< Roma 10 >

1 Mga igsoon, ang tinguha sa akong kasingkasing ug ang akong hangyo sa Dios alang kanila, alang sa ilang kaluwasan.
Abale, chokhumba cha mtima wanga ndi pemphero langa kwa Mulungu ndi chakuti Aisraeli apulumutsidwe.
2 Kay ako nagsaksi mahitungod kanila nga sila adunay kasibot sa Dios, apan dili pinasikad sa kahibalo.
Popeza ndiwachitira umboni kuti ndi achangu pa zinthu za Mulungu koma osati mwachidziwitso.
3 Kay sila wala masayod sa pagkamatarong sa Dios, ug sila nagtinguha sa pagtukod sa ilang kaugalingon nga pagkamatarong. Wala sila nagpailalom sa pagkamatarong sa Dios.
Pakuti sanadziwe chilungamo chochokera kwa Mulungu ndipo anafuna kukhazikitsa chawochawo. Iwo sanagonjere chilungamo cha Mulungu.
4 Kay si Cristo maoy katumanan sa balaod sa pagkamatarong sa tanan nga motuo.
Khristu ndiye mathero amalamulo kuti aliyense amene akhulupirira akhale olungama pamaso pa Mulungu.
5 Kay si Moises nagsulat mahitungod sa pagkamatarong nga gikan sa balaod: “Ang tawo nga mibuhat sa pagkamatarong sa balaod mabuhi pinaagi niining pagkamatarong.”
Mose akulemba motere zachilungamo cha malamulo, “Munthu amene achita zinthu izi adzakhala ndi moyo pozichita.”
6 Apan ang pagkamatarong nga gikan sa pagtuo nagaingon niini, “Ayaw pagsulti sa inyong kasingkasing, 'Kinsa ang mokayab didto sa langit?' (nga sa ato pa, aron pagdala kang Cristo paubos).
Koma chilungamo cha chikhulupiriro chikuti, “Usanene mu mtima mwako kuti, ‘Kodi ndani amene akwere kumwamba?’” (ndiko, kukatsitsa Khristu)
7 Ug ayaw pagsulti, kinsa ang monaog didto sa bung-aw?'” (nga sa ato pa, aron pagdala kang Cristo pataas gikan sa mga patay.) (Abyssos g12)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
8 Apan unsa ang gisulti niini? “Ang pulong duol na kaninyo, sa inyong baba ug sa inyong kasingkasing.” Mao kana ang pulong sa pagtuo, nga among gimantala.
Nanga akuti chiyani? “Mawu ali pafupi ndi inu. Ali mʼkamwa mwanu ndi mu mtima mwanu.” Ndiwo mawu achikhulupiriro amene ife tikuwalalikira,
9 Kay kung sa inyong baba inyong ilhon si Jesus ingon nga Ginoo, ug motuo sa inyong kasingkasing nga ang Dios nagbanhaw kaniya gikan sa mga patay, kamo maluwas.
kuti ngati udzavomereza ndi pakamwa pako kuti, “Yesu ndiye Ambuye,” ndi kukhulupirira mu mtima mwako kuti Mulungu anamuukitsa kwa akufa, udzapulumuka.
10 Kay pinaagi sa kasingkasing ang tawo mituo sa pagkamatarong, ug pinaagi sa baba iyang giila ang kaluwasan.
Pakuti ndi mtima wanu mukhulupirira ndi kulungamitsidwa, ndipo ndi pakamwa panu muvomereza ndi kupulumutsidwa.
11 Kay ang kasulatan nag-ingon, “Ang tanan nga motuo kaniya dili mabutang sa kaulawan.”
Pakuti Malemba akuti, “Aliyense amene akhulupirira Iye, sadzachititsidwa manyazi.”
12 Kay walay kalahi-an tali sa Judio ug sa Griyego. Kay ang sama lamang nga Ginoo mao ang Ginoo sa tanan, ug siya dato sa tanan nga mosangpit kaniya.
Pakuti palibe kusiyana pakati pa Myuda ndi a mitundu ina, pakuti Ambuye mmodzi yemweyo ndi Ambuye wa onse ndipo amadalitsa mochuluka onse amene ayitana pa Iye
13 Kay ang tanan nga mosangpit sa ngalan sa Ginoo maluwas.
pakuti, “Aliyense amene adzayitana pa dzina la Ambuye adzapulumuka.”
14 Unsaon man nila pagtawag kaniya nga wala nila tuohi? Ug unsaon man nila pagtuo kaniya nga wala nila madungog? Ug unsaon nila pagkadungog kung walay magwawali?
Kodi adzayitana bwanji amene sanamukhulupirire? Ndipo adzakhulupirira bwanji asanamve za Iye? Ndipo adzamva bwanji popanda wina kulalikira kwa iwo?
15 Ug unsaon nila pagwali, gawas kung ipadala sila? —Ingon kini nahisulat, “Pagkatahom sa mga tiil niadtong nagmantala sa malipayong mga balita sa maayong mga butang!”
Ndipo iwo adzalalikira bwanji osatumidwa? Kwalembedwa kuti, “Akongoladi mapazi a iwo amene amabweretsa Uthenga Wabwino!”
16 Apan silang tanan wala maminaw sa ebanghelyo. Kay si Isaias miingon, “Ginoo, kinsa man ang mituo sa among mensahe?”
Koma si onse amene anavomereza Uthenga Wabwino. Pakuti Yesaya akuti, “Ambuye, ndani amene wakhulupirira uthenga wathu?”
17 Busa ang pagtuo nagagikan sa pagpaminaw, ug sa pagpaminaw sa pulong ni Cristo.
Motero, chikhulupiriro chimabwera pamene timva uthenga ndipo uthenga umamveka kuchokera ku mawu a Khristu.
18 Apan ako moingon, “Wala ba sila makadungog?” Oo, tinuod gayod. “Ang ilang tingog nangabot sa tanang kayutaan, ug ang ilang mga pulong didto sa kinatumyan sa kalibotan.”
Koma ndikufunsa kuti kodi iwo anamva? Inde, iwo anamva kuti, “Liwu lawo linamveka ponseponse pa dziko lapansi. Mawu awo anafika ku malekezero a dziko lonse.”
19 Dugang pa, moingon ako, “Wala ba masayod ang Israel?” Sauna si Moises miingon, “Ako maghagit kaninyo aron masina sa unsa nga dili nasod. Pinaagi sa nasod nga walay salabutan, agdahon ko kamo ngadto sa kasuko.”
Ine ndifunsanso kuti, kodi Israeli sanazindikire? Poyamba Mose akuti, “Ine ndidzawachititsa kuti achite nsanje ndi mtundu wina wopandapake. Ine ndidzawakwiyitsa ndi mtundu wina wachabechabe.”
20 Ug si Isaias maisogon kaayo ug miingon, “Nakaplagan ako niadtong wala nangita kanako. Nagpakita ako niadtong wala naghangyo kanako.”
Ndipo Yesaya molimba mtima akuti, “Anandipeza anthu amene sanali kundifunafuna. Ndinadzionetsera kwa amene sanafunse za Ine.”
21 Apan ngadto sa Israel miingon siya, “Sa tanang adlaw gitunol ko ang akong mga kamot ngadto sa mga masinupakon ug masupilon nga katawhan.”
Koma zokhudzana ndi Aisraeli akuti, “Tsiku lonse ndinatambasulira manja anga kwa anthu osandimvera ndi okanika.”

< Roma 10 >