< Псалми 65 >

1 За първия певец, Давидов псалом. Песен. Тебе чака хваление, Боже, в Сион; И пред Тебе ще се изпълни обрекът.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Nyimbo. Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni; kwa inu malumbiro athu adzakwaniritsidwa.
2 Ти, Който слушаш молитва, При Тебе ще дохожда всяка твар.
Inu amene mumamva pemphero, kwa inu anthu onse adzafika.
3 Беззакония ми надвиха; Но престъпленията ни, - Ти ще ги очистиш.
Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo, Inu munakhululukira mphulupulu zathu.
4 Блажен човекът, когото избираш И приемаш, за да живее в Твоите дворове; Ще се наситим от благата на Твоя дом На светия Ти храм.
Odala iwo amene inu muwasankha ndi kuwabweretsa pafupi kukhala mʼmabwalo anu! Ife tadzazidwa ndi zinthu zabwino za mʼNyumba mwanu, za mʼNyumba yanu yoyera.
5 С ужасни неща ще ни отговаряш в правда, Боже, Избавителю наш, Надеждо на всичките земни краища, И на ония, които са далеч по море,
Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo, Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, chiyembekezo cha mathero onse a dziko lapansi ndi cha nyanja zomwe zili kutali kwambiri,
6 Ти Който със силата Си утвърждаваш планините, Препасан с могъщество,
amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu, mutadziveka nokha ndi mphamvu.
7 Който правиш да утихва шума на морето, Бученето на вълните му и размирието на племената.
Amene munakhalitsa bata nyanja kukokoma kwa mafunde ake, ndi phokoso la anthu a mitundu ina.
8 Така и тия, които живеят по краищата на земята, се боят от Твоите знания. Развеселяваш излиянията на зората и на вечерта:
Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu; kumene dzuwa limatulukira ndi kumene dzuwa limalowera. Inu mumafuna nyimbo zachimwemwe.
9 Като посещаваш земята и я напояваш Ти я преобогатяваш; Ръката Божия като е пълна с вода. Ти промишляваш жито за тях, Когато така си приготвил земята:
Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira; Inuyo mumalilemeretsa kwambiri. Mtsinje wa Mulungu ndi wodzaza ndi madzi kuti upereke tirigu kwa anthu, pakuti Inu munakhazikitsa zimenezi.
10 Като напояваш нейните бразди Изравняваш буците й; Като я размекваш с капките на дъжда Благославяш поникналото от нея;
Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake, mwayifewetsa ndi mvula yamawawa ndi kudalitsa mbewu zake.
11 Върху годината на благостта Си туряш венец, И от следите Ти капе тлъстина;
Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka, ndipo ngolo zanu zimasefukira ndi zinthu zochuluka.
12 Пасбищата на пустинята капят от изобилията си, И хълмовете се опасват с радост;
Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira; mapiri avekedwa ndi chisangalalo.
13 Ливадите се обличат със стада, И долините се покриват с жито; Възклицават, още и пеят.
Madambo akutidwa ndi zoweta ndi zigwa zavekedwa ndi tirigu; izo pamodzi zikufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe.

< Псалми 65 >