< Woshetswotsi 9 >

1 Manoor Sawuol doonzo danifuwotsi úd'osh naakefere kahaniyots naashok bíami.
Pa nthawi imeneyi, Saulo ankaopsezabe okhulupirira Ambuye nafuna kuwapha. Iye anapita kwa mkulu wa ansembe,
2 Doonzo weerindion shairu ashuwotsi nungushwotsno máátsuwotsno b́ daatsor tifde Iyerusalem maants de'er woo bín faliyit debdabeyo guud'de Demask'oyitsi ayhudiwots Ik' k'oni moowwots sh bísh imetwok'o kahini naash naasho bí aati.
ndi kukapempha makalata a chilolezo kuti apite nawo ku masunagoge a ku Damasiko, kuti ngati atakapezeka ena kumeneko otsata Njirayo, kaya ndi amuna kapena amayi, akawamange ndi kuwatenga kubwera nawo ku Yerusalemu.
3 Amfetst Demask'o maants b́ t'intsok'on b́ gúúratse gawerawon darotse shááno gol b́wutsi.
Akuyandikira ku Damasikoku paulendo wake, mwadzidzidzi kuwala kochokera kumwamba kunamuzungulira iye.
4 Manoor datsats dihb́wutsi, «Sa'olo! Sa'olo! eegishe taan ngishiri?» etiru k'aaro b́shishi.
Iye anagwa pansi ndipo anamva mawu akuti, “Saulo, Saulo ukundizunziranji Ine?”
5 Sa'oluwere «Doonzono! kone nee?» bí eti, bíwere «Taahe nee ngishiruwo Iyesus taane, bín kosheef birro n k'efiyale neeshe iki b́gonditi,
Saulo anafunsa kuti, “Ndinu yani Ambuye?” Ambuye anayankha kuti, “Ndine Yesu amene iwe ukumuzunza.”
6 Eshe, and tuur kitots kiduwee, bíyoke k'alo neesh geyituwonowere manoke neesh keewetuwe» bí eti.
“Tsopano dzuka, lowa mu mzindamo, ndipo udzawuzidwa zoyenera kuchita.”
7 Sa'olnton amfetst teshts ashuwots k'aaro shishfetst konnor bobe'awotse bo keewituwo t'ut't s'ik ett need'bowutsi.
Anthu amene anali naye paulendo, anasowa chonena; iwo anamva mawu koma sanaone wina aliyense.
8 Sa'oluwere b́ dihtsoke b́ tuwi, bí aawwotsi b́ k'eshormó bek'o falratse, mansh ashaashwots b́ kisho dets dek't jishfere Demask'o maants dek't boam.
Saulo anayimirira, ndipo pamene anatsekula maso ake sanathe kuona. Kotero anamugwira dzanja ndi kulowa naye mu Damasiko.
9 Keez aawu s'eenosh eegor bek'o b́ falrawo, b́ marawo, b́ úyawo b́tesh.
Anakhala wosaona kwa masiku atatu ndiponso sanadye kapena kumwa kanthu kalikonse.
10 Manoor Demask'on Hananiyi eteefo Iyesus danif iko fa'e b́tesh, doonzo bek'on «Hananiyo!» ett b́s'eegi bíwere «Hamb taane, doonzono!» bí et.
Ku Damasiko kunali wophunzira wina dzina lake Hananiya. Ambuye anamuyitana mʼmasomphenya kuti, “Hananiya!” Iye anayankha kuti, “Ine Ambuye.”
11 Doonzonu hank'o bíeti, «Tuur kááwi eteyiru werindu maants amee, manokno Yhud mootse Sa'oli eteetso T'erses asho gewowe, bíwere and Ik' k'onoke b́ fa'oni.»
Ambuye anamuwuza iye kuti, “Nyamuka, pita ku nyumba ya Yudasi imene ili pa Njira Yolunjika ndipo ukafunse za munthu wochokera ku Tarisisi dzina lake Saulo, pakuti akupemphera.
