< Йов 40 >

1 Господ говори на Иова и каза:
Yehova anati kwa Yobu:
2 Тоя, която е изобличил Всемогъщият, ще ли се бори с Него? Тоя, който се препира с Бога, нека отговори на всичко това.
“Kodi iwe ufuna kukangana ndi Wamphamvuzonse? Iwe amene unatsutsana ndi Mulungu umuyankhe Iyeyo!”
3 Тогава Иов отговори Господу, казвайки:
Pamenepo Yobu anayankha Yehova:
4 Ето, аз съм нищожен; какво да Ти отговоря? Турям ръката си на устата си.
“Ine sindili kanthu konse, kodi ndingathe kukuyankhani chiyani? Ndagwira pakamwa panga.
5 Веднъж съм говорил, и не ще да отговарям вече, Дори дваж, но няма да повторя.
Ndinayankhula kamodzi, koma pano ndilibe yankho, ndinayankha kawiri, koma sindiwonjezeranso mawu ena.”
6 Тогава Господ отговори на Иова из бурята, като каза:
Ndipo Yehova anayankha Yobu mʼkamvuluvulu kuti,
7 Опаши сега кръста си като мъж; Аз ще те попитам, и ти Ми изявявай.
“Tsopano vala dzilimbe ngati mwamuna; ndikufunsa mafunso ndipo iwe undiyankhe.
8 Дори не ще ли допускаш Моята съдба? Ще осъдиш ли Мене, за да оправдаеш себе си?
“Kodi iwe unganyoze chiweruzo changa cholungama? Kodi ungandidzudzule kuti iweyo ukhale wolungama?
9 Или имаш ли мишца като Бога? И можеш ли да гърмиш с глас като Него?
Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu, ndipo mawu ako angagunde ngati mphenzi monga a Mulungu?
10 Украси се сега с превъсходство и достолепие, И облечи се в чест и величие.
Ngati zili choncho udzikometsere ndi ulemerero ndi kukongola, ndipo udziveke ulemu ndi ulemerero waufumu.
11 Изсипвай преливащия си гняв; И гледай на всеки горделив, и смирявай го;
Tsanula ukali wako wosefukirawo, uyangʼane aliyense wodzikuza ndipo umuchepetse,
12 Гледай на всеки горделив, и снишавай го; И стъпквай нечестивите на мястото им;
Uyangʼane aliyense wodzikweza ndipo umutsitse, uwapondereze oyipa onse pamalo pomwe alilipo.
13 Скрий го купно в пръстта; Вържи лицата им в скрито място.
Onsewo uwakwirire pamodzi mfumbi; ukulunge nkhope zawo mʼmanda.
14 Тогава и Аз ще изповядам пред тебе, Че твоята десница може да те спаси.
Ukatero Ine ndidzakuvomereza kuti dzanja lako lamanja lakupulumutsadi.
15 Ето сега речния кон който съм направил както и тебе; Яде трева като вол.
“Taganiza za mvuwu, imene ndinayipanga monga momwe ndinapangira iwe, ndipo imadya udzu ngati ngʼombe.
16 Ето сега, силата му е в чреслата му, И якостта му е в мускулите на корема му.
Mphamvu zake ndi zazikulu kwambiri, thupi lake ndi lanyonga kwambiri!
17 Клати опашката си като кедър; Жилите на бедрата му са сплотени.
Mchira wake umayima tolotolo ngati mtengo wamkungudza; mitsempha ya ntchafu zake ndi yogwirana bwino.
18 Костите му са като медни цеви; Ребрата му са като железни лостове.
Mafupa ake ali ngati mapayipi amkuwa, nthiti zake zili ngati mipiringidzo yachitsulo.
19 Той е изящното дело Божие; Оня, Който го е направил, го е снабдил с меча Си.
Mvuwuyo ndi yayikulu mwa zolengedwa za Mulungu, komatu mlengi wake amatha kuyiopseza ndi lupanga lake.
20 Наистина планините промишляват за него храна. Гдето играят всичките полски зверове.
Imapeza chakudya chake ku mtunda ndipo nyama zakuthengo zonse zimasewera pambali pake.
21 Ляга под сенчестите дървета, В съкровището на тръстиката, и в блатата;
Imagona pa tsinde pa zitsamba za mipeta, imabisala mʼbango ndiponso pa thawale.
22 Сенчестите дървета го покриват със сянката си; Върбите на потоците го обкръжават.
Imaphimbika ndi mthunzi wazitsamba za mipeta; imazunguliridwa ndi misondozi ya mu mtsinje.
23 Ето, ако би придошла река, той не трепери; Не се смущава, ако би се и Иордан устремил по устата му.
Madzi a mu mtsinje akakokoma, sichita mantha, iyo sitekeseka, ngakhale madzi a mu Yorodani afike mʼkhosi mwake.
24 Може ли някой да го хване когато е на щрек. Или да прободе носа му с примка?
Kodi alipo amene angathe kukola mvuwu ndi mbedza kapena kuyikola mu msampha?

< Йов 40 >