< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam Seth Enosh.
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Kenan Mahalalel Jared.
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch Methuselah Lamech.
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noah Shem Ham and Japheth.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
[the] sons of Japheth Gomer and Magog and Madai and Javan and Tubal and Meshech and Tiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
And [the] sons of Gomer Ashkenaz and Diphath and Togarmah.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
And [the] sons of Javan [were] Elishah and Tarshish Kittim and Rodanim.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
[the] sons of Ham Cush and Mizraim Put and Canaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
And [the] sons of Cush Seba and Havilah and Sabta and Raamah and Sabteca and [the] sons of Raamah Sheba and Dedan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
And Cush he fathered Nimrod he he began to be a mighty [man] on the earth.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
And Mizraim he fathered ([the] Ludites *Q(K)*) and [the] Anamites and [the] Lehabites and [the] Naphtuhites.
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
And [the] Pathrusites and [the] Casluhites whom they came forth from there [the] Philistines and [the] Caphtorites.
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
And Canaan he fathered Sidon firstborn his and Heth.
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
And the Jebusite[s] and the Amorite[s] and the Girgashite[s].
15 Ahivi, Aariki, Asini
And the Hivite[s] and the Arkite[s] and the Sinite[s].
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
And the Arvadite[s] and the Zemarite[s] and the Hamathite[s].
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
[the] sons of Shem Elam and Asshur and Arphaxad and Lud and Aram and Uz and Hul and Gether and Meshech.
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
And Arphaxad he fathered Shelah and Shelah he fathered Eber.
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
And to Eber it was born two sons [the] name of one [was] Peleg for in days his it was divided the earth and [the] name of brother his [was] Joktan.
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
And Joktan he fathered Almodad and Sheleph and Hazarmaveth and Jerah.
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
And Hadoram and Uzal and Diklah.
22 Obali, Abimaeli, Seba,
And Ebal and Abimael and Sheba.
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
And Ophir and Havilah and Jobab all these [were] [the] sons of Joktan.
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Shem - Arphaxad Shelah.
25 Eberi, Pelegi, Reu
Eber Peleg Reu.
26 Serugi, Nahori, Tera
Serug Nahor Terah.
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
Abram he [is] Abraham.
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
[the] sons of Abraham Isaac and Ishmael.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
These [were] generations their [the] firstborn of Ishmael Nebaioth and Kedar and Adbeel and Mibsam.
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
Mishma and Dumah Massa Hadad and Tema.
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
Jetur Naphish and Kedemah these they [were] [the] sons of Ishmael.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
And [the] sons of Keturah [the] concubine of Abraham she bore Zimran and Jokshan and Medan and Midian and Ishbak and Shuah and [the] sons of Jokshan Sheba and Dedan.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
And [the] sons of Midian Ephah and Epher and Hanoch and Abida and Eldaah all these [were] [the] sons of Keturah.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
And he fathered Abraham Isaac. [the] sons of Isaac Esau and Israel.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
[the] sons of Esau Eliphaz Reuel and Jeush and Jalam and Korah.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
[the] sons of Eliphaz Teman and Omar Zephi and Gatam Kenaz and Timna and Amalek.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
[the] sons of Reuel Nahath Zerah Shammah and Mizzah.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
And [the] sons of Seir Lotan and Shobal and Zibeon and Anah and Dishon and Ezer and Dishan.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
And [the] sons of Lotan Hori and Homam and [was] [the] sister of Lotan Timna.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
[the] sons of Shobal Alyan and Manahath and Ebal Shephi and Onam. And [the] sons of Zibeon Aiah and Anah.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
[the] sons of Anah Dishon. And [the] sons of Dishon Hamran and Eshban and Ithran and Keran.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
[the] sons of Ezer Bilhan and Zaavan Jaakan [the] sons of Dishon Uz and Aran.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
And these [were] the kings who they reigned in [the] land of Edom before reigned a king of [the] people of Israel Bela [the] son of Beor and [the] name of city his [was] Dinhabah.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
And he died Bela and he reigned in place of him Jobab [the] son of Zerah from Bozrah.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
And he died Jobab and he reigned in place of him Husham from [the] land of the Temanite[s].
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
And he died Husham and he reigned in place of him Hadad [the] son of Bedad who struck down Midian in [the] region of Moab and [the] name of city his ([was] Avith. *Q(K)*)
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
And he died Hadad and he reigned in place of him Samlah from Masrekah.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
And he died Samlah and he reigned in place of him Shaul from Rehoboth the river.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
And he died Shaul and he reigned in place of him Baal-Hanan [the] son of Achbor.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
And he died Baal-Hanan and he reigned in place of him Hadad and [the] name of city his [was] Pai and [the] name of wife his [was] Mehetabel [the] daughter of Matred [the] daughter of Me-Zahab.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
And he died Hadad. And they were [the] chiefs of Edom chief Timna chief (Alvah *Q(K)*) chief Jetheth.
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
Chief Oholibamah chief Elah chief Pinon.
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
Chief Kenaz chief Teman chief Mibzar.
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
Chief Magdiel chief Iram these [were] [the] chiefs of Edom.

< 1 Mbiri 1 >