12 Sa'oluwere bí ááwuwots aani bek'o bofalituwok'o Hanani eteets asho bíyok kindt b́ kisho bíyats b́ gedfere bek'on b́ bek'i.
Ndipo waona mʼmasomphenya munthu, dzina lake Hananiya atabwera ndi kumusanjika manja kuti aonenso.”
13 Hananiyuwere hank'o ett bíaani, «Doonzono! ashaan Iyerusalemitse beyiru amantsuwotsats ay gond keewo b́fintsok'o ayuwotsoke shishre.
Hananiya anayankha kuti, “Ambuye, ndinamva zambiri za munthu uyu ndi zonse zoyipa anachitira oyera mtima a ku Yerusalemu.
14 Manoknowere n shúts s'eegiru jamwotsi tiposh kahni naashuwotsoke alo dek're.»
Ndipo wabwera kuno ndi ulamuliro wa akulu ansembe kuti adzamange onse amene amayitana pa dzina lanu.”
15 Doonzonuwere Hananiysh hank'owa bíet, «Bí t shútso Ik' danawu ashuwots shinatse, naashuwots shinatsnat Isra'el ashuwotssh danituwoniye, bí t k'ac'i sheengo b́ wottsotse bíyok amee,
Koma Ambuye anati kwa Hananiya, “Pita! Munthu uyu ndi chida changa chosankhika chonyamulira dzina langa pamaso pa anthu a mitundu ina ndi mafumu awo ndiponso kwa anthu a Israeli.
16 T jangosh awuk'o gondbek'o b́dek'etuwok'owo kitsituwe bísha.»
Ine ndidzamuonetsa zowawa zonse zimene ayenera kumva chifukwa cha dzina langa.”
17 Mann Ananiyi maa man maants amt b́ beyiru mootsowere b́ kindi, b́ kishonowere Sa'olaats geddek't, «Ti eshu Sa'olo! hanmand n wafere weratse ni ats be'etso Doonzo Iyesus aani bek'o n falituwok'onat S'ayin shayiron n s'enetuwok'o niyok taan woshere» bí eti.
Pamenepo Hananiya ananyamuka ndi kukalowa mʼnyumbayo. Anamusanjika manja Sauloyo ndipo anati, “Mʼbale Saulo, Ambuye Yesu, amene anakuonekera pa msewu pamene umabwera kuno wandituma kuti uwonenso ndi kudzazidwa ndi Mzimu Woyera.”
18 Manorowere k'ok'r arts keewo bí ááwatse fed'at bí eree bek'o b́fali, tuutnwere b́gupeyi.
Nthawi yomweyo mʼmaso mwa Saulo munachoka zinthu zokhala ngati mamba ansomba, ndipo anayambanso kuona. Iye anayimirira nabatizidwa,
19 Meetwo b́ meeyihakon kup'b́wutsi, Demask'on teshts Iyesus danifuwotsnton muk' aawwotssh manoke b́ teshi.
ndipo atadya chakudya, anapezanso mphamvu. Saulo anakhala masiku angapo ndi ophunzira a ku Damasiko.
20 Manorowere Sa'ol Demask'on «Iyesus Ik'o naayiye» etfere ayhudiwots Ik' k'oni mootse daniyo b́ tuwi.
Posakhalitsa anayamba kulalikira mʼsunagoge kuti Yesu ndiye Mwana wa Mulungu.
21 Shishts jamwotswere, «Ashaan Iyerusalemitse shútsan s'eegiru jamwotsi t'afifoniyosha? Hanok b́wowuwere boon tifde'er kahni naashuwotsok de'er amooshoshna?» ett bo'adi.
Onse amene anamva iye akulalikira anadabwa ndipo anafunsa kuti, “Kodi uyu si munthu amene anayambitsa kuzunza okhulupirira ku mpingo wa ku Yerusalemu? Kodi siwabwera kuno kuti awamange ndi kuwapereka kwa akulu a ansembe?”
