< 1 Mbiri 25 >
1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
Hina bagade Da: ibidi amola Lifai fi ilia fada: i dunu, ilia da Lifai sosogo fi amo A: isa: fe, Hima: ne amola Yediudane amo Godema nodone sia: ne gadosu gilisisu ouligima: ne ilegei. Ilia da Gode Ea sia: olelema: ne ilegei. Amola ilia da sia: olelesea, sani baidama amola giga: mesa duduna ahoanebe ba: mu galu. Godema nodone sia: ne gadosu ouligisu dunu ilia dio amola ilia hawa: hamosu ilegei da hagudu dedei diala: -
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
A: isa: fe egefelali biyaduale amo da Sa: ge, Yousefe, Nedanaia amola A: salila. Ilia ouligisu dunu da A: isa: fe. Da: ibidi da hamoma: ne sia: noba, A:isa: fe da Gode Ea sia: olelelalu.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
Yediudane egefelali gafeyale da Gedalaia, Silai, Yisa: ia, Simiai, Ha: siabaia amola Ma: didaia. Ilia da ilia eda ea sia: nabawane, Gode Ea sia: olelelalu, amola gesa: mi hea: le, Hina Godema nodonanu. Ilia gesami hea: sa gilisili, sani baidama dubi nabi.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Hima: ne egefelali genesi ilia dio da Bagaia, Ma: danaia, Asaiele, Sibiuele, Yelimode, Ha: nanaia, Hana: inai, Ilaida, Gida: ladai, Louma: madisi, Yosiabiga: sia, Ma: loudai, Houdie amola Maha: isiode.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Gode da Ea ilegele sia: i defele, hina bagade ea balofede dunu Hima: ne e gasa fili hamoma: ne, amo dunu mano genesi amola uda mano udiana ema i.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Hima: ne egefe huluane da ilia eda sia: nababeba: le, giga: mesa amola sani baidama amo Debolo nodone sia: ne gadosu amola gesami hea: su fidimusa: dusu. A: sa: fe, Yediudane amola Hima: ne, ilia da hina bagade Da: ibidi ea hamoma: ne sia: i defele hamosu.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Amo dunu 24 agoane da medenegi dunu ba: i. Amola Lifai fi dunu ilima gilisi, huluane da 288 agoane, ilia da dusu liligi dawa: ma: ne, ado boba: i dagoi.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Dunu huluane, ayeligi amola da: i hamoi, medenegi dunu amola buludui dunu, huluane ilia ilegei hawa: hamosu dawa: ma: ne, ululuasu.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
Amo dunu 288 agoane da ilia sosogo fi defele, gilisisu 24 agoane hamoma: ne, momogi ba: i. Gilisisu afae afae ilia idi da fagoane ba: i amola gilisisu afae afaega, ouligisu dunu esalebe ba: i. Ilia da agoane hawa: hamosu. A: isa: fe sosogo fi dunu Yousefe da bisili hawa: hamosu. Amalu Gedalaia, Sa: ge, Isilai, Nedanaia, Bagaia, A:salela, Yisa: ia, Ma: danaia, Simiai, Asaiele, Ha: siabaia, Siuba: iele, Ma: didaia, Yelimode, Ha: nanaia, Yosiabiga: sia, Ha: nani, Ma: loudi, Ilaiada, Houdie, Gida: lidai, Maha: isiode, Louma: madisi.
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.