< 1 Mbiri 25 >

1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
David le a sepai jalamkaiten Asaph, Heman chule Jeduthun insungmi chu Kipana thupha sapphong tohthoa semjang gin ngei, tumging chule Khutbeh la lamkai din alhengdoh taove.
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
Asaph chapate Zaccur, Joseph, Nethaniah chule Asarelah in jong a pau maikainan lengpa thupeh dungjuiyin kipana thupha chu alhangsap uve.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
Heduthun chapate, Gedaliah, Zeri, Jeshiah, Shimei, Hashabiah chule Mattithah mi gup cheng hin jong a pau makainan semjang gin ngei, thangvah le vahchoi toh thon kipana thupha sapphong toh thon Pathen athangvah uve.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Heman chapate chu Bukkiah, Mattaniah, Hanani, Eliathah, Giddalti, Romam’ti-e’zer, Joshbekashah, Mallothi, Hothir chule Mahazioth cheng hi ahiuve.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Lengpa Themgao a pang Heman hin Pakaiya a konin chapa Somle li le chanu thum ahing e.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Heman le achapate chu Houin sunga tumging thei, Selangdah gin ngei, Semjang sai chule khutbeh a Pakai vahchoina lamkaiya pang ahiuve. Chule ijakaiyin, Asaph, Jeduthun chule Heman jong lengpa toh aki thukop jing uve.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Amaho insung hi Pakai vahchoi na mun a tumging sai ding mong a hung kitillu ahi. Abonchauvin tumging sai thei cheh mi Jani somget le get alhing uve.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Mi hichengse hi teh le khang hihen jilkung le simlai umlouvin athepna cheh uva apang un chuleh vang kibang in akisan cheh uve.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
Mi jani somget le get ho hin, chapa somle ni cheh in asauvin, hichengse ho hi hop somni le li in aki homson uvin asopite cheng to vang akisan uve. Vang kisan masapen chu Asaph chilhah lah a Joseph le asopite ahiuvin. Anina a vang kisan chu Gedaliah le asopite ahi,
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
athum channa Zaccur,
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
ali channa Zeri,
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
a nga channa Nethaniah,
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
a gup channa Bukkiah,
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
a sagi channa Asarelahz,
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
a get channa Jessiah,
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
a ko channa Mattaniah,
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
a som channa Shimei,
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
a somle khat na Uzziel,
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
a somle ni na Hashabiah,
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
a somle thumna Shubael,
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
a somle li na Mattithiah,
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
a somle nga na Jerimoth,
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
a somle gup na Hannaniah,
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
a somle sagi na Joshbekashah,
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
a somle get na Hanani,
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
a somle ko na Mallothi,
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
a somni na Eliathah,
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
a somni le khat na Hothir,
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
a somni le ni na Giddalti,
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
a somni le thumna Mahazioth,
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
a somni le li na Romamti-ezer.

< 1 Mbiri 25 >