22 Sa'olmó iki kup'efere bí ami, Iyesus mesihiyo b́wottsok'o keewut Demask'oyitse beyat teshts Ayhudiwots noono bo keewituwo b́t'ut'ifoni b́ tesh.
Koma mphamvu za Saulo zinali kukulirakulira ndipo anathetsa nzeru Ayuda okhala ku Damasiko powatsimikizira kuti Yesu ndi Mpulumutsi.
23 Ay aawoniyere il ayhudiwots Sa'oli úd'osh boshiyeyi,
Patapita masiku ambiri, Ayuda anapangana zoti aphe Saulo,
24 Bímo gondon bíats bo shiyetsman danb́k'iri, boowere bín úd'osh t'uwe aawo b́ keshf fengshuwotsi bo kotfoni.
koma iye anadziwa za chiwembucho. Anthu ankadikirira usana ndi usiku pa zipata za mzindawo kuti amuphe.
25 Ernmó t'úwon b́ danifuwots Sa'oli oshots geddek't gimbiyi múlotse maskotiyon oorsh bo k'ri.
Koma ophunzira ake anamutenga usiku, namutsitsira kunja kwa mpandawo mʼdengu.
26 Sa'ol Iyerusalem maants bíamor manoke fa'a Iyesus danifuwotsnton eeho b́geyi, bomó bí Krstosi bí amantsok'o arik boosh arewo b́ k'aztsotse bojamets bín boshati.
Saulo atafika ku Yerusalemu, anayesetsa kulowa mʼgulu la ophunzira koma onse anamuopa chifukwa sanakhulupirire kuti anali wophunziradi.
27 Bernabasmó Sa'oli woshetswotsok b́ t'intsre weeratse b́befere doonzo bísh b́ be'etsok'onat bín noono b́ keewitsok'o, Iyesus Shútsonowere Demask'on ááwu shuuk'on b́ danitsok'o boosh b́ keewi.
Koma Barnaba anamutenga napita naye kwa atumwi. Iye anawafotokozera iwo za mmene Saulo anaonera Ambuye pa njira paja, ndi kuti Ambuye anamuyankhula, ndi momwe analalikira ku Damasiko mʼdzina la Yesu mosaopa.
28 Mansh Sa'ol bonton wotdek't Iyerusalemitse bíananefo. Doonzo shútsonowere ááwu shuk'on b́ danifoni.
Kotero Saulo anakhala nawo nayendayenda mwaufulu mu Yerusalemu akulalikira molimba mtima mʼdzina la Ambuye.
29 Grik dats ash noonon keewuf ayhudiwotsnton keewefetstni b́ mooshfo, bomó bín úd'osh k'anwutskno botesh.
Anayankhula ndi kutsutsana ndi Ayuda a Chihelene, koma iwo ankafuna kumupha.
30 Eshuwots man dan bok'rtsok'on K'isariy maants k'az dek'boami, manoknowere Terses maants k'aybíametuwok'o bowoshi.
Abale atadziwa zimenezi, anamutenga Saulo ndi kupita naye ku Kaisareya, ndipo anamutumiza ku Tarisisi.
31 Yhuditse, Gelilitsnat Semaritse fa'a jam Ik'i moowu jeeno datsrane, kúp'onowere kup'eraniye, Doonzono! mangiyifetsat S'ayin shayirowere kup'efetsat taawon eenranee.
Pamenepo mpingo wa ku Yudeya konse, ku Galileya ndi ku Samariya unakhala pamtendere, unalimbikitsidwa; ndi kupatsidwa mphamvu ndi Mzimu Woyera, unakula mʼchiwerengero, ndi kukhala moopa Ambuye.
32 P'et'ros dats datsatse gúúroke b́ befere Ldiyn beyiru amantsuwotsok bíami.
Pamene Petro amayendera mpingo, anapita kukachezera oyera mtima a ku Luda.
33 Manoknowere shmt nati s'eenosh es'atse k'eets Eniyi eteef duro daats b́de'k'i.
Kumeneko anakapeza munthu dzina lake Eneya, wofa ziwalo amene anagona pa mphasa kwa zaka zisanu ndi zitatu.
