< 1 Mbiri 25 >
1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
David and some of the temple officials (OR, army commanders) chose some of the descendants of Asaph, Heman, and Jeduthun to be in charge of proclaiming God’s messages, and to play harps and lyres and cymbals. This is a list of the men whom they chose for that work:
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
From the sons of Asaph they chose Zaccur, Joseph, Nethaniah, and Aserelah. Asaph supervised them. And the king appointed Asaph to proclaim God’s messages.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
From the sons of Jeduthun they chose six men: Gedaliah, Zeri, Jeshaiah, Shimei, Hashabiah, and Mattithiah. Jeduthun supervised them and also proclaimed God’s messages, playing his harp while he thanked and praised Yahweh.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
From the sons of Heman, who was one of the king’s prophets, they chose Bukkiah, Mattaniah, Uzziel, Shubael, Jerimoth, Hananiah, Hanani, Eliathah, Giddalti, Romamti-Ezer, Joshbekashah, Mallothi, Hothir, and Mahazioth.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
God promised to cause Heman to be strong, so altogether, God have him 14 sons and three daughters.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
All those men were supervised by their fathers while they played music in the temple of Yahweh. They played cymbals, lyres, and harps. And their fathers—Asaph, Jeduthun and Heman—were supervised by the king.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Those men and their relatives were all trained and skilled for playing musical instruments in the temple. That was their work for Yahweh. Including their relatives, there were 288 of them.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
All of them, including ones who were young and those who were old, cast lots to determine what work they would do.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
From the family of Asaph, the first ones selected were Joseph and 12 of his sons and relatives.
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Gedaliah and 12 of his sons and relatives were selected.
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Zaccur and 12 of his sons and relatives were selected.
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Nethaniah and 12 of his sons and relatives were selected.
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Bukkiah and 12 of his sons and relatives were selected.
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Jesarelah and 12 of his sons and relatives were selected.
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Jeshaiah and 12 of his sons and relatives were selected.
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Mattaniah and 12 of his sons and relatives were selected.
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Shimei and 12 of his sons and relatives were selected.
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Azarel and 12 of his sons and relatives were selected.
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Hashabiah and 12 of his sons and relatives were selected.
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Shubael and 12 of his sons and relatives were selected.
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Mattithiah and 12 of his sons and relatives were selected.
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Jerimoth and 12 of his sons and relatives were selected.
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Hananiah and 12 of his sons and relatives were selected.
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Joshbekashah and 12 of his sons and relatives were selected.
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Hanani and 12 of his sons and relatives were selected.
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Mallothi and 12 of his sons and relatives were selected.
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Eliathah and 12 of his sons and relatives were selected.
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Hothir and 12 of his sons and relatives were selected.
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Giddalti and 12 of his sons and relatives were selected.
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
Next, Mahazioth and 12 of his sons and relatives were selected.
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
Next, Romamti-Ezer and 12 of his sons and relatives were selected.