< 1 Mbiri 24 >
1 Magulu a ana a Aaroni anali awa: Ana a Aaroni anali Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.
Un šī bija Ārona bērnu kārta. Ārona bērni bija: Nadabs un Abijus, Eleazars un Ītamars.
2 Koma Nadabu ndi Abihu anamwalira abambo awo asanamwalire, ndipo analibe ana aamuna. Kotero Eliezara ndi Itamara ankatumikira monga ansembe.
Bet Nadabs un Abijus nomira priekš sava tēva, un tiem bērnu nebija, un Eleazars un Ītamars palika par priesteriem.
3 Mothandizidwa ndi Zadoki chidzukulu cha Eliezara ndi Ahimeleki chidzukulu cha Itamara, Davide anawagawa mʼmagulu molingana ndi ntchito yawo yotumikira.
Un Dāvids tos nodalīja, Cadoku no Eleazara bērniem un Aķimeleku no Ītamara bērniem, pēc viņu kalpošanas kārtas.
4 Atsogoleri ambiri anapezeka pakati pa zidzukulu za Eliezara kusiyana ndi zidzukulu za Itamara ndipo anagawidwa moyenera: atsogoleri 16 a mabanja ochokera kwa Eliezara, ndipo atsogoleri asanu ndi atatu a mabanja ochokera kwa zidzukulu za Itamara.
Un Eleazara bērnos tapa atrastas vairāk vīriešu galvas, nekā Ītamara bērnos, un tie tos nodalīja; no Eleazara bērniem bija sešpadsmit tēvu namu virsnieki, bet no Ītamara bērniem bija astoņi virsnieki pēc saviem tēvu namiem.
5 Anawagawa mosakondera pochita maere, pakuti iwo anali akuluakulu a ku malo opatulika ndi akuluakulu a Mulungu pakati pa zidzukulu za Eliezara ndi Itamara.
Un tos nodalīja caur meslošanu, tā šos kā viņus, jo virsnieki svētā vietā un virsnieki Dieva priekšā bija no Eleazara un Ītamara bērniem.
6 Mlembi Semaya mwana wa Netaneli, Mlevi, analemba mayina awo pamaso pa mfumu ndi akuluakulu ake: wansembe Zadoki, Ahimeleki mwana wa Abiatara ndi atsogoleri a mabanja a ansembe ndiponso Alevi, banja limodzi kuchokera kwa Eliezara kenaka limodzi kuchokera kwa Itamara.
Un Šemaja, Netaneēļa dēls, skrīveris no Levitiem, tos uzrakstīja ķēniņa priekšā un lielkungu un priestera Cadoka un Aķimeleka, Abjatara dēla, un priesteru un Levitu tēvu namu virsnieku priekšā; viens tēva nams tapa ņemts no Eleazara, un viens tāpat tapa ņemts no Ītamara.
7 Maere woyamba anagwera Yehoyaribu, achiwiri anagwera Yedaya,
Un tā pirmā meslu zīme krita Jojaribam, otrā Jedajam,
8 achitatu anagwera Harimu, achinayi anagwera Seorimu,
Trešā Harimam, ceturtā Zeorimam,
9 achisanu anagwera Malikiya, achisanu ndi chimodzi anagwera Miyamini,
Piektā Malhijam, sestā Mejaminam,
10 achisanu ndi chiwiri anagwera Hakozi, achisanu ndi chitatu anagwera Abiya,
Septītā Akocam, astotā Abijam,
11 achisanu ndi chinayi anagwera Yesuwa, a khumi anagwera Sekaniya,
Devītā Jezuam, desmitā Šekanijam,
12 a 11 anagwera Eliyasibu, a 12 anagwera Yakimu,
Vienpadsmitā Eliazibam, divpadsmitā Jaķimam,
13 a 13 anagwera Hupa, a 14 anagwera Yesebeabu,
Trīspadsmitā Upam, četrpadsmitā Jezebeabam,
14 a 15 anagwera Biliga, a 16 anagwera Imeri,
Piecpadsmitā Bilgam, sešpadsmitā Imeram.