34 P'et'rosuwere «Eniyo! Iyesus Krstos neen kashituwe, tuur níees'o ec'ee!» bí eti. Bíwere manoor k'az b́tuwi.
Petro anati kwa iye, “Eneya, Yesu Khristu akukuchiritsa iwe, dzuka ndipo yalula mphasa yako.” Nthawi yomweyo Eneya anayimirira.
35 Ldaanat Saronon beyiru jametsuwots bín bek't doonzo maants k'az boaani.
Anthu onse amene anakhala ku Luda ndi ku Sharoni anamuona ndipo anatembenukira kwa Ambuye.
36 Iyop'e datsatse T'abiti eteefu amants iku fa'a b tesh, Griki noonon Doork'ayi eta, b́ biitsonwere t'it'a etee, biwere sheeng keewo k'alonat t'owwotssh úni aawu imf máátsi btesh,
Ku Yopa kunali wophunzira wina dzina lake Tabita (mʼChigriki amati Dorika) amene nthawi zonse ankachita zachifundo ndiponso kuthandiza osauka.
37 Manoor bi shodat b k'iri, mashdek'tnuwere dadirotse danbani gaad'ots bin gedbok'ri.
Nthawi imeneyi anadwala ndipo anamwalira, anasambitsa thupi lake, namugoneka mʼchipinda chammwamba.
38 Ldi Iyop'esh karn bteshtsotse Iyop'eyitse fa'a Iyesus danifwots P'et'ros Lditse b́ fa'ok'owo shisht «Oona muk'i nteyawo noosh kaari waa boree» et git ashuwotsi bíyok woshbok'ri.
Popeza ku Yopa kunali pafupi ndi Luda; pamene ophunzira anamva kuti Petro anali ku Luda, anatuma anthu awiri kuti akamudandaulire kuti, “Chonde bwerani kuno msanga!”
39 Mansh P'et'ros tuut wosheetsuwotsnton b́weyi, b́ bodtsook'onowere dambani maa gáádots dek't boami, bo kenih k'irts mááts jametso bín guurdek' need' dek't eepfetst Doork' bonton kashon b beyor bwozits faaruwotsnat tah tahuwotsi bísh bokitsiri botesh,
Petro ananyamuka, napita nawo, ndipo atafika anamutengera ku chipinda chammwamba. Amasiye onse anayima momuzungulira akulira ndi kumuonetsa mwinjiro ndi zovala zina zimene Dorika ankapanga akanali moyo.
40 P'et'ros jametsuwotsnor úratse kishk'raat tuk'maldek't Ik'o b́ k'oni, duuno maantsowere aandek't «T'abitee! tuwwe!» bíeti, biwere bi ááwwotsi wogdek'at P't'rosi b s'iili, tuuwatnu beebdek'i.
Petro anatulutsa anthu onse mʼchipindamo; ndipo anagwada pansi ndi kupemphera. Anatembenukira mtembo uja nati, “Tabita, dzuka,” Tabita anatsekula maso ake, ndipo ataona Petro anakhala pansi.
41 Bíwere b́ kisho jargt bin detsdek't b́ tuuzi, bo kenihi k'irts máátsuwotsnat k'osh máántsuwotsi s'eegdek't naú kashon bo shinats b́ t'intsi.
Petro anamugwira dzanja, namuyimiritsa. Ndipo anayitana okhulupirira ndi amasiye namupereka wamoyo.
42 Keewanuwere Iyop'e dats jamatse b́ daneyi, ay ashuwotswere Doonzon boamani.
Zimenezi zinadziwika ku Yopa konse, ndipo anthu ambiri anakhulupirira Ambuye.
43 P'et'ros Simo'oni eteets gook' shik'iru ikonton ay aawosh Iyop'en b́ beyi.
Petro anakhala ku Yopa kwa masiku ambiri kwa munthu wina, dzina lake Simoni, mmisiri wa zikopa.

< Woshetswotsi 9 >