< Gesami Hea:su 85 >

1 Hina Gode, Di da Dia soge amoma asigi hou hamoi, amola Di da Isala: ili bu noga: le hahamonesi.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Yehova munakomera mtima dziko lanu; munabwezeretsa ulemerero wa Yakobo.
2 Di da Dia dunu ilia wadela: i hou gogolema: ne olofoi dagoi, amola ilia wadela: i hou huluane gogolema: ne olofolesi dagoi.
Munakhululukira mphulupulu za anthu anu ndi kuphimba machimo awo onse. (Sela)
3 Di da ilima ougisu amo yolesi dagoi, amola gasa bagade nimi hou amo Di guminisi dagoi.
Munayika pambali ukali wanu wonse ndi kutembenuka kuchoka ku mkwiyo wanu woopsa.
4 Nini gaga: su Gode, nini bu oule sinidigima, amola ninima hahawane hame ba: su amo yolesima!
Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, ndipo mutichotsere mkwiyo wanu.
5 Di da mae yolele ninima gebewane ougi dialoma: bela: ? Dia ougi da mae gumini gebewane dialoma: bela: ?
Kodi mudzatikwiyira mpaka liti? Kodi mudzapitiriza kukwiya pa mibado yathu yonse?
6 Nini bu gasa filisima, amola Dia fi dunu ninia da Dima nodone sia: nanumu.
Kodi simudzatitsitsimutsanso, kuti anthu anu asangalale mwa Inu?
7 Hina Gode, Dia mae fisili asigidafa hou amo ninima olema, amola Dia nini fidili gaga: ma.
Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova, ndipo tipatseni chipulumutso chanu.
8 Na da Hina Gode Ea sia: be amo nabala. E da Ea fi dunuma hahawane olofosu hou amo imunusa: ilegele sia: sa, be amo da ninia musa: gagaoule hamonanusu hou amoga hame buhagisia,
Ndidzamvetsera zimene Yehova Mulungu adzanena; Iye amalonjeza mtendere kwa anthu ake, oyera mtima ake, koma musawalole kuti abwerere ku zopusa.
9 E da dafawanedafa Ema nodone sia: be dunu amo gaga: musa: momagele ouesala, amola Ea gaga: su hou da ninia soge amo ganodini dialumu.
Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye, kuti ulemerero wake ukhale mʼdziko lathu.
10 Asigi hou amola didili hamosu hou da ela disimu! Moloidafa hou amola olofosu hou da ela yosia: mu.
Chikondi ndi kukhulupirika zimakumana pamodzi; chilungamo ndi mtendere zimapsompsonana.
11 Dunu ilia madelagisu hou da osoboga gudunini gado heda: mu, amola Gode Ea moloidafa hou amo da fedege agoane Hebenega gadonini gudu ba: legudumu.
Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi, ndipo chilungamo chimayangʼana pansi kuchokera kumwamba.
12 Hina Gode da nini bu noga: le hahamonesimu amola ninia soge da ha: i manu noga: le heda: mu.
Ndithu Yehova adzapereka chimene chili chabwino, ndipo dziko lathu lidzapereka zokolola zake.
13 Moloidafa hou da Hina Gode Ea midadi bisili, E misa: ne logo fofodola masunu.
Wolungama amapita patsogolo pake ndi kukonza njira za mapazi ake.

< Gesami Hea:su 85 >