< 1 Mbiri 25 >

1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
Et David et les chefs de l’armée mirent à part pour le service, d’entre les fils d’Asaph et d’Héman et de Jeduthun, ceux qui devaient prophétiser avec des harpes, et des luths, et des cymbales; et le nombre des hommes employés au service était:
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
Des fils d’Asaph: Zaccur, et Joseph, et Nethania, et Ashareéla, fils d’Asaph, sous la direction d’Asaph, qui prophétisait sous la direction du roi.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
De Jeduthun, les fils de Jeduthun: Guedalia, et Tseri, et Ésaïe, Hashabia, et Matthithia, [et Shimhi], six, sous la direction de leur père Jeduthun, qui prophétisait avec la harpe, pour célébrer et louer l’Éternel.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
D’Héman, les fils d’Héman: Bukkija, Matthania, Uziel, Shebuel, et Jerimoth, Hanania, Hanani, Éliatha, Guiddalthi, et Romamthi-Ézer, Joshbekasha, Mallothi, Hothir, Makhazioth:
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
tous ceux-là étaient fils d’Héman, le voyant du roi dans les paroles de Dieu, pour exalter sa puissance; et Dieu donna à Héman 14 fils et trois filles.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
– Tous ceux-là étaient sous la direction de leurs pères, d’Asaph, et de Jeduthun, et d’Héman, dans le chant de la maison de l’Éternel, avec des cymbales, des luths, et des harpes, pour le service de la maison de Dieu, sous la direction du roi.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Et leur nombre, avec leurs frères instruits dans l’art de chanter à l’Éternel, tous les hommes experts, était de 288.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Et ils jetèrent les sorts pour leurs charges, le petit comme le grand, l’homme expert avec le disciple.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
Et le premier sort échut, pour Asaph, à Joseph; à Guedalia, le second; lui et ses frères et ses fils étaient douze.
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
Le troisième, à Zaccur, ses fils et ses frères, douze.
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
Le quatrième, à Jitseri, ses fils et ses frères, douze.
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
Le cinquième, à Nethania, ses fils et ses frères, douze.
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
Le sixième, à Bukkija, ses fils et ses frères, douze.
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
Le septième, à Jeshareéla, ses fils et ses frères, douze.
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
Le huitième, à Ésaïe, ses fils et ses frères, douze.
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
Le neuvième, à Matthania, ses fils et ses frères, douze.
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
Le dixième, à Shimhi, ses fils et ses frères, douze.
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
Le onzième, à Azareël, ses fils et ses frères, douze.
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
Le douzième, à Hashabia, ses fils et ses frères, douze.
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
Le treizième, à Shubaël, ses fils et ses frères, douze.
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
Le quatorzième, à Matthithia, ses fils et ses frères, douze.
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
Le quinzième, à Jerémoth, ses fils et ses frères, douze.
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
Le seizième, à Hanania, ses fils et ses frères, douze.
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
Le dix-septième, à Joshbekasha, ses fils et ses frères, douze.
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
Le dix-huitième, à Hanani, ses fils et ses frères, douze.
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
Le dix-neuvième, à Mallothi, ses fils et ses frères, douze.
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
Le vingtième, à Élijatha, ses fils et ses frères, douze.
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
Le vingt et unième, à Hothir, ses fils et ses frères, douze.
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
Le vingt-deuxième, à Guiddalthi, ses fils et ses frères, douze.
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
Le vingt-troisième, à Makhazioth, ses fils et ses frères, douze.
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
Le vingt-quatrième, à Romamthi-Ézer, ses fils et ses frères, douze.

< 1 Mbiri 25 >