< Segalaia 12 >
1 Hina Gode da mu fadegale gai. E da osobo bagade hahamoi. E da osobo bagade dunu ilima esalusu iasu. Amo Hina Gode da Isala: ili soge ea fa: no misunu hou olelema: ne, amo sia: ne iasu i.
Uthenga wa Yehova kwa Israeli. Yehova, amene amayala mlengalenga, amene amayika maziko a dziko lapansi, ndiponso amene amalenga mzimu wokhala mwa munthu, akunena kuti,
2 E da amane sia: sa, “Na da Yelusaleme amo faigelei waini hanoga nabai agoane hamomu. Fifi asi gala ema sisiga: le disi da amoga nalu, adini ba: i dunu defele felowale masunu. Amola ilia da Yelusaleme doagala: musa: masea, ilia da Yuda moilai bai bagade huluane doagala: mu.
“Taonani, ndidzasandutsa Yerusalemu kukhala chakumwa choledzeretsa chimene chidzasokoneza mitundu yonse ya anthu yomuzungulira. Yuda adzazingidwa pamodzinso ndi Yerusalemu.
3 Be amo esoha, Na da Yelusaleme amo igi dioi bagadedafa agoane hamomu. Nowa fifi asi gala da amo gaguia gadomusa: dawa: sea da se bagade nabimu. Osobo bagade fifi asi gala huluane da Yelusaleme doagala: musa: gilisimu.
Pa tsiku limenelo, pamene mitundu yonse ya anthu a dziko lapansi idzasonkhana kulimbana naye, ndidzasandutsa Yerusalemu thanthwe losatheka kusunthidwa ndi mitundu yonse ya anthu. Onse oyesa kumusuntha adzadzipweteka.
4 Amo esoha, Na da ilia hosi huluane beda: ne fofogadigima: ne hamomu. Amola ilima fila heda: i dunu huluane Na da doula masa: ne hamomu. Na da Yuda fi sosodo aligimu, be ilima ha lai dunu ilia hosi si huluane Na da dofonesimu.
Pa tsiku limenelo kavalo aliyense ndidzamuchititsa mantha kuti asokonezeke, ndipo wokwerapo wake ndidzamuchititsa misala,” akutero Yehova. “Ndidzayangʼanira nyumba ya Yuda koma ndidzachititsa khungu akavalo onse a anthu a mitundu ina.
5 Amasea, Yuda sosogo fi ilia da ilisu amane sia: mu, ‘Hina Gode Bagadedafa da Ea fi dunu Yelusaleme ganodini esalebe ilima gasa fufugilisisa.’
Pamenepo atsogoleri a Yuda adzayankhula mʼmitima mwawo kuti, ‘Anthu a ku Yerusalemu ndi amphamvu, chifukwa Yehova Wamphamvuzonse ndiye Mulungu wawo.’
6 Amo galu, Na da Yuda sosogo fi ili, lalu amo da iwila ganodini o gagoma bugi denesi ganodini nebe, agoane hamomu. Ilia da ili sisiga: le fifi asi gala amo huluane wadela: lesimu. Yelusaleme fi dunu ilia da ilia moilai bai bagade ganodini hahawane gaga: iwane esalebe ba: mu.
“Pa tsiku limenelo ndidzasandutsa atsogoleri a Yuda kukhala ngati mbawula yotentha pakati pa nkhuni, ngati sakali yoyaka pa mitolo ya tirigu. Adzatentha mitundu yonse ya anthu yowazungulira, kumanja ndi kumanzere, koma Yerusalemu sadzasuntha pa malo ake.
7 Na, Hina Gode, da hidadea Yuda dadi gagui wa: i ilima hasalasu imunu. Amasea, Da: ibidi egaga fi dunu amola Yelusaleme fi dunu iligaga fi dunu ilima nodosu da Yuda fi dunu eno ilima nodosu hame baligimu.
“Yehova adzapulumutsa malo okhala Yuda poyamba, kuti ulemu wa nyumba ya Davide ndi wa anthu okhala mu Yerusalemu usapambane ulemu wa Yuda.
8 Amo esoha, Hina Gode da Yelusaleme ganodini esalebe dunu gaga: mu. Ilia gilisisu ganodini, gogayaidafa dunu da Da: ibidi defele gasa bagade ba: mu. Da: ibidi egaga fi dunu da Hina Gode Ea a: igele dunu amola Godedafa amo defele, ili sigi masunu.
Pa tsiku limenelo Yehova adzatchinjiriza onse okhala mu Yerusalemu, kotero kuti anthu ofowoka kwambiri pakati pawo adzakhala ngati Davide, ndipo nyumba ya Davide idzakhala ngati Mulungu, ngati mngelo wa Yehova wowatsogolera.
9 Amo esoha, nowa fifi asi gala da Yelusaleme doagala: musa: adoba: sea, Na da amo fi gugunufinisimu.
Pa tsiku limenelo ndidzawononga mitundu yonse yofuna kuthira nkhondo Yerusalemu.
10 Na da Da: ibidi egaga fi dunu amola Yelusaleme fi dunu eno huluane amo asigidafa amola sia: ne gadosu a: silibu amoga nabalesimu. Ilia da Na bogoma: ne soi dagoi, amola amo esoha ilia da Na bu ba: muba: le, dunu da ea magobo mano bogoiba: le didiga: su defele, ha: giwane didiga: mu.
“Ndipo pa nyumba ya Davide ndi pa anthu okhala mu Yerusalemu ndidzakhuthulirapo mzimu wachisomo ndi wopemphera. Iwo adzandiyangʼana Ine, amene anamubaya, ndipo adzamulirira kwambiri monga momwe munthu amalirira mwana wake mmodzi yekhayo, ndiponso adzamva chisoni kwambiri monga momwe amachitira ndi mwana woyamba kubadwa.
11 Megidou umi ganodini, ogogole ‘gode’ Ha: ida: delimone da bogoiba: le, dunu da ha: giwane didiga: sa. Na da Yelusaleme amoma bu masea, Yelusaleme fi dunu ilia didiga: su da amo defele ba: mu.
Pa tsiku limenelo mudzakhala kulira kwakukulu mu Yerusalemu, monga kulira kwa ku Hadadi-Rimoni ku chigwa cha Megido.
12 Yuda soge ganodini, sosogo fi huluane afafai da higagale dimu. Da: ibidi egaga fifi misi, Na: ida: ne egaga fifi misi, Lifai egaga fifi misi, Simiai egaga fifi misi amola eno fifi misi huluane da higagale didiga: mu. Dunu da ilisu didiga: mu amola uda da ilisu didiga: mu.
Dziko lidzalira kwambiri, fuko lililonse pa lokha, akazi awo pa okhanso: fuko la Davide pamodzi ndi akazi awo, fuko la Natani pamodzi ndi akazi awo,
nyumba ya Levi pamodzi ndi akazi awo, fuko la Simei pamodzi ndi akazi awo,
ndiponso mafuko onse pamodzi ndi akazi awo.