< 1 Mbiri 2 >

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
Estos son los hijos de Israel: Rubén, Simeón, Leví, Judá, Isacar, Zabulón,
2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Dan, José, Benjamín, Neftalí, Gad y Aser.
3 Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
Los hijos de Judá: Er, Onán y Sala, los tres que le nacieron de la hija de Súa, la cananea. Er, el primogénito de Judá, fue malvado a los ojos de Yahvé; y lo mató.
4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
Tamar, su nuera, le dio a luz a Fares y a Zéraj. Todos los hijos de Judá fueron cinco.
5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
Los hijos de Fares: Esrom y Hamul.
6 Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
Los hijos de Zera: Zimri, Etán, Hemán, Calcol y Dara: cinco en total.
7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
Los hijos de Carmi: Acar, el perturbador de Israel, que cometió una infracción en la cosa consagrada.
8 Mwana wa Etani anali Azariya.
El hijo de Etán: Azarías.
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
También los hijos de Esrom, que le nacieron: Jerajmeel, Ram y Quelubai.
10 Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
Ram fue padre de Aminadab, y Aminadab fue padre de Naasón, príncipe de los hijos de Judá;
11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
y Naasón fue padre de Salma, y Salma fue padre de Booz,
12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
y Booz fue padre de Obed, y Obed fue padre de Isaí
13 Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
e Isaí fue padre de su primogénito Eliab, Abinadab el segundo, Simea el tercero,
14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
Netanel el cuarto, Raddai el quinto,
15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
Ozem el sexto y David el séptimo;
16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
y sus hermanas fueron Zeruiah y Abigail. Los hijos de Sarvia: Abisai, Joab y Asael, tres.
17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
Abigail dio a luz a Amasa, y el padre de Amasa fue Jeter, el ismaelita.
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
Caleb, hijo de Esrom, fue padre de hijos de Azubá, su mujer, y de Jeriot; y estos fueron sus hijos Jesher, Shobab y Ardón.
19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
Murió Azubá, y Caleb se casó con Efrat, que le dio a luz a Hur.
20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
Hur fue el padre de Uri, y Uri fue el padre de Bezalel.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
Después, Esrom se acercó a la hija de Maquir, padre de Galaad, a la que tomó como esposa cuando tenía sesenta años, y ella le dio a luz a Segub.
22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
Segub fue el padre de Jair, quien tuvo veintitrés ciudades en la tierra de Galaad.
23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
Gesur y Aram les arrebataron las ciudades de Jair, con Kenat y sus aldeas, hasta sesenta ciudades. Todos estos fueron los hijos de Maquir, padre de Galaad.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
Después de la muerte de Esrom en Caleb Efrata, Abías, mujer de Esrom, le dio a luz a Ashur, padre de Tecoa.
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
Los hijos de Jerajmeel, primogénito de Esrom, fueron Rama el primogénito, Buna, Orén, Ozem y Ahías.
26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
Jerajmeel tuvo otra esposa que se llamaba Atará. Ella fue la madre de Onam.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
Los hijos de Ram, primogénito de Jerajmeel, fueron Maaz, Jamín y Eker.
28 Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
Los hijos de Onam fueron Shammai y Jada. Los hijos de Shammai: Nadab y Abisur.
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
La mujer de Abisur se llamaba Abihail, y dio a luz a Ahban y a Molid.
30 Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
Los hijos de Nadab: Seled y Appaim; pero Seled murió sin hijos.
31 Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
El hijo de Appaim: Ishi. El hijo de Ishi: Sesán. El hijo de Sesán: Ahlai.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
Los hijos de Jada, hermano de Shammai: Jeter y Jonatán; pero Jeter murió sin hijos.
33 Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
Los hijos de Jonatán: Pelet y Zaza. Estos fueron los hijos de Jerajmeel.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
Sesán no tuvo hijos, sino sólo hijas. Sesán tenía un sirviente, un egipcio, que se llamaba Jarha.
35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
Sesán dio su hija a Jarha, su siervo, como esposa, y ella le dio a luz a Atai.
36 Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
Atai fue padre de Natán, y Natán fue padre de Zabad,
37 Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
y Zabad fue padre de Eflal, y Eflal fue padre de Obed,
38 Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
y Obed fue padre de Jehú, y Jehú fue padre de Azarías
39 Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
y Azarías fue padre de Helez, y Helez fue padre de Eleasah,
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
y Eleasah fue padre de Sismai, y Sismai fue padre de Sallum,
41 Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
y Sallum fue padre de Jekamiah, y Jekamiah fue padre de Elishama.
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
Los hijos de Caleb, hermano de Jerajmeel, fueron Mesá, su primogénito, que fue padre de Zif, y los hijos de Maresá, padre de Hebrón.
43 Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
Los hijos de Hebrón: Coré, Tapú, Recem y Sema.
44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
Sema fue el padre de Raham, el padre de Jorkeam; y Rekem fue el padre de Shammai.
45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
El hijo de Samai fue Maón; y Maón fue el padre de Bet Zur.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
Efá, concubina de Caleb, dio a luz a Harán, Moza y Gazez; y Harán fue padre de Gazez.
47 Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
Los hijos de Jahdai: Regem, Jotán, Gesán, Pelet, Efá y Shaaf.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
Maaca, concubina de Caleb, dio a luz a Seber y a Tirana.
49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
También dio a luz a Shaaf, padre de Madmaná, a Sheva, padre de Macbena, y al padre de Gbea; y la hija de Caleb fue Acsa.
50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
Estos fueron los hijos de Caleb, hijo de Hur, primogénito de Efrata: Sobal, padre de Quiriat Jearim,
51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
Salma, padre de Belén, y Haref, padre de Bet Gader.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
Sobal, padre de Quiriat Jearim, tuvo hijos: Haroeh, la mitad de los Menuhoth.
53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
Las familias de Quiriat Jearim: los itritas, los putitas, los shumatitas y los misraítas; de ellos salieron los zoratitas y los eshtaolitas.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
Los hijos de Salma: Belén, los netofatitas, Atrot Bet Joab, y la mitad de los manaítas, los zoritas.
55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
Las familias de escribas que vivían en Jabes: los tiratitas, los simeatitas y los sucatitas. Estos son los ceneos que vinieron de Hamat, el padre de la casa de Recab.

< 1 Mbiri 2 >