< 1 Mbiri 25 >

1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
Weiter sonderte David mit den Heeresobersten von den Söhnen Asaphs, Hemans und Jeduthuns diejenigen aus, die auf Zithern, Harfen und mit Zimbeln als Leiter der geistlichen Kunstmusik für den heiligen Dienst tätig waren. Die Zahl der zu diesem Dienst bestellten Männer war folgende:
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
Von den Söhnen Asaphs: Sakkur, Joseph, Nethanja und Asarela, die Söhne Asaphs, unter der Leitung Asaphs, der nach Anweisung des Königs geistliche Kunstmusik darbot.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
Von Jeduthun: Jeduthuns Söhne: Gedalja, Zeri, Jesaja, Hasabja, Matthithja und Simei, zusammen sechs, unter der Leitung ihres Vaters Jeduthun, der zum Lobpreis und zur Verherrlichung des HERRN geistliche Kunstmusik auf der Harfe darbot.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Von Heman: Hemans Söhne: Bukkia, Matthanja, Ussiel, Subael, Jerimoth, Hananja, Hanani, Eliatha, Giddalthi, Romamthi-Eser, Josbekasa, Mallothi, Hothir und Mahasioth.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Diese alle waren Söhne Hemans, des Sehers des Königs, nach der Verheißung Gottes, ihm das Horn zu erhöhen; denn Gott hatte dem Heman vierzehn Söhne und drei Töchter geschenkt.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Diese alle waren unter der Leitung ihres Vaters Asaph beim Gesang im Tempel des HERRN mit Zimbeln, Harfen und Zithern für den Gottesdienst im Tempel nach der Anweisung des Königs, Asaphs, Jeduthuns und Hemans tätig.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Ihre Anzahl, inbegriffen ihre Amtsgenossen, die im Gesang für den HERRN geübt waren, allesamt Künstler, betrug 288.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Als sie nun die Losung zur Feststellung der Reihenfolge ihres Dienstes vornahmen, die jüngeren ganz wie die älteren, die Meister samt den Schülern,
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
fiel das erste Los für Asaph auf Joseph nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf; das zweite auf Gedalja nebst seinen Brüdern und Söhnen, zusammen zwölf;
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
das dritte auf Sakkur nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
das vierte auf Jizri nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
das fünfte auf Nethanja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
das sechste auf Bukkia nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
das siebte auf Jesarela nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
das achte auf Jesaja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
das neunte auf Matthanja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
das zehnte auf Simei nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
das elfte auf Ussiel nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
das zwölfte auf Hasabja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
das dreizehnte auf Subael nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
das vierzehnte auf Matthitja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
das fünfzehnte auf Jeremoth nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
das sechzehnte auf Hananja nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
das siebzehnte auf Josbekasa nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
das achtzehnte auf Hanani nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
das neunzehnte auf Mallothi nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
das zwanzigste auf Eliatha nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
das einundzwanzigste auf Hothir nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
das zweiundzwanzigste auf Giddalthi nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
das dreiundzwanzigste auf Mahasioth nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf;
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
das vierundzwanzigste auf Romamthi-Eser nebst seinen Söhnen und Brüdern, zusammen zwölf.

< 1 Mbiri 25 >