< 1 Mbiri 25 >
1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
Además, David y los jefes de los siervos del lugar santo seleccionaron a algunos de los hijos de Asaf y de Hemán y de Jedutún para la obra de los profetas, para hacer melodías con arpas salterios y platillos; y el número de hombres para el trabajo que tenían que hacer era:
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
De los hijos de Asaf: Zacur, José, y Netanias y Asarela; bajo la dirección de Asaf, actuando como un profeta bajo las órdenes del rey;
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
De Jedutún: los seis hijos de Jedutún, Gedalías y Zeri y Jesaias, Simei, Hasabias y Matatias; bajo la dirección de su padre Jedutún quien, actuando como un profeta, acompañado de arpa, alabó y glorificó al Señor.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Los hijos de Hemán: Buquias, Matanias, Uziel, Sebuel, Jeremot, Hananias, Hanani, Eliata, Gidalti y Romanti-ezer, Josbecaza, Maloti, Hotir, Mahaziot;
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Todos estos fueron hijos de Hemán, profeta del rey en las palabras de Dios. Y para hacer grande su poder, Dios le dio a Hemán catorce hijos y tres hijas.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Todos estos, bajo la dirección de su padre, hicieron música en la casa del Señor, con instrumentos de bronce y cuerdas, para la adoración de la casa de Dios; Asaf, Jedutún y Hemán están bajo las órdenes del rey.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Y el número de ellos, con sus hermanos que fueron entrenados y expertos en hacer melodías para el Señor, era de doscientos ochenta y ocho.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Y se hizo una selección de ellos para su trabajo especial, todos con iguales oportunidades, tanto pequeños como excelentes, el maestro como aprendiz.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
Ahora, del grupo de Asaf, el primer nombre que salió fue José; el segundo Gedalias; él y sus hermanos e hijos eran doce;
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
El tercer Zacur, con sus hijos y sus hermanos, doce;
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
La cuarta Izri, con sus hijos y sus hermanos, doce;
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
La quinta Netanias, con sus hijos y sus hermanos, doce;
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
El sexto Buquias, con sus hijos y sus hermanos, doce;
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
El séptimo Jesarela, con sus hijos y sus hermanos, doce;
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
El octavo Jesahias, con sus hijos y sus hermanos, doce;
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
El noveno Matanías, con sus hijos y sus hermanos, doce;
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
El décimo Simei, con sus hijos y sus hermanos, doce;
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
El undécimo Azareel, con sus hijos y sus hermanos, doce;
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
El duodécimo Hasabias, con sus hijos y sus hermanos, doce;
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
El decimotercer Subael, con sus hijos y sus hermanos, doce;
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
La decimocuarta Matatías, con sus hijos y sus hermanos, doce;
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
El decimoquinto Jeremot, con sus hijos y sus hermanos, doce;
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
La decimosexta Hananías, con sus hijos y sus hermanos, doce;
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
El decimoséptimo Josbecasa, con sus hijos y sus hermanos, doce;
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
La decimoctava Hanani, con sus hijos y sus hermanos, doce;
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
El decimonoveno Maloti, con sus hijos y sus hermanos, doce;
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
La vigésima Eliata, con sus hijos y sus hermanos, doce;
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
El vigésimo primero Hotir, con sus hijos y sus hermanos, doce;
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
El vigésimo segundo Gidalti, con sus hijos y sus hermanos, doce;
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
El vigésimo tercer Mahaziot, con sus hijos y sus hermanos, doce;
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
El vigésimo cuarto Romanti-ezer, con sus hijos y sus hermanos, doce.