< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
アダム、セツ、エノス、
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
ケナン、マハラレル、ヤレド、
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
エノク、メトセラ、ラメク、
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
ノア、セム、ハム、ヤペテ。
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
ヤペテの子らはゴメル、マゴグ、マダイ、ヤワン、トバル、メセク、テラス。
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
ゴメルの子らはアシケナズ、デパテ、トガルマ。
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
ヤワンの子らはエリシャ、タルシシ、キッテム、ロダニム。
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
ハムの子らはクシ、エジプト、プテ、カナン。
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
クシの子らはセバ、ハビラ、サブタ、ラアマ、サブテカ。ラアマの子らはシバとデダン。
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
クシはニムロデを生んだ。ニムロデは初めて世の権力ある者となった。
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
エジプトはルデびと、アナムびと、レハブびと、ナフトびと、
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
パテロスびと、カスルびと、カフトルびとを生んだ。カフトルびとからペリシテびとが出た。
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
カナンは長子シドンとヘテを生んだ。
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
またエブスびと、アモリびと、ギルガシびと、
15 Ahivi, Aariki, Asini
ヒビびと、アルキびと、セニびと、
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
アルワデびと、ゼマリびと、ハマテびとを生んだ。
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
セムの子らはエラム、アシュル、アルパクサデ、ルデ、アラム、ウズ、ホル、ゲテル、メセクである。
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
アルパクサデはシラを生み、シラはエベルを生んだ。
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
エベルにふたりの子が生れた。ひとりの名はペレグ彼の代に地の民が散り分れたからであるその弟の名はヨクタンといった。
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
ヨクタンはアルモダデ、シャレフ、ハザル・マウテ、エラ、
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
ハドラム、ウザル、デクラ、
22 Obali, Abimaeli, Seba,
エバル、アビマエル、シバ、
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
オフル、ハビラ、ヨバブを生んだ。これらはみなヨクタンの子である。
24 Semu, Aripakisadi, Sela
セム、アルパクサデ、シラ、
25 Eberi, Pelegi, Reu
エベル、ペレグ、リウ、
26 Serugi, Nahori, Tera
セルグ、ナホル、テラ、
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
アブラムすなわちアブラハムである。
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
アブラハムの子らはイサクとイシマエルである。
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
彼らの子孫は次のとおりである。イシマエルの長子はネバヨテ、次はケダル、アデビエル、ミブサム、
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
ミシマ、ドマ、マッサ、ハダデ、テマ、
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
エトル、ネフシ、ケデマ。これらはイシマエルの子孫である。
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
アブラハムのそばめケトラの子孫は次のとおりである。彼女はジムラン、ヨクシャン、メダン、ミデアン、イシバク、シュワを産んだ。ヨクシャンの子らはシバとデダンである。
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
ミデアンの子らはエパ、エペル、ヘノク、アビダ、エルダア。これらはみなケトラの子孫である。
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
アブラハムはイサクを生んだ。イサクの子らはエサウとイスラエル。
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
エサウの子らはエリパズ、リウエル、エウシ、ヤラム、コラ。
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
エリパズの子らはテマン、オマル、ゼピ、ガタム、ケナズ、テムナ、アマレク。
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
リウエルの子らはナハテ、ゼラ、シャンマ、ミッザ。
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
セイルの子らはロタン、ショバル、ヂベオン、アナ、デション、エゼル、デシャン。
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
ロタンの子らはホリとホマム。ロタンの妹はテムナ。
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
ショバルの子らはアルヤン、マナハテ、エバル、シピ、オナム。ヂベオンの子らはアヤとアナ。
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
アナの子はデション。デションの子らはハムラン、エシバン、イテラン、ケラン。
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
エゼルの子らはビルハン、ザワン、ヤカン。デシャンの子らはウズとアラン。
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
イスラエルの人々を治める王がまだなかった時、エドムの地を治めた王たちは次のとおりである。ベオルの子ベラ。その都の名はデナバといった。
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
ベラが死んで、ボズラのゼラの子ヨバブが代って王となった。
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
ヨバブが死んで、テマンびとの地のホシャムが代って王となった。
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
ホシャムが死んで、ベダテの子ハダデが代って王となった。彼はモアブの野でミデアンを撃った。彼の都の名はアビテといった。
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
ハダデが死んで、マスレカのサムラが代って王となった。
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
サムラが死んで、ユフラテ川のほとりのレホボテのサウルが代って王となった。
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
サウルが死んで、アクボルの子バアル・ハナンが代って王となった。
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
バアル・ハナンが死んで、ハダデが代って王となった。彼の都の名はパイといった。彼の妻はマテレデの娘であって、名をメヘタベルといった。マテレデはメザハブの娘である。
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
ハダデも死んだ。エドムの族長は、テムナ侯、アルヤ侯、エテテ侯、
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
アホリバマ侯、エラ侯、ピノン侯、
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
ケナズ侯、テマン侯、ミブザル侯、
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
マグデエル侯、イラム侯。これらはエドムの族長である。

< 1 Mbiri 1 >