< Soloumane ea Gesami 6 >

1 “Saga! Baligili noga: i ba: su uda! Dia sasagesu da habidili asibala: ? Ninia di fidili hogole ba: musa: , ea asi logo ninima adoma.” Uda da amane sia: i,
Iwe wokongola kuposa akazi onsewa, kodi wokondedwa wakoyo wapita kuti? Kodi wokondedwa wakoyo wakhotera njira iti kuti timufunefune pamodzi ndi iwe?
2 “Na sasagesu dunu da ea ifabia (amogawi ‘bolosame’ ifa da heda: la) amoga asi dagoi. E da amogawi ea sibi wa: i amoma ha: i manu iana amola ‘lili’ mosoi gagadolala.
Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake, ku timinda ta zokometsera zakudya, akukadyetsa ziweto zake ku minda, ndiponso akuthyola maluwa okongola.
3 Na sasagesu dunu da na: Amola na da ea: E da ‘lili’ bugi amo ganodini ea sibi wa: i amoma ha: i manu iana.” Dunu da amane sia: i,
Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga; amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.
4 “Na dogolegei! Di da Yelusaleme moilai bai bagade amola Disa moilai bai bagade defele, noga: idafa ba: sa. Dunu da amo moilai bai bagade ela hahalogoboi ba: sea, fofogadigiba: le, habe ha: sa. Amola dia isisima: goi ba: sea, agoaiwane hamosa.
Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza, wokongola kwambiri ngati Yerusalemu, ndiwe woopsa ngati gulu lankhondo lonyamula mbendera.
5 Dia si hamega ba: legama! Dia si da na gagulaligisa! Dia dialuma hinabo da goudi wa: i amo da Gilia: de agologa soagagala: ahoa agoane giginisa dabe ba: sa.
Usandipenyetsetse; pakuti maso ako amanditenga mtima. Tsitsi lako lili ngati gulu la mbuzi zikutsetsereka kuchokera ku Giliyadi.
6 Dia bese da sibi amo da hinabo waha dodofei agoane ba: sa. Afae da hame gumi ba: sa. Ilia huluane da defele dadalei ba: sa.
Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zimene zikubwera kuchokera kokazisambitsa, iliyonse ili ndi ana amapasa, palibe imene ili yokha.
7 Dia ba: da dia odagi dedebosu abula baligiadili da nenemegisa.
Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu, masaya ako ali ngati mabandu a makangadza.
8 Defea! Hina bagade da uda 60 lamu da defea. Amola gidisedagi uda 80 amola uda afini idimu hamedei lamu da defea.
Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60, ndi azikazi 80, ndi anamwali osawerengeka;
9 Be na da afae fawane ni dogolegesa. Amola amo da ‘dafe’ sio defele, isisima: goi ba: sa. E da ea: me ea dogolegei uda mano afae fawane gala. Uda huluane ema ba: le nodone sia: sa. Hina bagade uda ilia, amola gidi sedagi uda ilia da e nodoma: ne gesami hea: sa.
koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense; mwana wamkazi yekhayo wa amayi ake, mwana wapamtima wa amene anamubereka. Anamwali anamuona ndipo anamutcha wodala; akazi a mfumu ndi azikazi anamutamanda.
10 Amo da nowala: ? Ea ba: la ahoabe da eso mabe agoai ba: sa. E da isisima: goi amola hadigi. E da eso amola oubi agoai, si nenemegini, ba: mu gogolei.
Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha, wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa, wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?
11 Na da ‘amode’ ifa bugi bobodole ganodini amo nono heda: i amola lubi gaheabolo efega lai amola ‘bomigala: nidi’ ifa amo ea mosoi ba: la misi dagoi.
Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi kukayangʼana zomera zatsopano ku chigwa, kukaona ngati mpesa waphukira kapena ngati makangadza ali ndi maluwa.
12 Na da yagugubi. Sa: liode genonesisu dunu da gegemusa: hanai gala, amo defele na da dima sasagesu hou hamomu hanai.” Yelusaleme uda ilia da amane sia: i,
Ndisanazindikire kanthu, ndinakhala ngati ndikulota kuti ndili mʼgaleta pambali pa mfumu yanga.
13 “Siogoma! Siulame uda a: fini! Di siogoma! Ninia ba: musa: , dia siogoma!” Uda da amane sia: i, “Na da la: idi amola la: idi dadalele lefulubi dunu dogoa siogosea, dilia abuliba: le na ba: musa: hanabela: ?”
Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami; bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe! Mwamuna Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami, pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?

< Soloumane ea Gesami 6 >