< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam, Seth, Enosh,
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Kenan, Mahalalel, Jared,
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch, Methuselah, Lamech,
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noah, Shem, Ham, and Japheth.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
The sons of Japheth: Gomer, Magog, Madai, Javan, Tubal, Meshech, and Tiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
The sons of Gomer: Ashkenaz, Diphath, and Togarmah.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
The sons of Javan: Elishah, Tarshish, Kittim, and Rodanim.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
The sons of Ham: Cush, Mizraim, Put, and Canaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
The sons of Cush: Seba, Havilah, Sabta, Raama, Sabteca. The sons of Raamah: Sheba and Dedan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
Cush became the father of Nimrod. He began to be a mighty one in the earth.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
Mizraim became the father of Ludim, Anamim, Lehabim, Naphtuhim,
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
Pathrusim, Casluhim (where the Philistines came from), and Caphtorim.
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
Canaan became the father of Sidon his firstborn, Heth,
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
the Jebusite, the Amorite, the Girgashite,
15 Ahivi, Aariki, Asini
the Hivite, the Arkite, the Sinite,
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
the Arvadite, the Zemarite, and the Hamathite.
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
The sons of Shem: Elam, Asshur, Arpachshad, Lud, Aram, Uz, Hul, Gether, and Meshech.
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
Arpachshad became the father of Shelah, and Shelah became the father of Eber.
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
To Eber were born two sons: the name of the one was Peleg, for in his days the earth was divided; and his brother’s name was Joktan.
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
Joktan became the father of Almodad, Sheleph, Hazarmaveth, Jerah,
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
Hadoram, Uzal, Diklah,
22 Obali, Abimaeli, Seba,
Ebal, Abimael, Sheba,
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
Ophir, Havilah, and Jobab. All these were the sons of Joktan.
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Shem, Arpachshad, Shelah,
25 Eberi, Pelegi, Reu
Eber, Peleg, Reu,
26 Serugi, Nahori, Tera
Serug, Nahor, Terah,
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
Abram (also called Abraham).
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
The sons of Abraham: Isaac and Ishmael.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
These are their generations: the firstborn of Ishmael, Nebaioth; then Kedar, Adbeel, Mibsam,
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
Mishma, Dumah, Massa, Hadad, Tema,
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
Jetur, Naphish, and Kedemah. These are the sons of Ishmael.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
The sons of Keturah, Abraham’s concubine: she bore Zimran, Jokshan, Medan, Midian, Ishbak, and Shuah. The sons of Jokshan: Sheba and Dedan.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
The sons of Midian: Ephah, Epher, Hanoch, Abida, and Eldaah. All these were the sons of Keturah.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
Abraham became the father of Isaac. The sons of Isaac: Esau and Israel.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
The sons of Esau: Eliphaz, Reuel, Jeush, Jalam, and Korah.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
The sons of Eliphaz: Teman, Omar, Zephi, Gatam, Kenaz, Timna, and Amalek.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
The sons of Reuel: Nahath, Zerah, Shammah, and Mizzah.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
The sons of Seir: Lotan, Shobal, Zibeon, Anah, Dishon, Ezer, and Dishan.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
The sons of Lotan: Hori and Homam; and Timna was Lotan’s sister.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
The sons of Shobal: Alian, Manahath, Ebal, Shephi, and Onam. The sons of Zibeon: Aiah and Anah.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
The son of Anah: Dishon. The sons of Dishon: Hamran, Eshban, Ithran, and Cheran.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
The sons of Ezer: Bilhan, Zaavan, and Jaakan. The sons of Dishan: Uz and Aran.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
Now these are the kings who reigned in the land of Edom, before any king reigned over the children of Israel: Bela the son of Beor; and the name of his city was Dinhabah.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
Bela died, and Jobab the son of Zerah of Bozrah reigned in his place.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
Jobab died, and Husham of the land of the Temanites reigned in his place.
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
Husham died, and Hadad the son of Bedad, who struck Midian in the field of Moab, reigned in his place; and the name of his city was Avith.
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
Hadad died, and Samlah of Masrekah reigned in his place.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
Samlah died, and Shaul of Rehoboth by the River reigned in his place.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
Shaul died, and Baal Hanan the son of Achbor reigned in his place.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
Baal Hanan died, and Hadad reigned in his place; and the name of his city was Pai. His wife’s name was Mehetabel, the daughter of Matred, the daughter of Mezahab.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
Then Hadad died. The chiefs of Edom were: chief Timna, chief Aliah, chief Jetheth,
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
chief Oholibamah, chief Elah, chief Pinon,
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
chief Kenaz, chief Teman, chief Mibzar,
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
chief Magdiel, and chief Iram. These are the chiefs of Edom.

< 1 Mbiri 1 >