< Mark'os Dooshishiyo 1 >
1 Hań Ik'onaayi Iyesus Krstosko doo shishiyo b́ tuwokoni.
Chiyambi cha Uthenga Wabwino wa Yesu Khristu, Mwana wa Mulungu,
2 Nebiyiyo Isayasn, «Hambe, nwerind foketwo T woshtso nshinatse beshide woshitwee.
monga zalembedwera mʼbuku la mneneri Yesaya: “Ine ndidzatuma mthenga wanga patsogolo panu, amene adzakonza njira yanu,”
3 Hanwere ‹Doonzosh weerindo k'aniwere B́fudonowere manutsiwere› etfere, Worwotse b́k'aaro eenshde'k't keewiru asho k'aaroniyee» ett guut'etsok'one.
“Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’”
4 Mansh gupfo Yohans «It morrosh orowe eto itdatsish naandrone err gupewere» ett worwotse kuhdek'et keewfere b́weyi.
Ndipo Yohane anabwera mʼmadera a mʼchipululu nabatiza, ndi kulalikira za ubatizo wa kutembenuka mtima ndi wa chikhululukiro cha machimo.
5 Yhud datsonat Iyerusalem kitutse ay asho b́maantsa bowaafo, bo morro kish keewr Yordanosi eteets fokotse b́ kishatsna bogupefo.
Madera onse a ku Yudeya ndi anthu onse a ku Yerusalemu anatuluka napita kwa iye. Akavomereza machimo awo, amawabatiza mu mtsinje wa Yorodani.
6 Yohans tahonwere kambuli s'iron wozeka b́tesh. B́gebatso shaak'a bí edefo, b́maafonwere p'elonat dok'shi mas'ona.
Yohane amavala zovala zopangidwa ndi ubweya wangamira, ndi lamba wachikopa mʼchiwuno mwake, ndipo amadya dzombe ndi uchi wamthengo.
7 Bí hank'owa bí'etfo «Túmr b́c'aami tipi joko bitsosh tborawo taayere ayidek' bogtso tshutsatse weeyirwe.
Ndipo uthenga wake unali uwu: “Pambuyo panga pakubwera wina wondiposa ine mphamvu. Ine si woyenera kuwerama ndi kumasula zingwe za nsapato zake.
8 Taa iti aatson gupetwe, bímó itn S'ayn shayiron gupetwe.»
Ine ndikubatizani ndi madzi, koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.”
9 Manoor Iyesus Galili eteets datsatse beyiru Naazreti eteef kituts waat́ Yordanos fokotse Yohans kishon b́gupeyi.
Pa nthawi imeneyo Yesu anabwera kuchokera ku Nazareti wa ku Galileya ndipo anabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani.
10 Yohans manoor, Iyesus aatsotse b́keshtsok'on daro gaad'at́ b́k'eshefere, S'ayin shayiro kurkund areyat bíyats b́ oot'́fere b́bek'i.
Pamene Yesu ankatuluka mʼmadzi, anaona kumwamba kukutsekuka ndipo Mzimu Woyera akutsikira pa Iye ngati nkhunda.
11 Manoor «Taan gene'úshtso t shunts na'o neene» etiru k'ááro darotse b́weyi.
Ndipo Mawu anamveka kuchokera kumwamba: “Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa; ndipo ndikondwera nawe.”
12 Manóór Ik'i Shayiro Iyesusi worwots dek't bí'ami.
Nthawi yomweyo Mzimu Woyera anamutumiza Iye ku chipululu,
13 Manoknowere worwotse Shed'ano Iyesusi hab aawosh b́ fadfera b́teshi, dín s'ootswotsntoni b́ tesh, melkiwotsu bísh finernó botesh.
ndipo anali mʼchipululumo masiku makumi anayi, akuyesedwa ndi Satana. Anali pakati pa nyama zakuthengo; ndipo angelo anamutumikira.
14 Yohans detseyat tipimo b́ kindiyakon Iyesus, Ik'i mengsti jangosh doo shishiyo nabfere Galil maants b́weyi.
Yohane atamutsekera mʼndende, Yesu anapita ku Galileya nalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu nati,
15 B́daniyoro, «Dúro s'uuwtsere, Ik'imengstu karnfere b́watsotse it naandrone erere, dooshishi nabetsono amanore!» bí etfo.
“Nthawi yafika, ufumu wa Mulungu wayandikira. Tembenukani mtima ndi kukhulupirira Uthenga Wabwino!”
16 Maniye il Iyesus Gelil aatsk'ari ganoke beshefetst Simon nat bí eshu Indriyasn mus' detsfwotsi boteshtsotse bo mus' kambo aats k'aro maants boshap'fere boon b́ bek'i.
