< 1 Mbiri 2 >

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
Or les fils d’Israël sont: Ruben, Siméon, Lévi, Juda, Issachar et Zabulon,
2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Dan, Joseph, Benjamin, Nephthali, Gad et Aser.
3 Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
Les fils de Juda: Her, Onan et Séla; ces trois lui naquirent de la fille de Sué, Ghananéenne. Mais Her, le premier-né de Juda, fut méchant devant le Seigneur, qui le frappa de mort.
4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
Or Thamar, belle-fille de Juda, lui enfanta Pharès et Zara. Tous les fils de Juda furent au nombre de cinq.
5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
Pharès eut deux fils: Hesron et Hamul.
6 Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
Et les fils de Zara furent Zamri, Ethan, Eman, ainsi que Chalchal et Dara; cinq en tout.
7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
Les fils de Charmi: Achar, qui troubla Israël, et pécha par le larcin de l’anathème;
8 Mwana wa Etani anali Azariya.
Les fils d’Ethan, Azarias;
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
Mais les fils d’Hesron, qui lui naquirent: Jéraméel, Ram, et Calubi.
10 Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
Or Ram engendra Aminadab; Aminadab engendra Nahasson, prince des fils de Juda.
11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
Nahasson aussi engendra Salma, duquel est né Booz.
12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
Or Booz engendra Obed, qui lui-même engendra Isaï.
13 Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
Mais Isaï engendra son premier-né Eliab; le second, Abinabad; le troisième, Simmaa;
14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
Le quatrième, Nathanaël; le cinquième, Raddaï;
15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
Le sixième, Asom; le septième, David;
16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
Dont les sœurs furent Sarvia et Abigaïl; les fils de Sarvia, trois: Abisaï, Joab et Asaël.
17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
Or Abigaïl enfanta Amasa, dont le père fut Jéther, l’Ismahélite.
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
Or Caleb, fils d’Hesron, prit une femme du nom d’Azuba, dont il engendra Jérioth; et ses fils furent Jaser, Sobab et Ardon.
19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
Mais lorsque Azuba fut morte, Caleb prit pour femme Ephratha, qui lui enfanta Hur.
20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
Or Hur engendra Uri; et Uri engendra Bézéléel.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
Après cela, Hesron s’unit à la fille de Machir, père de Galaad; et il la prit, lorsqu’il avait soixante ans: elle lui enfanta Ségub.
22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
Mais Ségub aussi engendra Jaïr; et il posséda vingt-trois villes dans la terre de Galaad.
23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
Et Gessur et Aram prirent les villes de Jaïr, et Canath, et ses bourgades, soixante villes. Tous ceux-là étaient les fils de Machir, père de Galaad.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
Mais après qu’Hesron fut mort, Caleb s’unit à Ephratha; Hesron eut encore pour femme Abia, qui lui enfanta Ashur, père de Thécua.
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
Or il naquit des fils à Jéraméel, premier-né d’Hesron: Ram, son premier-né, ensuite Buna, Aram, Asom et Achia.
26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
Et Jéraméel prit encore une autre femme: Atara, qui fut mère d’Onam.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
Mais, de plus, les fils de Ram, fils aîné de Jéraméel, furent Moos, Jamin et Achar.
28 Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
Or Onam eut pour fils Séméi et Jada. Les fils de Séméi sont Nadab et Abisur.
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
Et le nom de la femme d’Abisur était Abihaïl, laquelle lui enfanta Ahobban et Molid.
30 Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
Or les fils de Nadab furent Saled et Apphaïm. Quant à Saled, il mourut sans enfants.
31 Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
Mais le fils d’Apphaïm fut Jési; lequel Jési engendra Sésan. Or Sésan engendra Oholaï.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
Et les fils de Jada, frère de Séméi, furent Jéther et Jonathan. Mais Jéther aussi mourut sans enfants.
33 Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
Or Jonathan engendra Phaleth et Ziza. Voilà quels ont été les fils de Jéraméel.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
Pour Sésan, il n’eut point de fils, mais des filles, et un esclave égyptien nommé Jéraa,
35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
Et il lui donna sa fille pour femme, laquelle lui enfanta Ethéi.
36 Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
Or Ethéi engendra Nathan, et Nathan engendra Zabad.
37 Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
Zabad aussi engendra Ophlal, et Ophlal engendra Obed.
38 Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
Obed engendra Jéhu, Jéhu engendra Azarias.
39 Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
Azarias engendra Hellès, et Hellès engendra Elasa.
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
Elasa engendra Sisamoï; Sisamoï engendra Sellum.
41 Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
Sellum engendra Icamia, mais Icamia engendra Elisama.
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
Or les fils de Caleb, frère de Jéraméel, furent Mésa, son premier-né; c’est le père de Ziph, et les fils de Marésa, père d’Hébron;
43 Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
Et les fils d’Hébron furent Coré, Taphua, Récem et Samma.
44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
Or Samma engendra Rahani, père de Jercaam, et Récem engendra Sammaï.
45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
Le fils de Sammaï fut Maon, et Maon fut père de Bethsur.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
Or Epha, femme du second rang de Caleb, enfanta Haran, Mosa et Gézez. Et Haran engendra Gézez.
47 Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
Mais les fils de Jahaddaï furent Régom, Joathan, Gésan, Phalet, Epha et Saaph.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
Maacha, femme du second rang de Caleb, enfanta Saber, et Tharana.
49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
Mais Saaph, père de Madména, engendra Sué, père de Machbéna, et père de Gabaa. Or la fille de Caleb fut Achsa,
50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
Voici quels furent les fils de Caleb, fils d’Hur, premier-né d’Ephratha: Sobal, père de Cariathiarim;
51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
Salma, père de Bethléhem; Hariph, père de Bethgader.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
Or Sobal, père de Cariathiarim, eut des fils. Il voyait la moitié des lieux de repos.
53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
Et des familles de Cariathiarim sont venus les Jéthréens, les Aphuthéens, les Sémathéens, les Maséréens. C’est d’eux que sont sortis les Saraïtes et les Esthaolites.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
Les fils de Salma, Bethléhem et Nétophathi, les Couronnes de la maison de Joab, et la Moitié du lieu de repos de Saraï.
55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
Et les familles des scribes habitant à Jabès, chantant et jouant des instruments, et demeurant dans des tabernacles. Ce sont les Cinéens, qui sont venus de Calor, père de la maison de Réchab.

< 1 Mbiri 2 >