亞生的。
6 Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,
還有益轄、以利沙瑪、以利法列、
8 Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.
以利沙瑪、以利雅大、以利法列,共九人。
9 Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.
這都是大衛的兒子,還有他們的妹子她瑪,妃嬪的兒子不在其內。
10 Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu, Rehabiamu anabereka Abiya, Abiya anabereka Asa, Asa anabereka Yehosafati,
所羅門的兒子是羅波安;羅波安的兒子是亞比雅;亞比雅的兒子是亞撒;亞撒的兒子是約沙法;
11 Yehosafati anabereka Yehoramu, Yehoramu anabereka Ahaziya, Ahaziya anabereka Yowasi,
約沙法的兒子是約蘭;約蘭的兒子是亞哈謝;亞哈謝的兒子是約阿施;
12 Yowasi anabereka Amaziya, Amaziya anabereka Azariya, Azariya anabereka Yotamu,
約阿施的兒子是亞瑪謝;亞瑪謝的兒子是亞撒利雅;亞撒利雅的兒子是約坦;
13 Yotamu anabereka Ahazi, Ahazi anabereka Hezekiya, Hezekiya anabereka Manase,
約坦的兒子是亞哈斯;亞哈斯的兒子是希西家;希西家的兒子是瑪拿西;
14 Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.
瑪拿西的兒子是亞們;亞們的兒子是約西亞;
15 Ana a Yosiya anali awa: Yohanani mwana wake woyamba, Yehoyakimu mwana wake wachiwiri, Zedekiya mwana wake wachitatu, Salumu mwana wake wachinayi.
約西亞的長子是約哈難,次子是約雅敬,三子是西底家,四子是沙龍。
16 Ana a Yehoyakimu: Yekoniya ndi Zedekiya mwana wake.
約雅敬的兒子是耶哥尼雅和西底家。
17 Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi: mwana wake Silatieli,
耶哥尼雅被擄。他的兒子是撒拉鐵、
18 Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.
瑪基蘭、毗大雅、示拿薩、耶加米、何沙瑪、尼大比雅。
19 Ana a Pedaya anali awa: Zerubabeli ndi Simei. Ana a Zerubabeli anali awa: Mesulamu ndi Hananiya. Mlongo wawo anali Selomiti.
毗大雅的兒子是所羅巴伯、示每。所羅巴伯的兒子是米書蘭、哈拿尼雅,他們的妹子名叫示羅密。
20 Panalinso ana ena asanu awa: Hasubu, Oheli, Berekiya, Hasabiya ndi Yusabu-Hesedi.
米書蘭的兒子是哈舒巴、阿黑、比利家、哈撒底、于沙‧希悉,共五人。
21 Zidzukulu za Hananiya zinali izi: Pelatiya ndi Yesaiya, ndiponso ana a Refaya, ana a Arinani, ana a Obadiya ndi ana a Sekaniya.
哈拿尼雅的兒子是毗拉提、耶篩亞。還有利法雅的眾子,亞珥難的眾子,俄巴底亞的眾子,示迦尼的眾子。
22 Zidzukulu za Sekaniya zinali izi: Semaya ndi ana ake: Hatusi, Igala, Bariya, Neariya ndi Safati. Onse anali asanu ndi mmodzi.
示迦尼的兒子是示瑪雅;示瑪雅的兒子是哈突、以甲、巴利亞、尼利雅、沙法,共六人。
23 Ana a Neariya anali awa: Eliyoenai, Hezekiya ndi Azirikamu. Onse anali atatu.
尼利雅的兒子是以利約乃、希西家、亞斯利干,共三人。
24 Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu, Yohanani, Delaya ndi Anani, onse anali asanu ndi awiri.
以利約乃的兒子是何大雅、以利亞實、毗萊雅、阿谷、約哈難、第萊雅、阿拿尼,共七人。