Pamene Yesu ankayenda mʼmbali mwa nyanja ya Galileya, anaona Simoni ndi mʼbale wake Andreya akuponya khoka mʼnyanja, popeza anali asodzi.
17 Iyesuswere «T jafrats woore itsh tdanisha, err mus' it detsirwok'o ashuwotsi it detsetwok'ó woshitwe» bí eti.
Yesu anati, “Bwerani, tsateni Ine, ndipo ndidzakusandutsani asodzi a anthu.”
18 Bowere manoor bo mus' detsi kambo k'azk'rat́ b́shuutso bo tuwi.
Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.
19 Maniyere múk'i beshat k'osh eshu gitwotsi b́bek'i. Bowere Zebdiyos nana'úwots Ya'ak'obnat Yohansna botesh. Bowere bo jelbotse bedek't bo mus' detsi kambo bok'anifera botesh.
Atapita patsogolo pangʼono, anaona Yakobo ndi mʼbale wake Yohane ana a Zebedayo, ali mʼbwato akukonza makoka awo.
20 Iyesus manoor boon b́s'eegi. Bowere bonih Zebdiyosnat bísh fin finirwotsn jelbatse k'azk'rat Iyesus jafrats boami.
Mosataya nthawi anawayitana, ndipo anasiya abambo awo Zebedayo ndi anyamata aganyu ali mʼbwatomo, namutsata Iye.
21 Beshatnu K'frnahom kitots bobodi. Manoori waats sanbatots Iyesus Ayhdiwots Ik' k'oni mootse daniyo dek't b́twi.
Iwo anapita ku Kaperenawo, ndipo tsiku la Sabata litafika, Yesu analowa mʼsunagoge nayamba kuphunzitsa.
22 Iyesus, Muse nemo danifwots kok'o b́woterawo naashikook'o b́danifotse shishts jamwots b́daniyor ada bo adfo.
Anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake, chifukwa anawaphunzitsa ngati munthu amene anali ndi ulamuliro, osati ngati aphunzitsi amalamulo.
23 Ayhudiwots Ik' k'oni mootse beyiru ash iko gond shayiron s'eentso hank'o ett b́kúhi,
Pomwepo munthu wina mʼsunagogemo amene anali wogwidwa ndi mzimu woyipa anafuwula kuti,
24 «Nazrettso Iyesuso, nee nooke eeg kis'e ndetsi? Noon t'afiyosh waafi? Nee koni n wottsok'o taa daank'reree. Ik'oko S'ayino neene.»
“Mukufuna chiyani kwa ife, Yesu wa ku Nazareti? Kodi mwabwera kudzatiwononga? Ndikudziwa kuti ndinu ndani, ndinu Woyerayo wa Mulungu!”
25 Iyesuswere gond shayirmansh «S'ik err, bí atsotse kee» ett b́fayi.
Yesu anadzudzula chiwandacho mwamphamvu nati, “Khala chete! Tuluka mwa iye!”
26 Gond shayronwere ashman dikdek't b́s'ik'iyakon b́k'aaro eensh dek't kuhefetst bí atsotse b́ keshi.
Mzimu woyipawo unamugwedeza mwamphamvu ndipo unatuluka mwa iye ukufuwula.
27 «Eebi han naaroni? Hanwo handr daniyeya?» Gond shayirwotsi bí aloro bo bíshere bo aleyiri, ett adt bo atsatseyo aateyo dek' bo tuwi.
Anthu anadabwa kwambiri kotero kuti anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Ichi nʼchiyani? Chiphunzitso chatsopano ndi ulamuliro! Iye akulamula, ngakhale mizimu yoyipa ikumumvera.”
28 Muk'i b́teyawo, Iyesus shúútso Galil gúúratsi dats jamatse dane b́wtsi.
Mbiri yake inafalikira kudera lonse la Galileya mofulumira.
29 Muk'ib́teyawo Iyesus ayhudi Ik' k'oni mootse kesht Yak'obnat Yohansnton, Simoonnat Indryasn moots b́kindi.
Atangochoka mu sunagoge, Yesu pamodzi ndi Yakobo ndi Yohane anakalowa mʼnyumba ya Simoni ndi Andreya.
30 Maa manitsno Simon awu ats k'ees'its shodo shodat bk'efera btesh. Bshodmanowere manoor Iyesussh keewbok'ri.
Mpongozi wa Simoni anali chigonere akudwala malungo, ndipo anamuwuza Yesu za iye.
