< Segalaia 4 >

1 A: igele amo da musa: nama sia: dasu, da nama bu misini, na da golai dianabeyale dawa: le, na didilisi.
Kenaka mngelo amene amayankhula nane anabwerera nandidzutsa, ngati mmene amadzutsira munthu amene ali mʼtulo.
2 E da nama amane adole ba: i, “Dia da adi ba: sala: ?” Na da bu adole i, “Na da gamali bugisu ba: i gouliga hamoi amo ba: be. Gamali bai dabuagado da susuligi salima: ne fagoi gala. Amola gamali bugisu bai amoga da gamali fesuale gala. Amola gamali afae afae da wigi sogebi fesuale gala ba: sa.
Anandifunsa kuti, “Kodi ukuona chiyani?” Ndinayankha kuti, “Ine ndikuona choyikapo nyale, chonse chagolide ndi mbale pamwamba pake ndi nyale zoyaka zisanu ndi ziwiri, iliyonse ili ndi zibowo zisanu ndi ziwiri zolowetsera zingwe zoyatsira.
3 Gamali bugisu bai la: idi la: idili da olife ifa lelebe ba: sa.”
Ndiponso pambali pake pali mitengo ya olivi iwiri, umodzi uli kumanja kwa mbaleyo ndipo winawo kumanzere.”
4 Amalalu, na da a: igele dunuma adole ba: i, “Hina! Amo liligi ea bai da adi olelesala: ?”
Ndinamufunsa mngelo amene amayankhula nane kuti, “Kodi zimenezi nʼchiyani mbuye wanga?”
5 E da nama amane adole ba: i, “Di da amo hame dawa: bela: ?” Na bu adole i, “Hina! Na da hame dawa: !” (Segalaia 4:10b asili Segalaia 4:14 da idisu dunu ilia bai noga: le dawa: ma: ne goeguda: dedei) b A: igele dunu da nama amane sia: i, “Gamali fesuale da fedege agoane Hina Gode Ea si fesuale, amoga E da osobo bagade fifi asi gala huluane ba: lala.” Amalalu, na da ema adole ba: i, “Olife ifa aduna gamali bugisu bai la: idi la: idi lelebe amo elea bai da adila: ? Amola olife amoda aduna amo da gouliga hamoi buni damagelei aduna amoga olife susuligi da amodili bubuga: sa, amo la: idi la: idi lela, amo elea bai da adila: ?” E da nama amane adole ba: i, “Di da amo hame dawa: bela: ?” Nabu adole i, “Hina! Na da hame dawa:” Amalalu, e da nama bu adole i, “Amo liligi aduna da fedege agoane dunu aduna amo Gode (E da osobo bagade huluanedafa amoga Hina Gode esala) E da Ea hawa: hamoma: ne, elama susuligi sogagala: le ilegele lai.”
Iye anandiyankha kuti, “Kodi iwe sukuzidziwa zimenezi?” Ndinayankha kuti, “Ayi mbuye wanga.”
6 A: igele dunu da nama amo Hina Gode Ea sia: ne iasu Selababelema sia: ma: ne sia: i, “Di da dadi gagui wa: i ilia gasaga o dia gasa, amoga hame hasalasimu. Be di da Na A: silibu amoga hasalasimu.
Choncho iye anandiwuza kuti, “Mawu a Yehova kwa Zerubabeli ndi awa: ‘Osati mwa nkhondo kapena ndi mphamvu, koma ndi Mzimu wanga,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
7 Di da ahoasea, dia logo ga: su liligi goumi bagade defele ba: mu. Be Na gasaga amo da alalolesimu. Di da Debolo diasu bu gagumu. Amola, amo dagosea, di da fa: nodafa igi ligisisia, dunu huluane da, ‘Noga: idafa! Noga: idafa!’ nodone sia: mu.”
“Kodi ndiwe yani, iwe phiri lamphamvu? Pamaso pa Zerubabeli udzasanduka dziko losalala. Pamenepo adzabweretsa mwala wotsiriza. Akamadzawuyika pamwamba anthu adzafuwula kuti, ‘Mulungu adalitse Nyumbayi! Mulungu adalitse Nyumbayi!’”
8 Hina Gode da eno sia: ne iasu nama i.
Ndipo Yehova anayankhulanso nane kuti,
9 E amane sia: i, “Selababele da Debolo bai fa: si dagoi. Amola e da Debolo diasu amo gaguli dagomu. Amo hou ba: sea, Na fi dunu da Na da di ilima asunasi, amo dawa: digimu.
“Manja a Zerubabeli ndiwo ayika maziko a Nyumbayi; adzatsiriza ndi manja ake omwewo. Pamenepo iwe udzadziwa kuti Yehova Wamphamvuzonse ndiye anakutuma.
10 Wali, hawa: hamosu da hame hehenaiba: le, ilia da da: i dioi. Be fa: no ilia da Selababele gebewane Debolo diasu gagulalebe ba: sea, ilia da hahawane ba: mu.”
“Ndani wanyoza tsiku la zinthu zazingʼono? Anthu adzasangalala akadzaona chingwe choyezera mʼmanja mwa Zerubabeli. (“Nyale zisanu ndi ziwirizi ndi maso a Yehova, amene amayangʼanayangʼana pa dziko lapansi.”)
Kenaka ndinafunsa mngelo uja kuti, “Kodi mitengo ya olivi iwiri ili kumanja ndi kumanzere kwa choyikapo nyalechi ikutanthauza chiyani?”
Ndinamufunsanso kuti, “Kodi nthambi ziwiri za mtengo wa olivi zomwe zili pambali pa mipopi yodzera mafuta iwiri yagolide zikutanthauza chiyani?”
Iye anandiyankha kuti, “Kodi iwe sukuzidziwa zimenezi?” Ine ndinati, “Ayi mbuye wanga.”
Choncho iye anati, “Amenewa ndi anthu awiri amene adzozedwa kuti atumikire Ambuye pa dziko lonse lapansi.”

< Segalaia 4 >