15 a 17 anagwera Heziri, a 18 anagwera Hapizezi,
Septiņpadsmitā Heziram, astoņpadsmitā Apicecam,
16 a 19 anagwera Petahiya, a 20 anagwera Ezekieli,
Deviņpadsmitā Petahjam, divdesmitā Jezķelim,
17 a 21 anagwera Yakini, a 22 anagwera Gamuli,
Divdesmit pirmā Jaķinam, divdesmit otrā Gamulam,
18 a 23 anagwera Delaya, ndipo a 24 anagwera Maaziya.
Divdesmit trešā Delajam, divdesmit ceturtā Maāzijam.
19 Umu ndi mmene anasankhidwira kuti azigwira ntchito yotumikira pamene alowa mʼNyumba ya Yehova, motsatira dongosolo limene anapatsidwa ndi kholo lawo Aaroni, monga momwe Yehova Mulungu wa Israeli anamulamulira.
Šī ir viņu kalpošanas kārta, iet Tā Kunga namā pēc sava likuma caur Āronu, savu tēvu, kā tam Tas Kungs, Israēla Dievs, bija pavēlējis.
20 Za zidzukulu zina zonse za Levi: Kuchokera kwa ana a Amramu: Subaeli; kuchokera kwa ana a Subaeli: Yehideya.
Un no tiem citiem Levja bērniem: no Amrama bērniem bija Zubaēls, no Zubaēla bērniem Jekdeja.
21 Kwa Rehabiya, kuchokera kwa ana ake: Mtsogoleri anali Isiya.
No Rekabejas: Rekabejas bērniem virsnieks bija Jezija.
22 Kuchokera ku banja la Izihari: Selomoti; kuchokera kwa ana a Selomoti: Yahati.
No Jeceara bērniem bija Zalomots, no Zalamota bērniem Jakats.
23 Ana a Hebroni: woyamba anali Yeriya, wachiwiri anali Amariya, wachitatu anali Yahazieli ndipo Yekameamu anali wachinayi.
Un no (Hebrona) bērniem bija: Jerijus (pirmais), Amarija otrais, Jaēziēls trešais, Jakmeams ceturtais.
24 Mwana wa Uzieli: Mika; kuchokera kwa ana a Mika: Samiri.
Uziēļa bērni Miha: no Mihas bērniem: Zamirs.
25 Mʼbale wa Mika: Isiya; kuchokera kwa ana a Isiya: Zekariya.
Mihas brālis bija Jezija: no Jezijas bērniem: Zaharija.
26 Ana a Merari: Mahili ndi Musi. Mwana wa Yaaziya: Beno.
Merarus bērni bija: Maēlus un Muzus; tā dēls Jaēzija.
27 Ana a Merari: Kuchokera kwa Yaaziya: Beno, Sohamu, Zakuri ndi Ibiri.
Merarus bērni no Jaēzijas, viņa dēla, bija: Zoams un Zakurs un Jbrus.
28 Kuchokera kwa Mahili: Eliezara, amene analibe ana aamuna.
No Maēlus bija Eleazars; tam nebija bērnu.
29 Kuchokera kwa Kisi: Mwana wa Kisi: Yerahimeeli.
No Ķisa: Ķisa bērni: Jerameēls.
30 Ndipo ana a Musi: Mahili, Ederi ndi Yerimoti. Awa anali Alevi potsata mabanja a makolo awo.
Un Muzus bērni bija: Maēlus un Eders un Jeremots. Šie ir Levitu bērni pēc saviem tēvu namiem.
31 Iwonso anachita maere, monga anachitira abale awo, zidzukulu za Aaroni, pamaso pa mfumu Davide, ndi Zadoki ndi Ahimeleki, atsogoleri a mabanja a ansembe ndi Alevi. Mabanja a mwana wamkulu anachita nawo mofanana ndi a mwana wamngʼono.
Un priekš tiem tapa arī meslots, tāpat tā priekš viņu brāļiem, Ārona dēliem, ķēniņa Dāvida priekšā un Cadoka un Aķimeleka un priesteru un Levitu tēvu namu virsnieku priekšā, tā tēvu nama virsniekam, kā mazākam brālim.