31 Iyesuswere bmaand t'int́ bkisho detsdek't b́tuuzi. Bi atsi k'ees'onwere manoor binfakshb́k'ri. Tuwatnwere boon b ibiy.
Ndipo Yesu anapita kwa iye, namugwira dzanja namuthandiza kudzuka. Malungo anachoka ndipo anayamba kuwatumikira.
32 Aawu bkindre datso bí iliyakon ashuwots shodtswotsnat fo'erawon detsets jamwotsi Iyesusok dek't boweyi.
Madzulo omwewo dzuwa litalowa anthu anabweretsa kwa Yesu anthu onse odwala ndi ogwidwa ndi ziwanda.
33 Kititsi ash jamo maa úratse kakwe b́wtsi.
Anthu onse a mʼmudzimo anasonkhana pa khomo,
34 Iyesus ay naari shoodon kic'iru ay ashuwotsi kashi b́k'ri. Fo'eraw aywotsno b́kishi. Fo'erawwotswere bí koni b́woto danfno botesh. Ernmó bokeewrawok'o boon b́baziyi.
Yesu anachiritsa ambiri amene anali ndi matenda osiyanasiyana, komanso anatulutsa ziwanda zambiri, ndipo sanalole kuti ziwandazo ziyankhule chifukwa zinkamudziwa Iye.
35 Datso gatsosh bí etfere, Iyesus guuron tuut mootse kesht Ik' k'onosh ash aalok k'az bíami.
Mmamawa, kukanali kamdima, Yesu anadzuka, nachoka pa nyumbapo kupita kumalo kwa yekha, kumene anakapemphera.
36 Simoonnat bínton teshtswots bín geyo kesht boami.
Simoni ndi anzake anapita kokamufunafuna Iye,
37 Bín bodatstsok'ono «Ash jamonwo neenere b́geyiri» bo eti.
ndipo atamupeza, anamuwuza kuti, “Aliyense akukufunani!”
38 Iyesuswere, «Taa twaa danyosh b́wottsotse doo shishiyo danyosh karnoke fa'a gal galóts amone!» bí et.
Yesu anayakha kuti, “Tiyeni tipite kwina ku midzi ya pafupi kuti ndikalalikirenso kumeneko. Ichi ndi chifukwa chimene ndinabwerera.”
39 Mann ayhudiwots Ik' k'oni maa mootse danifetsit fo'erawwotsnowere kishfere Galil dats jamatse b́gúúrefo b́tesh.
Potero anayendayenda mu Galileya, kulalikira mʼmasunagoge awo ndi kutulutsa ziwanda.
40 Een shod detsts ash iko Iyesus maants waat b́ tufi shirots tuk'maldek't, «Ni eekiyal taan s'ayintso falfne» eton bín b́k'oni.
Munthu wakhate anabwera kwa Iye, nagwada, namupempha kuti, “Ngati mukufuna, mukhoza kundiyeretsa.”
41 Iyesuswere bísh maac'o k'ewat, b́kisho jargdek't shu'efetst, «Eekere s'ayine!» bí et.
Yesu pomva naye chifundo, anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo nati, “Ndikufuna, yeretsedwa!”
42 Ashmanwere manoor bí een shodotse s'ayinb́wtsi.
Nthawi yomweyo khate linachoka ndipo anachiritsidwa.
43 Iyesus ashmansh kup'shdek't, ntooko korde'e ett faksh b́k'r.
Nthawi yomweyo Yesu anamuwuza kuti apite koma anamuchenjeza kuti,
44 «Wotts keewan ik doonzshor nkeewrawok'o ni tooko korde'e, ernmó amr ntooko kahniyosh kitswe. Ashjamosh gaw b́wotish nkashtsotse Muse k'aluwere bí etts wosho t'intswe» ett bíazazi.
“Wonetsetsa kuti usawuze aliyense za zimenezi. Koma pita, kadzionetse wekha kwa wansembe ndi kukapereka nsembe zimene Mose analamulira zotsimikizira kuyeretsedwa kwanu, ngati umboni kwa iwo.”
45 Ernmó ashman manoke kesht keewman ashosh keewo dek't b́tuwi. Manatse tuutson Iyesus kit ikutsnor be'efetst kindo b́maawi. Ernmó kitoniye úratse ash aaloka b́befo. B́ wotefere ashuwots bo be beewoke b́ maants waa bowaafo.
Mʼmalo mwake anapita nayamba kuyankhula momasuka, nafalitsa mbiriyo. Zotsatira zake, Yesu sanathe kulowa mʼmudzi moonekera, koma anakhala kunja kumalo kopanda anthu. Komabe anthu amabwera kwa Iye kuchokera kulikonse.